< 約伯記 6 >
Tsono Yobu anayankha kuti,
2 恨不得有人衡量衡量我的痛苦,把我所受的災禍一起放在天秤上!
“Achikhala mavuto anga anayezedwa, ndipo zipsinjo zanga zonse zikanayikidwa pa sikelo!
Ndithu, zikanalemera kupambana mchenga wa ku nyanja; nʼchifukwa chake mawu anga akhala okhadzula.
4 因為全能者的箭射中了我,我的心靈喝盡它們的毒汁,天主的恐嚇列陣攻擊我。
Mivi ya Wamphamvuzonse yandibaya, thupi langa likumva ululu wa miviyo; zoopsa za Mulungu zandizinga.
5 野驢有青草,難道還嘶叫﹖牛對著草料,難道還吼鳴﹖
Kodi bulu wakuthengo amalira akakhala ndi msipu, nanga ngʼombe imalira ikakhala ndi chakudya?
Kodi chakudya chosakoma nʼkuchidya chopanda mchere, nanga choyera cha dzira chimakoma?
Zakudya zimenezi sindifuna nʼkuzilawa komwe; zakudya zimenezi zimabwerera kukhosi.
“Aa, ndikanalandira chimene ndikuchipempha, chikhala Mulungu anandipatsa chimene ndikuchiyembekezera,
achikhala chinamukomera Mulungu kuti anditswanye, kulola dzanja lake kuti lindimenye ndi kundiwonongeratu!
10 這樣,我仍有安慰,在悽慘的痛苦中,仍然喜悅,因為我沒有違犯聖者的教訓。
Pamenepo ine ndikanakhalabe ndi chitonthozo ichi, ndikanakondwa mu ululu wanga wosalekezawu podziwa kuti sindinakane mawu a Woyerayo.
11 我有什麼力量使我期待,有什麼結局使我拖延生命﹖
“Kodi mphamvu zanga nʼzotani kuti ndizikhalabe ndi chiyembekezo? Nanga zoyembekezera zanga nʼzotani kuti ndipirirebe?
Kodi ine ndili ndi mphamvu? Nanga thupi langa ndi lolimba ngati chitsulo?
13 在我內還能找到什麼作援助﹖任何扶助豈不都遠離了我﹖
Kodi ndili ndi mphamvu zodzithandizira ndekha, nanga pakuti thandizo lachotsedwa kwa ine?
14 誰不憐憫自己的友人,就是放棄了敬畏天主之心。
“Munthu amene ali kakasi ayenera kukhala ndi abwenzi odzipereka, ngakhale kuti iyeyo wasiya kuopa Wamphamvuzonse.
15 我的兄弟們詭詐有如溪水,有如水過即乾的河床。
Koma abale anga ndi wosadalirika ngati mitsinje yowuma msanga, ngati mitsinje imene imathamanga.
Ali ngati mitsinje ya madzi akuda nthawi ya dzinja, imene madzi ake amakhala ambiri chifukwa chakuchuluka kwa mvula,
17 季節一溫暖,溪水即竭,天氣一炎熱,河床即乾。
koma madziwo amasiya kuyenda nthawi yachilimwe, ndipo nthawi yotentha madziwo amawumiratu mʼmitsinjemo.
Anthu oyenda pa ngamira amapatukirako kufuna madzi; iwo amangoyendayenda nʼkufera mʼchipululu.
Anthu oyenda pa ngamira a ku Tema amafunafuna madzi, anthu amalonda apaulendo a ku Seba amafunafuna mwa chiyembekezo.
20 但他們的希望落了空,他們不管到了那裏,必狼狽不堪。
Amataya mtima chifukwa ankayembekezera kupeza madzi; koma akafika kumeneko, amangokhumudwako.
21 現今你們待我也是一樣:看見了我,就驚惶失措。
Tsono inunso mukuonetsa kuti ndinu osathandiza, mukuona chinthu choopsa kwambiri ndipo mukuchita mantha.
22 難道我說過:「請送我禮物! 把你們的財產送我一分﹖
Kodi ine ndinanenapo kuti, ‘Ndiperekereni kenakake, ndilipirireni dipo kuchokera pa chuma chanu,
23 救我擺脫仇人的權勢,贖我脫離殘暴者的掌握﹖」
ndilanditseni mʼdzanja la mdani, ndiwomboleni mʼdzanja la munthu wankhanza?’
24 請教訓我! 我必靜聽。我有什麼錯,請指示我!
“Phunzitseni, ndipo ine ndidzakhala chete; ndionetseni pomwe ndalakwitsa.
25 正義的言詞是多麼甘美! 但你們的責斥是指摘什麼﹖
Ndithu, mawu owona ndi opweteka! Koma mawu anu otsutsa akufuna kuonetsa chiyani?
26 你們豈能只在言詞上吹毛求疵﹖以絕望者的話當耳邊風﹖
Kodi inu mukufuna kundidzudzula pa zimene ndikunena, ndipo mukufuna kuyesa mawu a munthu wosweka mtima ngati mphepo chabe?
27 你們只想對孤兒擲骰下注,以你們的朋友作商品。
Inu mungathe kuchita maere kuti mugulitse ana amasiye ndi kumugulitsa bwenzi lanu.
28 現今請你們注視我,在你們注視之下,我決不說謊。
“Koma tsopano ndichitireni chifundo pamene mukundiyangʼana. Kodi ine ndingayankhule zabodza pamaso panu?
29 請你們再想一下,不要不公;請你們三思,我的正義仍然存在!
Fewani mtima, musachite zosalungama; ganiziraninso popeza chilungamo changa chikanalipobe.
Kodi pali choyipa chilichonse pa milomo yanga? Kodi pakamwa panga sipangathe kuzindikira kanthu koyipa?