< 歷代志上 8 >
1 [本雅明支派]本亞明的長子貝拉,次子阿市貝耳,三子阿希蘭,
Benjamini anabereka Bela mwana wake woyamba, wachiwiri Asibeli, wachitatu Ahara,
wachinayi Noha ndipo wachisanu Rafa.
Ana a Bela anali awa: Adari, Gera, Abihudi,
Gera, Sefufani ndi Hiramu.
6 厄胡得的子孫:─他們是居於革巴的家族的族長,曾被擄往瑪納哈特,─
Zidzukulu za Ehudi, zimene zinali atsogoleri a mabanja a amene amakhala ku Geba ndipo zinasamutsidwa kupita ku Manahati zinali izi:
7 納阿曼、阿希雅和革辣。革辣於被擄後,生烏匝和阿希胡得。
Naamani, Ahiya ndi Gera, amene anawasamutsa ndipo anabereka Uza ndi Ahihudi.
8 沙哈辣殷休了胡生和巴辣兩妻後,在摩阿布平原生了兒子;
Saharaimu anabereka ana ku Mowabu atalekana ndi akazi ake, Husimu ndi Baara.
9 由自己的妻子曷德士生了約巴布、漆彼雅、默沙、瑪耳干、
Mwa mkazi wake Hodesi anabereka Yobabu, Zibiya, Mesa, Malikamu,
Yeusi, Sakiya ndi Mirima. Awa ndiye ana ake, atsogoleri a mabanja awo.
Mwa mkazi wake Husimu anabereka Abitubi ndi Elipaala.
12 厄耳帕耳的兒子:厄貝爾、米商和舍默得;舍默得建立了敖諾、羅得和所屬村鎮。
Ana a Elipaala anali awa: Eberi, Misamu, Semedi (amene anamanga mizinda ya Ono ndi Lodi ndi midzi yake yozungulira)
13 貝黎雅和舍瑪為住在阿雅隆家族的族長,驅逐了加特的居民。
ndiponso Beriya ndi Sema, amene anali atsogoleri a mabanja a amene ankakhala ku Ayaloni ndipo anathamangitsa nzika za ku Gati.
Mikayeli, Isipa ndi Yoha anali ana a Beriya.
Zebadiya, Mesulamu, Hiziki, Heberi,
18 依市默賴、依次里雅和約巴布,是厄耳帕耳的兒子。
Isimerai, Iziliya ndi Yobabu anali ana a Elipaala.
Elienai, Ziletai, Elieli,
Adaya, Beraya ndi Simirati anali ana a Simei.
Hananiya, Elamu, Anitotiya,
Ifideya ndi Penueli anali ana a Sasaki.
Samuserai, Sehariya, Ataliya,
Yaaresiya, Eliya ndi Zikiri anali ana a Yerohamu.
Onsewa anali atsogoleri a mabanja, anthu otchuka potsata mibado yawo, ndipo ankakhala mu Yerusalemu.
29 住在基貝紅的,有基貝紅的父親耶依耳,他的妻子名叫瑪阿加。
Yeiyeli amene amabereka Gibiyoni ankakhala ku Gibiyoni. Dzina la mkazi wake linali Maaka,
30 他的長子阿貝冬,其次是族爾、克士巴耳、乃爾、納達布、
ndipo mwana wake woyamba anali Abidoni, motsatana ndi Zuri, Kisi, Baala, Neri, Nadabu,
32 米刻羅特;米刻羅特生史瑪。他們兄弟彼此為鄰,住在耶路撒冷。[撒耳烏的族譜]
ndi Mikiloti, amene anabereka Simea. Iwowa ankakhalanso ku Yerusalemu ndi abale awo.
33 乃爾生克士,克士生撒烏耳,撒烏耳生約納堂、瑪耳基叔亞、阿彼納達布和依市巴耳。
Neri anabereka Kisi. Kisi anabereka Sauli, ndipo Sauli anabereka Yonatani, Maliki-Suwa, Abinadabu ndi Esibaala.
Mwana wa Yonatani anali Meri-Baala, amene anabereka Mika.
Ana a Mika anali awa: Pitoni, Meleki, Tareya ndi Ahazi.
36 阿哈茲生約阿達,約阿達生阿肋默特、阿次瑪委特和齊默黎、齊默黎生摩匝,
Ahazi anabereka Yehoyada, Yehoyada anabereka Alemeti, Azimaveti ndi Zimuri, ndipo Zimuri anabereka Moza.
37 摩匝生彼納;彼納的兒子勒法雅,勒法雅的兒子厄拉撒,厄拉撒的兒子阿責耳;
Moza anabereka Bineya. Ana ake anali Rafa, Eleasa ndi Azeli.
38 阿責耳有六個兒子,他們的名字是:阿次黎岡、波革魯、依市瑪耳、沙黎雅、敖巴狄雅和哈南:以上是阿責耳的兒子。
Azeli anali ndi ana asanu ndi mmodzi, ndipo mayina awo anali awa: Azirikamu, Bokeru, Ismaeli, Seariya, Obadiya ndi Hanani. Onsewa anali ana a Azeli.
39 他兄弟厄舍克的兒子:長子烏藍,次子耶烏士,三子厄里培肋特。
Ana a Eseki mʼbale wake anali awa: Mwana wake woyamba Ulamu, wachiwiri Yeusi ndipo wachitatu Elifeleti.
40 烏藍的兒子是英勇的戰士和射手,有兒孫一百五十八人。以上全是本雅明的子孫。
Ana a Ulamu anali asilikali olimba mtima amene amadziwa kugwiritsa ntchito uta. Iwo anali ndi ana ndi adzukulu ambiri ndipo onse analipo 150. Onsewa anali adzukulu a Benjamini.