< 詩篇 115 >
1 上主,光榮不要歸於我們,不要歸於我們!只願那個光榮完全歸於您的聖名,那是為了您的慈愛,為了您的忠誠。
Kwa ife ayi Yehova, kwa ife ayi koma ulemerero ukhale pa dzina lanu, chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika ndiponso chifukwa cha kukhulupirika kwanu.
Chifukwa chiyani anthu a mitundu ina akunena kuti, “Mulungu wawo ali kuti?”
Mulungu wathu ali kumwamba; Iye amachita chilichonse chimene chimamukondweretsa.
Koma mafano awo ndi siliva ndi golide, opangidwa ndi manja a anthu.
Pakamwa ali napo koma sayankhula, maso ali nawo koma sapenya;
makutu ali nawo koma samva, mphuno ali nazo koma sanunkhiza;
7 有手,而不能動,有腳,而不能行,有喉,而不發聲。
manja ali nawo koma akakhudza samva kanthu; mapazi ali nawo koma sayenda; kapena pakhosi pawo kutulutsa mawu.
8 鑄造偶像的人,將與偶像同亡;凡信賴偶像的人,也將是一樣。
Anthu amene amapanga mafanowo adzafanana nawo, chimodzimodzinso onse amene amadalira mafanowo.
Inu Aisraeli, dalirani Yehova; Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.
10 亞郎的家族也信賴上主,祂是他們的助佑和盾護;
Iwe nyumba ya Aaroni, dalira Yehova; Iye ndiye thandizo lako ndi chishango chako.
11 敬愛上主的人信賴上主,祂是他們的助佑和盾護。
Inu amene mumaopa Iye, dalirani Yehova; Iye ndiye thandizo lanu ndi chishango chanu.
12 上主眷念我們,也必給我們祝福,祝福以色列家族,也祝福亞郎家族;
Yehova watikumbukira ndipo adzatidalitsa: adzadalitsa nyumba ya Israeli, adzadalitsa nyumba ya Aaroni,
13 祂向敬愛上主的人祝福,不拘貴賤都要獲得祝福,
adzadalitsa iwo amene amaopa Yehova; aangʼono ndi aakulu omwe.
14 願上主使您們的人口繁昌,使您們和您們的子女興旺!
Yehova akuwonjezereni madalitso; inuyo pamodzi ndi ana anu.
15 願您們蒙受上主的祝福,祂是上天下地的造化主。
Mudalitsidwe ndi Yehova, Wolenga kumwamba ndi dziko lapansi.
16 蒼天確實是上主的蒼天,上主給世人賞賜了塵寰。
Kumwamba ndi kwa Yehova, koma dziko lapansi Iye walipereka kwa anthu.
17 死人們不能夠讚美上主,降入陰府的人也不能夠,
Si anthu akufa amene amatamanda Yehova, amene amatsikira kuli chete;
ndi ife amene timatamanda Yehova, kuyambira tsopano mpaka muyaya. Tamandani Yehova.