< Sam 116 >
1 Kathutkung: Panuekhoeh BAWIPA teh ka lungpataw. Bangkongtetpawiteh, ka lawk hoi ka kâhei e hah na thai pouh.
Ndimakonda Yehova pakuti Iyeyo amamva mawu anga; Iye amamva kulira kwanga kopempha chifundo.
2 Kai koe lah a hnâ a pakeng dawkvah, ka hringyung thung ka kaw han.
Pakuti ananditchera khutu, ndidzayitana Iye masiku onse a moyo wanga.
3 Due patawnae ni na kalup, sheol patawnae ni na kuet, kângairu lungmathoe hoi ka o. (Sheol )
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol )
4 Hat toteh, Oe BAWIPA, pahren lahoi ka hringnae hah na rungngang haw telah BAWIPA min teh ka palaw.
Pamenepo ndinayitana dzina la Yehova: “Inu Yehova, pulumutseni!”
5 BAWIPA teh lungmakung hoi lannae lah ao. Bokheiyah, maimae Cathut teh lungmanae hoi akawi.
Yehova ndi wokoma mtima ndi wolungama Mulungu wathu ndi wodzaza ndi chifundo.
6 BAWIPA ni tami kamawngramenaw hah a khetyawt. Kai teh ka kârahnoum navah, ama ni na rungngang.
Yehova amateteza munthu wodzichepetsa mtima; pamene ndinali ndi chosowa chachikulu, Iye anandipulumutsa.
7 Oe, ka hringnae na lungmawngnae koe ban leih. Bangkongtetpawiteh, BAWIPA ni nang lathueng vah hnokahawi a sak toe.
Pumula iwe moyo wanga, pakuti Yehova wakuchitira zokoma.
8 Bangkongtetpawiteh, ka hringnae heh duenae koehoi na rungngang teh, ka mit heh mitphi bonae koehoi, ka khok heh tâlawnae koehoi na rungngang toe.
Pakuti Inu Yehova mwapulumutsa moyo wanga ku imfa, maso anga ku misozi, mapazi anga kuti angapunthwe,
9 BAWIPA hmalah kahringnaw onae hmuen koe ka kâhlai han.
kuti ine ndiyende pamaso pa Yehova mʼdziko la anthu amoyo.
10 Kai teh ka yuem dawkvah, lawk ka dei, puenghoi na rektap awh.
Ine ndinakhulupirira; choncho ndinati, “Ndasautsidwa kwambiri.”
11 Tami pueng laithoe a dei awh telah koe ka dei payon.
Ndipo ndili mʼnkhawa yanga ndinati, “Anthu onse ndi abodza.”
12 Kai lathueng vah, BAWIPA ni hnokahawi a sak e naw dawkvah, bangmouh ahni hanlah hawinae ka sak van han vai.
Ndingamubwezere chiyani Yehova, chifukwa cha zokoma zake zonse zimene wandichitira?
13 Rungngangnae manang hah ka la vaiteh, BAWIPA min teh ka kaw han.
Ndidzakweza chikho cha chipulumutso ndipo ndidzayitana dzina la Yehova.
14 Ka lawkkam e teh BAWIPA hmalah ka kuep sak han. A taminaw pueng e hmalah ka kuep sak han.
Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse.
15 A tami kathoungnaw due e teh, BAWIPA hmalah a phuopoung.
Imfa ya anthu oyera mtima ndi yamtengowapatali pamaso pa Yehova.
16 Oe BAWIPA, na san lah ka o. Na sannaw e capa lah ka o. Kai dawk e kateknae teh na rathap pouh toe.
Inu Yehova, zoonadi ndine mtumiki wanu: ndine mtumiki wanu, mwana wa mdzakazi wanu; Inu mwamasula maunyolo anga.
17 Lunghawilawkdeinae nalaihoi, BAWIPA min teh ka kaw han.
Ndidzapereka nsembe yachiyamiko kwa Inu ndipo ndidzayitanira pa dzina la Yehova.
18 Atuvah, ka lawkkam e hah BAWIPA hoi a taminaw e hmalah ka kuep sak han.
Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse,
19 Oe Jerusalem, na kho lungui BAWIPA e im thongma dawk roeroe ka kuep sak han. Hallelujah.
mʼmabwalo a nyumba ya Yehova, mʼkati mwako iwe Yerusalemu. Tamandani Yehova.