< 詩篇 126 >
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni, tinali ngati amene akulota.
2 那時我們滿口喜氣盈盈,我們雙脣其樂融融。那時外邦異民讚歎不已:上主向他們行了何等奇事!
Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka; malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe. Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti, “Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”
Yehova watichitira zinthu zazikulu, ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.
4 上主,求您轉變我們的命運!就像乃革布有流水的澆淋。
Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova, monga mitsinje ya ku Negevi.
Iwo amene amafesa akulira, adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.
6 他們邊行邊哭,出去播種耕耘,他們載欣載奔,回來背著禾捆。
Iye amene amayendayenda nalira, atanyamula mbewu yokafesa, adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe, atanyamula mitolo yake.