< 箴言 15 >
Kuyankha kofatsa kumathetsa mkwiyo, koma mawu ozaza amautsa ukali.
Munthu wanzeru amayankhula zinthu za nzeru, koma pakamwa pa zitsiru pamatulutsa za uchitsiru.
Maso a Yehova ali ponseponse, amayangʼana pa oyipa ndi abwino omwe.
4 撫慰的言辭,有如生命樹;刻薄的言語,能刺傷人心。
Kuyankhula kodekha kuli ngati mtengo wopatsa moyo, koma kuyankhula kopotoka kumapweteka mtima.
5 愚蠢的人,輕視父親的管教;遵守規勸的,為人必精明。
Chitsiru chimanyoza mwambo wa abambo ake, koma wochenjera amasamala chidzudzulo.
Munthu wolungama amakhala ndi chuma chambiri, zimene woyipa amapindula nazo zimamugwetsa mʼmavuto.
Pakamwa pa anthu anzeru pamafalitsa nzeru; koma mitima ya zitsiru sitero.
Nsembe za anthu oyipa zimamunyansa Yehova, koma amakondwera ndi pemphero la anthu owona mtima.
Ntchito za anthu oyipa zimamunyansa Yehova koma amakonda amene amafunafuna chilungamo.
10 離棄正道的,必遭嚴罰;憎恨規勸的,只有死亡。
Amene amasiya njira yabwino adzalangidwa koopsa. Odana ndi chidzudzulo adzafa.
11 陰府和冥域,都明擺在上主面前,何況世人的心懷! (Sheol )
Manda ndi chiwonongeko ndi zosabisika pamaso pa Yehova, nanji mitima ya anthu! (Sheol )
Wonyoza sakonda kudzudzulidwa; iye sapita kwa anthu anzeru.
13 心中愉快,使面容煥發;心中悲傷,精神即頹喪。
Mtima wokondwa umachititsa nkhope kukhala yachimwemwe, koma mtima wosweka umawawitsa moyo.
14 明達人的心,尋求智識;愚昧人的口,飽食昏愚。
Mtima wa munthu wozindikira zinthu umafunafuna nzeru, koma pakamwa pa zitsiru pamadya uchitsiru wawo.
15 心情憂傷的,日日困坐愁城;心胸暢快的,時時如享喜宴。
Munthu woponderezedwa masiku ake onse amakhala oyipa, koma mtima wachimwemwe umakhala pa chisangalalo nthawi zonse.
16 少有財寶而敬畏上主,勝於富有財寶而諸多煩惱。
Kuli bwino kukhala ndi zinthu pangʼono nʼkumaopa Yehova, kusiyana ndi kukhala ndi chuma chambiri uli pamavuto.
Kuli bwino kudyera ndiwo zamasamba pamene pali chikondi, kusiyana ndi kudyera nyama yangʼombe yonenepa pamene pali udani.
18 易怒的人,常引起爭端;含忍的人,卻平息爭論。
Munthu wopsa mtima msanga amayambitsa mikangano, koma munthu woleza mtima amathetsa ndewu.
19 懶惰人的道路,有如荊棘籬笆;正直人的行徑,卻是康莊大道。
Njira ya munthu waulesi ndi yowirira ndi mtengo waminga, koma njira ya munthu wolungama ili ngati msewu waukulu.
20 智慧的兒子,是父親的喜樂;只有愚昧人,輕視自己的母親。
Mwana wanzeru amakondweretsa abambo ake, koma mwana wopusa amanyoza amayi ake.
21 無知的人,以愚昧為樂;明智的人,卻直道而行。
Uchitsiru umakondweretsa munthu wopanda nzeru, koma munthu womvetsa zinthu amayenda mowongoka.
22 缺乏考慮,計劃必要失敗;謀士眾多,策略方克有成。
Popanda uphungu zolinga zako munthu zimalephereka, koma pakakhala aphungu ambiri zolinga zimatheka.
Munthu amakondwera ndi kuyankha koyenera, ndipo mawu onena pa nthawi yake ndi okoma.
24 生命之路使明智人向上,為此他能避免向下的陰府。 (Sheol )
Munthu wanzeru amatsata njira yopita ku moyo kuti apewe malo okhala anthu akufa. (Sheol )
25 上主將拆毀驕傲人的房屋,卻要堅定寡婦的地界。
Yehova amapasula nyumba ya munthu wonyada koma amasamalira malo a mkazi wamasiye.
26 邪惡的陰謀,為上主所憎惡;溫良的言語,卻為他所喜悅。
Maganizo a anthu oyipa amamunyansa Yehova, koma mawu a anthu oyera mtima amamusangalatsa.
27 貪求財貨的,困擾自己的家庭;憎惡饋贈的,生活必能安定。
Munthu wofuna phindu mwachinyengo amavutitsa banja lake, koma wodana ndi ziphuphu adzakhala ndi moyo.
28 義人的心,只默思善事;惡人的口,只吐露惡語。
Munthu wolungama amaganizira za mmene ayankhire, koma pakamwa pa munthu woyipa pamatulutsa mawu oyipa.
Yehova amakhala kutali ndi anthu oyipa, koma amamva pemphero la anthu olungama.
30 晶瑩的目光,使人心曠神怡;美好的訊息,使人筋骨壯健。
Kuwala kwa maso kumasangalatsa mtima ndipo uthenga wabwino umalimbitsa munthu.
31 喜聽有益生命勸戒的人,必得列於智慧人的中間。
Womvera mawu a chidzudzulo amene apatsa moyo adzakhala pakati pa anthu anzeru.
32 避免教導的,是作賤自己;聽從規勸的,必獲得機智。
Amene amanyoza mwambo amadzinyoza yekha, koma womvera mawu a chidzudzulo amapeza nzeru zomvetsa zinthu.
33 敬畏上主,是智慧的導師;謙卑自下,是榮耀的先聲。
Kuopa Yehova kumaphunzitsa munthu nzeru, ndipo kudzichepetsa ndi ulemu chili patsogolo ndi kudzichepetsa.