< 以斯帖記 10 >
Mfumu Ahasiwero anakhometsa msonkho mʼdziko lake lonse mpaka ku zilumba zonse.
2 他所行偉大英勇的事蹟,以及顯耀摩爾德開的詳細經過,都記載在瑪待和波斯君王的年鑑上。
Ndipo ntchito zonse zochitika ndi mphamvu zake komanso ndi zonse zofotokoza za ukulu wa Mordekai, kukwezedwa kwake ndi mfumu, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Mediya ndi Peresiya?
3 猶太人摩爾德開,位僅次於薛西斯王,受猶太人的敬重,受他全體同胞的愛戴;他也努力為他的民族謀幸福,關心他的整個種族的安全。
Pakuti Mordekai Myuda uja anali wachiwiri wa mfumu Ahasiwero. Kwa Ayuda onse Mordekai anali munthu wamkulu ndipo ankamukonda chifukwa ankachitira zabwino mtundu wake ndi kufunira mtendere abale ake.