< 诗篇 127 >
1 所罗门上行之诗。 若不是耶和华建造房屋, 建造的人就枉然劳力; 若不是耶和华看守城池, 看守的人就枉然警醒。
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Salimo la Solomoni. Yehova akapanda kumanga nyumba, omanga nyumbayo agwira ntchito pachabe. Yehova akapanda kulondera mzinda, mlonda akanangolondera pachabe.
2 你们清晨早起,夜晚安歇, 吃劳碌得来的饭,本是枉然; 惟有耶和华所亲爱的,必叫他安然睡觉。
Mumangodzivuta nʼkulawirira mmamawa ndi kusagona msanga madzulo, kuvutikira chakudya choti mudye, pakuti Iye amapereka tulo kwa amene amawakonda.
3 儿女是耶和华所赐的产业; 所怀的胎是他所给的赏赐。
Ana ndiye cholowa chochokera kwa Yehova, ana ndi mphotho yochokera kwa Iye.
Ana a pa unyamata ali ngati mivi mʼmanja mwa munthu wankhondo.
5 箭袋充满的人便为有福; 他们在城门口和仇敌说话的时候, 必不至于羞愧。
Wodala munthu amene motengera mivi mwake mwadzaza. Iwo sadzachititsidwa manyazi pamene alimbana ndi adani awo pa zipata.