< Hebru 9 >

1 Hmaloe e lawkkamnae dawk hai bawknae phungnaw hoi talai van kaawm e kathounge hmuen ao.
Pangano loyamba lija linali ndi malamulo okhudza chipembedzo, ndi malo opembedzeramo omangidwa ndi anthu.
2 Bangkongtetpawiteh, lukkareiim a sak awh navah, kathounge hmuen tie ahmaloe e rakhan dawkvah, hmaiimkhok, caboi hoi vaiyeinaw a ta awh.
Anthu ankamanga chihema. Mʼchipinda choyamba munali choyikapo nyale, tebulo ndi buledi woperekedwa kwa Mulungu. Chipinda chimenechi chinkatchedwa Malo Opatulika.
3 Apâhni e yaphni athunglah teh hmuen kathoung poung telah kaw e rakhan ao.
Kuseri kwa chinsalu chotchinga chachiwiri kunkatchedwa Malo Opatulika kwambiri.
4 Hote lukkareiim dawkvah, sui tongben hoi sui hoi sak e lawkkam thingkong ao. Hote thingkong dawk mana tanae sui hlaam, a pei ka pei e Aron e sonron, hoi kâlawk thutnae lungphennaw ao.
Mʼmenemo munali guwa lansembe lagolide lofukizirapo lubani. Munalinso Bokosi la Chipangano lokutidwa ndi golide. Mʼbokosimo munali mʼphika wagolide mʼmene ankasungiramo mana ndi ndodo ya Aaroni imene inaphuka ija, ndiponso miyala ya pangano.
5 Hote thingkong van vah, ka lentoe e cherubim ni yonthanae hmuen hah a ramuk. Hote hnonaw teh atu ka kamceng lah dei thai lah awmhoeh.
Pamwamba pa bokosilo panali zifanizo za angelo otchedwa akerubi aulemerero, ataphimba chivundikiro cha bokosilo chimene chinali malo okhululukirapo machimo. Koma nʼzosatheka tsopano kufotokoza zinthu mwatsatanetsatane.
6 Hottelah, hnonaw pueng koung rakueng awh torei teh, vaihmanaw teh lukkareiim apasuek e rakhan thungvah bawknae thawnaw tawk hanlah atu hoi atu a kâen awh.
Zinthu zonsezi zitakonzedwa, ansembe ankalowamo mʼchipinda choyamba chija nthawi ndi nthawi kumatumikiramo.
7 Apâhni e rakhan dawk teh vaihma kacue ni dueng doeh kum touh dawk vai touh ouk a kâen. Hottelah a kâen navah ama han hoi taminaw ni yon a sak payonnae hanlah thoseh, thueng nahanlah thi hoi ouk a kâen.
Koma Mkulu wa ansembe yekha ndiye ankalowa chipinda chachiwiri chija kamodzi kokha pa chaka. Iye sankalowamo wopanda magazi. Magaziwo ankapereka nsembe kwa Mulungu chifukwa cha iye mwini ndiponso chifukwa cha machimo a anthu amene ankachita mosazindikira.
8 Lukkareiim apasueke rakhan ao roukrak, kathoungpounge rakhan koe kâen thainae lam aw hoeh rah tie hah Kathoung Muitha ni hete hno hoi a pâpho.
Mwa njira imeneyi Mzimu Woyera ankaonetsa kuti njira yolowera ku malo opatulika inali isanaonetsedwe pamene Chihema choyamba chinali chilipo.
9 Hote teh, atutueng hanelah bangnuenae lah a o. Thuengnae poehnonaw hoi thueng e satheinaw ni mahoima kâpanuenae lung thoungsak thai hoeh.
Zimenezi nʼzofanizira chabe, ndipo zinkalozera nthawi ino, kusonyeza kuti mphatso ndi nsembe zimene zinkaperekedwa sizinkachotsa chikumbumtima cha wopembedzayo.
10 Hote hnonaw teh canei kawi hoi kâpasunae phungnaw hoi a kâkuet teh, a katha lah bout sak hoehnahlan totouh takthai hoi kâkuen e phunglam lah doeh ao.
Inali nkhani ya zakudya, ya zakumwa ndi ya miyambo yosiyanasiyana ya masambidwe. Anali malamulo akunja kokha mpaka pa nthawi imene anakonzanso zonse mwatsopano.
11 Hatei, Khrih teh hno kahawinaw hoi kâkuen e Vaihma Kacue lahoi a tho toung dawkvah, tami kut hoi sak e nahoeh, het talai van e nahoeh, hoe ka lentoe niteh hoe kakuep e lukkareiim dawkvah,
Koma Khristu atafika monga Mkulu wa ansembe wa zinthu zokoma zimene zilipo tsopano, Iye analowa mʼChihema chachikulu ndiponso changwiro chimene sichinamangidwe ndi munthu, ndiye kuti sichili pansi pano.
12 Hmae hoi Maitoca e thipaling tho laipalah amae thi roeroe a sin teh kathoungpounge hmuen koe a kâen teh maimouh han lah a yungyoe ratangnae vaitahoi kakhoutlah a sak toe. (aiōnios g166)
Iye sanalowemo ndi magazi ambuzi yayimuna, ana angʼombe amphongo, koma analowa Malo Opatulika kamodzi kokha ndi magazi ake, atatikonzera chipulumutso chosatha. (aiōnios g166)
13 Bangkongtetpawiteh, kathounghoehe taminaw van vah kahei e maito thi, hmae thi hoi Maitola sawi e hraba ni ahnimae takthai dawk thoungsak thai boipawiteh,
Ngati magazi ambuzi yayimuna, angʼombe yayimuna ndi phulusa la mwana wangʼombe wamkazi zimati zikawazidwa pa odetsedwa zimawayeretsa kotero kuti amakhala oyeretsedwa ku thupi,
14 a yungyoe Muitha lahoi yah yonnae ka tawn hoeh e amahoima Cathut koe ka kâthueng e Khrih e a thipaling teh kahring Cathut thaw tawk thai nahanelah, nangmae thoehawi panuenae lungthin duenae tawksaknae thung hoi hoe thoungsak thai mahoeh namaw. (aiōnios g166)
nʼkoposa kotani magazi a Khristu, amene mwa Mzimu wamuyaya anadzipereka yekha kwa Mulungu kukhala nsembe yopanda chilema. Iye adzayeretsa chikumbumtima chathu pochotsa ntchito za imfa, kuti ife titumikire Mulungu wamoyo. (aiōnios g166)
15 Hatdawkvah, hmaloe e lawkkam rahim yonnae dawk hoi hlout sak hanlah, Khrih teh a due toung dawkvah, a kaw e naw ni yungyoe râw hah a coe thai awh nahanlah Bawipa teh lawkkam katha e laicei lah ao. (aiōnios g166)
Pa chifukwa chimenechi Khristu ndi mʼkhalapakati wa pangano latsopano, kuti iwo amene anayitanidwa alandire chuma chamuyaya, pakuti Iye tsopano anafa ngati dipo lomasula iwo ku machimo amene anachita ali pansi pa pangano loyamba lija. (aiōnios g166)
16 Râw coenae lawk teh râw coenae lawk kadeikung a due hnukkhu to doeh ouk a coe awh.
Ngati munthu alemba pangano losiyira ena chuma, pafunika kutsimikiza kuti wolemba panganolo wamwaliradi,
17 Bangkongtetpawiteh lawk kadeikung a hring nathung teh cungkei hoeh, a due hnukkhu torei doeh to e lah ao.
chifukwa pangano lotere limakhala ndi mphamvu ngati wolembayo wamwalira. Siligwira ntchito pamene wolembayo ali ndi moyo.
18 Hatdawkvah, hmaloe e lawkkamnae haiyah thipaling laipalah sak hoeh.
Nʼchifukwa chake pangano loyamba lija silinachitike popanda kukhetsa magazi.
19 Mosi ni kâlawk cauk dawk kaawm e kâlawknaw pueng hah rangpuinaw koe a pathang pouh hnukkhu, tui hoi kalawt e maito hoi hmae thi hah a sin teh tumuen paling hoi dingsala dawn hoi kâlawk cauk hoi rangpuinaw hah a kahei sin.
Mose atawawuza anthu onse malamulo, anatenga magazi a ana angʼombe amphongo ndi ambuzi yayimuna pamodzi ndi madzi, ubweya wofiira ndiponso chitsamba chotchedwa hisope, ndi kuwaza pa buku ndi anthu onse.
20 Hete thi teh, Cathut ni nangmouh koe kâ a poe e lawkkamnae thipaling doeh a ti.
Iye anati, “Awa ndi magazi a pangano limene Mulungu wakulamulirani kuti mulisunge.”
21 Hathnukkhu hot patetvanlah, lukkareiim hoi bawknae koe hno e hnopainaw lathueng hai thipaling a kahei sin.
Momwemonso Mose anawaza magazi pa Chihema chija ndiponso pa zipangizo zonse zogwiritsa ntchito pa chipembedzo.
22 Kâlawk patetlah bangpuengpa heh thipaling hoi thoungsak thai lah ao. Thi palawng laipalah yon ngaithoumnae awmhoeh.
Monga mwa malamulo titha kunena kuti, pafupifupi zinthu zonse zimayeretsedwa ndi magazi ndipo popanda kukhetsa magazi palibe kukhululukidwa machimo.
23 Kalvanlae hnonaw e tâhlipnaw hah hottelah thuengnae lahoi thoungsak lah ao teh, kalvan lae hnonaw hateh hoe ka talue e thuengnae lahoi thoungsak lah ao.
Tsono panafunika kuti zinthu zingofanizira zenizeni za kumwamba, ziyeretsedwe ndi nsembe zimenezi, koma zinthu za kumwamba zenizenizo kuti ziyeretsedwe panafunika nsembe zina zoposa zimenezo.
24 Bangkongtetpawiteh, Khrih teh a katang e hmuen kathoungpounge tâhlip lah kaawm e tami ni kut hoi sak e kathoungpounge hmuen dawk kâen hoeh, maimouh han kecu dawk atu Cathut e a hmalah amahoima kâpâtue hanlah kalvan vah a kâen toe.
Pakuti Khristu sanalowe mʼmalo opatulika omangidwa ndi anthu amene anali chifaniziro cha malo enieniwo. Iye analowa kumwamba kwenikweniko kuti azionekera pamaso pa Mulungu chifukwa cha ife.
25 Vaihma kacue ni sathei thi sin laihoi kum tangkuem kathoungpounge hmuen koe a kâen e patetlah Khrih teh a mahoima atuhoitu thueng hanelah panki hoeh.
Iye sanalowe kumwamba kuti azikadziperekanso nsembe kachiwiri monga momwe mkulu wa ansembe ankachitira chaka ndi chaka ku Malo Opatulika kwambiri ndi magazi amene sanali ake.
26 Hottelah hoehpawiteh, talaivan a paw pasuek hoi avai moikapap a khang han doeh toe. Atuteh a tue abawnae koe lah a mahoima vai touh thuengnae lahoi yon thoungsak hanlah a tho toe. (aiōn g165)
Zikanatero bwenzi Khristu atamva zowawa kambirimbiri chilengedwere cha dziko lapansi. Koma tsopano anaoneka kamodzi kokha chifukwa cha onse pa nthawi yotsiriza kuti achotse tchimo podzipereka yekha nsembe. (aiōn g165)
27 Tami teh vai touh due hnukkhu lawkcengnae a kâhmo e patetlah,
Popeza kunayikika kwa munthu kufa kamodzi ndipo kenaka kuweruzidwa,
28 Khrih ni taminaw e yonnaw ceikhai hanelah, amahoima vai touh dueng thuengnae a sak teh, apâhni e dawk teh yon hoi kâkuen laipalah, rungngangnae kangaihawinaw han lah apâhni bout a kum han.
momwemonso Khristu anadzipereka nsembe kamodzi kokha kuchotsa machimo a anthu ambiri. Ndipo Iye adzaonekanso kachiwiri, osati kudzachotsa tchimo, koma kudzapereka chipulumutso kwa amene akumudikira.

< Hebru 9 >