< 詩篇 83 >
1 詠【求消滅聯盟的異民】阿撒夫的詩歌。 上主,求您不要一言不發,天主,您們不要靜默無話!
Nyimbo. Salimo la Asafu. Inu Mulungu musakhale chete; musangoti phee, Mulungu musangoti duu.
Onani adani anu akuchita chiwawa, amene amadana nanu autsa mitu yawo.
3 相聚密謀,陷害您的百姓,商議攻擊您保護的人民,
Mochenjera iwo akukambirana za chiwembu kutsutsana ndi anthu anu; Iwo akukonzekera kutsutsana ndi omwe mumawakonda.
4 說:大家來,由萬民將要他們驅散,使以色列的名不再被記念。
Iwo akunena kuti, “Bwerani” akutero, “Tiyeni tiwononge mtundu wonsewu kuti dzina la Israeli lisakumbukikenso.”
Ndi mtima umodzi akukonzekera chiwembu; Iwo achita mgwirizano kutsutsana nanu:
Matenti a Edomu ndi Aismaeli, Mowabu ndi Ahagiri,
7 還有革巴耳、阿孟和阿瑪肋克人,且有培肋舍特人和提洛的居民,
Agebala, Aamoni ndi Aamaleki, Afilisti, pamodzi ndi anthu a ku Turo.
Ngakhalenso Aasiriya aphatikizana nawo kupereka mphamvu kwa ana a Loti. (Sela)
9 求你對待他們像對待米德楊人,像在克雄河對待息色辣和雅賓,
Muwachitire zomwe munachitira Amidiyani, monga munachitira Sisera ndi Yabini ku mtsinje wa Kisoni.
Amene anawonongedwa ku Endori ndi kukhala ngati zinyalala.
11 使他們的王侯要與敖勒布和東一樣,使他們的將領與巴黑和匝耳慕一樣,
Anthu awo otchuka muwachite zomwe munachita Orebu ndi Zeebu ana a mafumu muwachite zomwe munachita Zeba ndi Zalimuna,
12 因為他們都曾如此說過:我們去佔領天主的住所。
amene anati, “Tiyeni tilande dziko la msipu la Mulungu.”
13 我的天主,求您使他們像旋風捲起的落葉,求您使他們像狂風吹起的碎楷,
Muwasandutse fumbi lowuluka, Inu Mulungu wanga, ngati mankhusu owuluka ndi mphepo.
14 好像被火燐焚燒的樹林,又似被火燄燃燒的山陵;
Monga moto umatentha nkhalango, kapena malawi a moto kuyatsa phiri,
15 求您也這樣以您的颶風驅散他們,以您的暴雨驚嚇他們。
kotero muwathamangitse ndi mphepo yamkuntho, ndi kuwachititsa mantha ndi namondwe.
16 上主,求您羞辱他們的面容,是為叫他們尋求您的聖名;
Muphimbe nkhope zawo ndi manyazi kuti adzafunefune dzina lanu Yehova.
Achite manyazi ndi mantha nthawi zonse; awonongeke mwa manyazi.
18 從此,認識您的名號是雅威,惟有您在普天下至尊無對。
Adziwe kuti Inu amene dzina lanu ndi Yehova, ndinu nokha Wammwambamwamba pa dziko lonse lapansi.