< Job 22 >

1 Teman tami Eliphaz ni a pathung teh,
Pamenepo Elifazi wa ku Temani anayankha kuti,
2 Tami teh Cathut hanelah a cungkeinae a tawn thai han namaw, A lungkaang e hai ama hanelah doeh cungkeinae ao.
“Kodi munthu nʼkukhala waphindu kwa Mulungu? Kodi munthu wanzeru angamupindulire Iye?
3 Tamikalan lah na onae hah, Athakasaipounge, a lungkahawi sak e lah ao han namaw Toun han awm laipalah na sak e na lamthung hah ahni hanelah a meknae ao han namaw
Kodi Wamphamvuzonse akanapeza chabwino chotani iweyo ukanakhala wolungama? Kodi iyeyo akanapeza phindu lanji makhalidwe ako akanakhala angwiro?
4 Ama na taki kecu dawk maw na toun teh, lawkcengnae dawk na kâenkhai.
“Kodi nʼchifukwa choti umamuopa, kuti azikudzudzula, kuti azifuna kukukokera ku mlandu?
5 Na hawihoehnae hah a len poung teh, pout laipalah na payonnae kecu dawk nahoehmaw.
Kodi osati nʼchifukwa chakuti kuyipa kwako nʼkwakukulu? Kodi machimo ako si opanda malire?
6 A khuekhaw awm laipalah na hmaunawngha e hno hah na man pouh teh, caici lah kaawm e hnicu hah na la pouh.
Iwe unkawumiriza abale ako kuti akupatse chikole popanda chifukwa; umalanda anthu zovala zawo ndi kuwasiya amaliseche.
7 Tha ka tawn e koe, nei hane tui hah na poe hoeh teh, von kahlamnaw hanelah vaiyei hah na pasoung pouh hoeh.
Sunawapatse madzi anthu otopa, ndipo unawamana chakudya anthu anjala,
8 Hateiteh, tami athakaawme ni ram a coe teh, a thung vah bari kaawm e tami ni kho a sak awh.
ngakhale unali munthu wamphamvu, wokhala ndi malo akeake, munthu waulemu wake, wokhala mʼdzikomo.
9 Lahmainu hah kut caici lah na ceisak awh teh, manu ka tawn hoeh e naranaw e kut hah na khoe pouh awh.
Ndipo akazi amasiye unawachotsa wopanda kanthu, ndipo unapondereza ana amasiye.
10 Hatdawkvah na tengpam e karap ni na kalup teh, puennae ni rucatnae na poe awh.
Nʼchifukwa chake misampha yakuzungulira, nʼchifukwa chake tsoka ladzidzidzi lakuchititsa mantha,
11 Na hmu thai hoeh nahanelah, hmonae hoi tuikalen poung ni muen a khu awh.
nʼchifukwa chake kuli mdima kuti sungathe kuona kanthu, nʼchifukwa chakenso madzi achigumula akumiza.
12 Kalvan arasang nah koe, Cathut awm hoeh namaw Karasangpoung e âsinaw hah khenhaw! banghloimaw arasang.
“Kodi Mulungu sali kutalitali kumwamba? Ndipo ona nyenyezi zili mmwamba kwambirizo, ona kutalika kwake pamene zililipo!
13 Nang ni, Cathut ni bangmaw a panue, Hmonae hloilah lawk a ceng thai maw.
Komabe iweyo ukunena kuti, ‘Kodi Mulungu amadziwa chiyani? Kodi Iye amaweruza mu mdima woterewu?
14 A hmu thai hoeh nahanelah, katha poung e tâmai ni a ramuk teh, kalvan lathueng lah a kâhlai, telah na ti.
Mitambo yakuda yamuphimba, kotero kuti Iye sakutiona pamene akuyendayenda pamwamba pa thambopo.’
15 Tamikathoutnaw ni karawk e lam karuem dawk meng na cei han namaw
Kodi iwe udzayendabe mʼnjira yakale imene anthu oyipa ankayendamo?
16 Apimaw atueng kuep hoehnahlan vah la e lah kaawm niteh, apini a ung e maw tuikalen ni a la.
Iwo anachotsedwa nthawi yawo isanakwane, maziko awo anakokoloka ndi madzi achigumula.
17 Cathut koe, na cettakhai yawkaw, Athakasaipounge ni ahnimouh hanelah bangmaw a sak thai telah ati awh.
Anthuwo anati kwa Mulungu, ‘Tichokereni! Kodi Wamphamvuzonse angatichitire chiyani?’
18 Hateiteh a imnaw hah hnokahawi hoi akawi sak. Hateiteh tamikathout e khokhangnae teh, kai koehoi kahlatpoung lah ao.
Chonsecho ndi Iye amene anadzaza nyumba zawo ndi zinthu zabwino, choncho ine sindigwirizana ndi uphungu wa anthu oyipa.
19 Tamikalan ni a hmu teh, a lunghawi. Yonnae ka tawn hoeh e ni dudamkungnaw hah a panuikhai awh.
“Anthu olungama amaona kuwonongeka kwawo ndipo amakondwera; anthu osalakwa amangoseka, akamuona woyipa akulangidwa.
20 Ka tarannaw teh, raphoe katang lah ao teh, kacawie naw hah hmai ni a kak han.
Amanena kuti, ‘Ndithudi adani athu awonongeka ndipo moto wawononga chuma chawo!’
21 Ama koe kâpanuek sak nateh, karoumcalah awm, haw hoi nang hanelah hnokahawi a tâco han.
“Gonjera Mulungu kuti ukhale naye pamtendere; ukatero udzaona zabwino.
22 Pahren lahoi amae kâko hoi ka tâcawt e hringnae na cangkhai e hah dâw haw. Na lungthin thungvah amae lawk hah kahawicalah kuem.
Landira malangizo a pakamwa pake ndipo usunge mawu ake mu mtima mwako.
23 Athakasaipounge, koevah na ban pawiteh, kangdout thai e lah o han. Na payonpakai e hah na im dawk hoi kahlatpoung lah na takhoe han.
Ukabwerera kwa Wamphamvuzonse udzabwezeretsedwa; ukachotsa zoyipa zonse zimene zimachitika mʼnyumba mwako,
24 Nange sui teh, vaiphu dawk na ta han. Ophir sui hah sawkca thung e, sadinaw patetlah na pâtung han.
ndipo chuma chamtengowapatali nuchiona ngati fumbi, golide wa ku Ofiri numutaya ku miyala ya ku zigwa.
25 Athakasaipounge teh, nange sui hoi aphu kaawm e ngun lah ao han.
Pamenepo Wamphamvuzonseyo adzakhala golide wako, siliva wako wamtengowapatali.
26 Hottelah Athakasaipounge dawkvah na lunghawi han. Cathut koe lah na khet han toe.
Pamenepo udzakondwera naye Wamphamvuzonse ndipo udzakweza nkhope yako kwa Mulungu.
27 Ama koe na ratoum vaiteh, na thai pouh han. Na lawkkam hah na kuep sak han.
Udzamupempha ndipo adzakumvera, ndipo udzapereka zimene unalonjeza.
28 Hno buet touh na kâcai vaiteh, nama hanelah caksak lah ao han. Hot patetvanlah na lamthung dawk angnae ni a tue han.
Chimene watsimikiza kuti uchite, chidzachitikadi, kuwala kudzakuwunikira pa njira yako.
29 Na tâkhawng navah tawmrasang e lah na o han telah na ti han. Hottelah kârahnoum e hah ama ni a rungngang han.
Pamene anthu agwetsedwa pansi, iwe nʼkunena kuti, ‘Akwezeni!’ Pamenepo Iye adzapulumutsa anthu oponderezedwa.
30 Ka yon hoeh e hah a rungngang han. Na kut thoungnae hoi rungngang lah ao han, telah a ti.
Iye adzapulumutsa ngakhale munthu amene ndi wolakwa, ameneyo adzapulumutsidwa kudzera mʼkulungama kwako.”

< Job 22 >