< Psalmi 100 >

1 Psalam. Zahvalnica. Kliči Jahvi, zemljo sva!
Salimo. Nyimbo yothokoza. Fuwulani kwa Yehova mwachimwemwe, inu dziko lonse lapansi.
2 Služite Jahvi u veselju! Pred lice mu dođite s radosnim klicanjem!
Mulambireni Yehova mosangalala; bwerani pamaso pake ndi nyimbo zachikondwerero.
3 Znajte da je Jahve Bog: on nas stvori, i mi smo njegovi, njegov smo narod i ovce paše njegove.
Dziwani kuti Yehova ndi Mulungu. Iye ndiye amene anatipanga ndipo ife ndife ake; ndife anthu ake, nkhosa za pabusa pake.
4 Uđite s hvalama na vrata njegova, u dvore njegove s pjesmama; hvalite ga, ime mu slavite!
Lowani ku zipata zake ndi chiyamiko ndi ku mabwalo ake ndi matamando; muyamikeni ndi kutamanda dzina lake.
5 Jer dobar je Jahve, dovijeka je ljubav njegova, od koljena do koljena vjernost njegova.
Pakuti Yehova ndi wabwino ndipo chikondi chake ndi chamuyaya; kukhulupirika kwake nʼkokhazikika pa mibado ndi mibado.

< Psalmi 100 >