< Psalmi 2 >

1 Zašto se bune narodi, zašto puci ludosti snuju?
Nʼchifukwa chiyani anthu a mitundu ina akufuna kuchita chiwembu? Akonzekeranji zopanda pake anthu?
2 Ustaju kraljevi zemaljski, knezovi se rotÄe protiv Jahve i Pomazanika njegova:
Mafumu a dziko lapansi akugwirizana nazo; ndipo olamulira asonkhana pamodzi kulimbana ndi Ambuye ndi wodzozedwa wakeyo.
3 “Skršimo okove njihove i jaram njihov zbacimo!”
Iwo akunena kuti, “Tiyeni timasule magoli awo ndipo titaye zingwe zawo.”
4 Smije se onaj što na nebu stoluje, Gospod im se podruguje.
Wokhala mmwamba akuseka; Ambuye akuwanyoza iwowo.
5 Tad im veli u svom gnjevu, žestinom ih on zbunjuje:
Ndipo iye awadzudzula mu mkwiyo wake ndi kuwaopseza mu ukali wake, kunena kuti,
6 “TÓa ja kralja svog postavih nad Sionom, svojom svetom gorom.”
“Ine ndakhazikitsa mfumu yanga pa Ziyoni, phiri langa loyera.”
7 Obznanjujem odluku Jahvinu: Gospodin mi reče: “Ti si sin moj, danas te rodih.
Ine ndidzalengeza zimene Yehova walamula: Iye anati kwa Ine, “Iwe ndiwe mwana wanga; lero Ine ndakhala Atate ako.
8 Zatraži samo, i dat ću ti puke u baštinu, i u posjed krajeve zemaljske.
Tandipempha, ndipo ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ikhale cholowa chako; malekezero a dziko lapansi kuti akhale chuma chako.
9 Vladat ćeš njima palicom gvozdenÄom i razbit ih kao sud lončarski.”
Iweyo udzawalamulira ndi ndodo yaufumu yachitsulo; udzawaphwanya zidutswazidutswa ngati zowumba zadothi.”
10 Opametite se sada, vi kraljevi, Urazumite se, suci zemaljski.
Kotero, inu mafumu, chenjerani; chenjezedwani, inu olamulira a dziko lapansi.
11 Služite Jahvi sa strahom, s trepetom se pokorite njemu,
Tumikirani Yehova mwa mantha ndi kukondwerera ulamuliro wake monjenjemera.
12 da se ne razgnjevi te ne propadnete na putu, kad uskoro plane srdžba njegova. Blago svima koji se njemu utječu!
Mpsopsoneni mwanayo kuti angakwiye; kuti mungawonongedwe mʼnjira zanu, pakuti ukali wake utha kuuka mʼkanthawi kochepa. Odala ndi onse amene amathawira kwa Iye.

< Psalmi 2 >