< Jawhan 15 >
1 Kai teh misurkung katang doeh. A Pa teh takha katawnkung doeh.
“Ine ndine mpesa weniweni, ndipo Atate anga ndiye mwini munda.
2 Kai dawk a paw ka paw hoeh e a kang pueng teh bouk lah ao han. A paw ka paw e a kangnaw teh hoe a paw nahan rasoun lah o awh han.
Iye amadula nthambi iliyonse ya mwa Ine imene sibala chipatso, koma nthambi iliyonse imene imabala chipatso amayisadzira bwino kuti ibale zipatso zambiri.
3 Nangmouh teh kai ni ka dei e lawk ni na thoungsak awh toe.
Inu ndinu oyera kale chifukwa cha mawu amene ndayankhula inu.
4 Kai dawk awm awh. Kai hai nangmouh dawk ka o han. A kang ni misurkung hoi kâkuen hoehpawiteh a mahmawk a paw paw thai hoeh e patetlah nangmouh hai kai dawk na awm hoehpawiteh a paw na paw thai awh mahoeh.
Khalani mwa Ine, monga Ine ndili mwa inu. Palibe nthambi imene ingabereke chipatso pa yokha ngati sinalumikizike ku mpesa. Chomwechonso inu simungathe kubereka chipatso pokhapokha mutakhala mwa Ine.
5 Kai teh misurkung doeh. Nangmouh teh akang doeh. Kai dawk kaawm e teh kai hai ahni koe ka o van han. Ahni teh moi a paw han. Kai hoi na kâkuen hoehpawiteh banghai na sak thai awh mahoeh.
“Ine ndine mpesa; inu ndinu nthambi zake. Ngati munthu akhala mwa Ine ndi Ine mwa iye, adzabereka zipatso zambiri; popanda Ine simungathe kuchita kanthu.
6 Kai dawk kaawm hoeh e teh ka ke e a kang patetlah alawilah tâkhawng han. Hot patetlah e a kangnaw teh taminaw ni a pâkhueng vaiteh hmai dawk koung phum vaiteh a kak han.
Ngati wina aliyense sakhala mwa Ine, iyeyo ali ngati nthambi imene yatayidwa ndi kufota. Nthambi zotero zimatoledwa, kuponyedwa pa moto ndi kupsa.
7 Nangmouh ni kai dawk na o awh teh kaie ka lawk hai nangmouh dawk awm pawiteh nangmouh ni na hei e naw pueng hai poe lah ao han.
Ngati inu mukhala mwa Ine ndipo mawu anga akhala mwa inu, pemphani chilichonse chimene mukufuna ndipo mudzapatsidwa.
8 Nangmouh ni a paw moikapap na paw pawi doeh, a Pa e a bawilennae a kamnue vaiteh nangmouh hai kaie hnukkâbang katang lah na o awh han.
Atate anga amalemekezedwa mukamabereka zipatso zochuluka, ndipo potero mudzionetsa kuti ndinu ophunzira anga.
9 Pa ni kai lung na pataw e patetlah kai ni nangmouh lung na pataw awh. Kaie lungpatawnae thungvah awm awh.
“Monga momwe Atate amandikondera Ine, Inenso ndakukondani. Tsopano khalani mʼchikondi changa.
10 Kai ni a Pa e kâpoelawknaw ka ngâi teh a Pa ni lung na pataw e patetlah, nangmouh ni kâpoelawknaw na ngâi awh pawiteh kaie lungpatawnae dawk na o awh han.
Ngati mumvera malamulo anga, mudzakhala mʼchikondi changa, monga Ine ndimamvera malamulo a Atate anga, ndipo ndimakhala mʼchikondi chawo.
11 Nangmouh lunghawinae ao vaiteh nangmae lunghawinae akuep nahanelah hete lawk heh nangmouh koe ka dei.
Ine ndakuwuzani izi kuti chimwemwe changa chikhale mwa Inu, kuti chimwemwe chanu chikhale chokwanira.
12 Kaie kâpoelawk teh kai ni nangmouh lungpataw e patetlah nangmouh ni buet touh hoi buet touh lungkâpataw awh.
Lamulo langa ndi ili: ‘Kondanani wina ndi mnzake monga Ine ndakonda inu.’
13 Tami ni a hui hanelah a hringnae a pasoung e hloilah ka talue e api koehai lungpatawnae alouke awm hoeh.
Palibe munthu ali ndi chikondi choposa ichi, choti munthu nʼkutaya moyo wake chifukwa cha abwenzi ake.
14 Nangmouh ni kaie kâ poe e na tarawi pawiteh ka hui lah na o awh.
Inu ndinu abwenzi anga ngati muchita zimene Ine ndikulamulani.
15 Atu totouh hoi san telah na kaw a mahoeh toe. San ni teh a bawipa ni a sak e hno panuek hoeh. Nangmouh teh huiko lah na o awh. Bangkongtetpawiteh a Pa ni a dei e hnonaw pueng teh nangmouh koe na panue sak.
Ine sindikutchulaninso antchito, chifukwa wantchito sadziwa zimene bwana wake akuchita. Mʼmalo mwake Ine ndakutchani abwenzi pakuti zilizonse zimene ndinaphunzira kwa Atate, Ine ndakudziwitsani.
16 Nangmouh ni kai na rawi awh hoeh. Kai ni doeh nangmouh na rawi awh. Hatdawkvah, cet awh nateh ka kangning e a paw na paw awh nahane hoi ka min lahoi Pa koe na hei awh e pueng na hmu awh nahanelah nangmanaw teh kai ni na rawi awh.
Inu simunandisankhe Ine, koma Ine ndinakusankhani kuti mupite ndi kukabereka zipatso, zipatso zake za nthawi yayitali. Choncho Atate adzakupatsani chilichonse chimene mudzapempha mʼdzina langa.
17 Nangmouh ni buet touh hoi buet touh lungpatawnae tawn awh telah kâ na poe.
Lamulo langa ndi ili: ‘Muzikondana.’
18 Talaivan taminaw ni na hmuhma awh pawiteh, nangmouh na hmuhma awh hoehnahlan vah kai hmaloe na hmuhma awh toe tie panuek awh.
“Ngati dziko lapansi lidana nanu, dziwani kuti linayamba kudana ndi Ine.
19 Nangmouh ni talaivan taminaw patetlah na awm awh pawiteh, talaivan taminaw ni na lungpataw awh van han. Nangmouh teh talaivan taminaw thung hoi rawi e lah na o teh talai taminaw patetlah na o awh hoeh dawkvah talai taminaw ni na hmawt ngai awh hoeh.
Inu mukanakhala anthu a dziko lapansi, dziko lapansi likanakukondani ngati anthu ake omwe. Koma mmene zilili, inu si anthu a dziko lapansi. Ine ndakusankhani kuchokera mʼdziko lapansi, nʼchifukwa chake dziko lapansi limakudani.
20 San teh a bawi hlak len hoeh ka tie hah thai panuek awh. Taminaw ni kai na dudam awh pawiteh nangmouh hai na dudam awh han. Ka lawk ngâi awh pawiteh na lawk hai a ngâi awh han.
Kumbukirani mawu amene ndinayankhula nanu akuti, ‘Palibe wantchito amene amaposa bwana wake.’ Ngati anandizunza Ine, iwo adzakuzunzaninso inu. Ngati anamvera chiphunzitso changa, iwo adzamvera chanunso.
21 Ahnimouh ni kai na kapatounkung a panue awh hoeh dawkvah kaie ka min kecu dawk hote hno pueng a sak awh han.
Iwo adzakuchitani zimenezi chifukwa cha dzina langa, popeza sakudziwa amene anandituma Ine.
22 Kai ni ka tho teh ahnimouh hanlah ka dei hoehpawiteh ahnimae yonnae awm hoeh. Hatei, atuvah a yonae hro thai lah awm hoeh toe.
Ine ndikanapanda kubwera ndi kuyankhula nawo, sakanakhala ndi mlandu. Koma tsopano alibe choti nʼkukanira mlandu wawo.
23 Kai na ka hmuhma e teh a Pa hai a hmuhma
Iye amene amadana ndi Ine amadananso Atate anga.
24 Apinihai a sak boihoeh e hnonaw hah, ahnimae hma lah ka sak pouh hoehpawiteh a yonae awm hoeh. Hatei, atuvah hote hno a hmu awh nahlangva vah kai hoi a Pa hah na hmuhma awh.
Ine ndikanapanda kuchita pakati pawo zinthu zimene wina aliyense sanachitepo, iwo sakanakhala ochimwa. Koma tsopano aona zodabwitsa izi, komabe akundida Ine pamodzi ndi Atate anga.
25 Ahnimae kâlawk cauk dawk thut e teh, kai hah ayawmyin lah na hmuhma awh ti e a kuep nahane doeh.
Koma zatere kuti zikwaniritse zimene zinalembedwa mʼmalamulo awo: ‘Iwo anandida Ine popanda chifukwa.’
26 Apa koehoi kai ni nangmouh koe ka patoun hane lawkkatang hoi kakawi e Muitha a tho toteh kaie ka kong hah a kampangkhai han.
“Nkhoswe ikadzabwera imene Ine ndidzakutumizireni kuchokera kwa Atate, ndiye Mzimu Woyera wachoonadi amene achokera kwa Atate, Iyeyo adzandichitira umboni Ine.
27 Nangmouh hai apuengcue hoi kai hoi cungtalah o awh dawkvah kai heh na kampangkhai han.
Inunso mudzandichitira umboni Ine, popeza mwakhala nane kuchokera pachiyambi.”