< Tâconae 36 >

1 Bezalel hoi Oholiab tinaw ni kutsakkathoumnaw pueng BAWIPA ni kâ a poe e patetlah, hmuen kathoung dawk thaw a tawk thai awh nahanelah, thaw phunkuep a tawk thai awh nahanelah lungangnae hoi thaipanueknae a poe e naw pueng ni lengkaleng tawk hane doeh, telah ati.
Choncho Bezaleli, Oholiabu pamodzi ndi anthu aluso onse amene Yehova anawapatsa luso ndi nzeru zodziwira kupanga zofunika zonse zomangira malo opatulika, adzapanga zonse iwowo, monga momwe Yehova analamulira.”
2 Mosi ni Bezalel hoi Oholiab tinaw kutsakkathoume, BAWIPA ni ahnimae lungthin dawk lungangnae a poe teh a thaw tawk hanelah a lungthin dawk lungthonae a poe e naw pueng hah a kaw.
Ndipo Mose anayitana Bezaleli ndi Oholiabu ndiponso munthu aliyense waluso amene Yehova anamupatsa luso ndiponso amene anali ndi mtima wofuna kugwira ntchito.
3 Isarel catounnaw ni hmuen kathoung thawtawknae koe a tâcokhai awh e pueng hah Mosi koehoi a coe awh. Hahoi amom tangkuem ngainae lahoi poe e hah ahni koe pou a poe awh.
Iwo analandira kuchokera kwa Mose zopereka zonse Aisraeli anabweretsa kuti agwirire ntchito yomanga malo wopatulika. Ndipo anthu anapitirira kupereka zopereka zaufulu mmawa uliwonse.
4 Kutsakkathoumnaw pueng, hmuen kathoung thaw katawknaw pueng ni thaw a tawk awh lahun e hah lengkaleng a ceitakhai awh teh,
Kotero amisiri onse amene amagwira ntchito yonse ya malo wopatulika anasiya ntchitoyo
5 Mosi koevah, BAWIPA ni tawk han kâ a poe e thaw tawk hanelah taminaw ni acawilah hno a sin awh, telah a pathang awh.
ndipo anati kwa Mose, “Anthu akubweretsa kuposa zimene zikufunika kugwirira ntchito imene Yehova analamulira kuti ichitike.”
6 Mosi ni kâ a poe teh, hmuen kathoung hanelah poehno hah napui hai tongpa hai apihai poe hanelah kâcai awh nahanh lawiseh, telah roenae hmuen koe a oung sak. Hottelah taminaw ni a poe awh e hah pasoung hoeh toe.
Choncho Mose analamulira ndipo analengeza mu msasa onse, “Mwamuna kapena mayi aliyense asaperekenso chopereka chilichonse cha ku malo wopatulika.” Choncho anthu analetsedwa kubweretsa zambiri,
7 Bangkongtetpawiteh, a tawn awh tangcoung e hah panki e pueng sak nahanelah a khout toe. Atangcalah apap poung toe.
chifukwa zimene anali nazo zinali zoposera zimene zimafunika kugwirira ntchito yonse.
8 Ahnimouh thung dawk a lungkaangnaw pueng ni, lukkareiim teh yaphni hra touh hoi a sak awh. Hote yaphni teh Loukloukkaang e hoi carouk e kamthim, paling, âthi naw hoi kathoumnaw ni cherubim mei a sak awh e hah kamnuek lah sak e lah ao.
Anthu onse aluso pakati pa anthu ogwira ntchitoyo anapanga chihema pogwiritsa ntchito nsalu khumi zofewa, zosalala ndi zolukidwa bwino, zobiriwira, zapepo ndi zofiira. Ndipo anthu aluso anapeta pa nsaluzo Akerubi.
9 Yaphni teh dong 28 touh lengkaleng a saw teh, akaw e teh dong pali touh rip a pha. Yaphni pueng ayung adangka koung a kâvan.
Nsalu zonse zinali zofanana. Mulitali mwake zinali mamita khumi ndi atatu, mulifupi mamita awiri.
10 Yaphni panga touh a kâbet teh, alouke panga touh hai koung a kâbet.
Iwo analumikiza nsalu zisanu, kuti ikhale nsalu imodzi ndipo anachita chimodzimodzi ndi nsalu zisanu zinazo.
11 Patawp e yaphni rui a poutnae koe vah, laikaw kamthim lah sak e lah ao. Hot patetlah patawp e yaphni avanglae a poutnae koe haiyah sak e lah ao.
Kenaka anapanga zokolowekamo za nsalu yobiriwira mʼmphepete mwa nsalu imodzi yotsiriza ya mbali ina. Ndipo anachita chimodzimodzi ndi nsalu yotsiriza ya mbali inayo.
12 Yaphni buet touh dawk laikaw 50 touh a sak teh alouke patawp e dawk haiyah, laikaw 50 touh a sak. Hote laikawnaw teh minhmai kâhmo lah ao awh.
Iwo anasokerera zokolowekamo makumi asanu pa nsalu yoyamba ndi zokolowekamo makumi asanu zinanso pa nsalu inayo. Anapanga kuti zokolowekamozo ziziyangʼanana.
13 Hahoi sui hetnae 50 touh a sak teh, hetnae naw ni yaphni hah a hetsin. Hottelah lukkareiim teh rakhan buet touh lah a coung.
Kenaka anapanga ngowe zagolide 50 zolumikizira nsalu ziwirizo kotero kuti zinapanga chihema chimodzi.
14 Hahoi lukkareiim lemphu ramuknae lah, Hmae muen yaphni hah hlaibun touh a sak.
Iwo anapanga nsalu za ubweya wambuzi zophimba pamwamba pa chihemacho. Nsalu zonse pamodzi zinalipo khumi ndi imodzi.
15 Yaphni teh dong 30 touh saw sak lah ao teh, akaw e teh dong pali touh lengkaleng a pha. Yaphni hlaibun touh teh koung a kâvan.
Nsalu zonse khumi ndi imodzi zinali zofanana. Mulitali mwake munali mamita khumi ndi anayi ndipo mulifupi mwake munali mamita awiri.
16 Yaphni panga touh hah patawp e lah ao teh, yaphni taruk touh hai patawp e lah ao.
Iwo analumikiza nsalu zisanu kukhala nsalu imodzi ndipo nsalu zinazo zisanu ndi imodzi, analumikizanso kukhala nsalu imodzinso.
17 Patawp e yaphni buet touh a rai poutnae koe vah laikaw 50 touh a sak teh, yaphni patawp e avanglae arai dawk hai laikaw 50 touh a sak.
Kenaka anasokerera zokolowekamo makumi asanu mʼmphepete mwa nsalu imodzi yotsirizira ya nsalu yoyamba yolumikiza ija ndiponso anapanga zokolowekamo zina makumi asanu mʼmphepete mwa nsalu yotsirizira ya nsalu inanso yolumikiza ija.
18 Lukkareiim hah rakhan buet touh lah ao nahanelah, hetsin nahanelah hetsinnae 50 touh hah rahum hoi a sak.
Iwo anapanga ngowe 50 zamkuwa zolowetsa mu zokolowekazo ndipo anaphatikiza nsalu ziwirizo kuti tentiyo ikhale imodzi.
19 Hahoi tutan pho paling bu e hoi lukkareiim lemphu ramuknae hoi hot van ramuk nahanelah saram pho hoi a sak.
Ndipo anapanga chikopa cha nkhosa zazimuna cha utoto wofiira chophimbira tentiyo ndipo pamwamba pake anapanganso chophimbira china cha zikopa za akatumbu.
20 Lukkareiim tapang thung hanelah anri thing hoi a sak.
Iwo anapanga maferemu amatabwa amtengo wa mkesha oyimikira chihemacho.
21 Thingphek teh dong hra touh asaw teh, dong touh hoi tangawn akaw.
Feremu iliyonse inali yotalika mamita anayi ndipo mulifupi mwake munali masentimita 69.
22 Thingphek tangkuem dawk a khok kahni touh hoi a kâkuetsak. Hottelah lukkareiim tapang pueng teh a sak.
Thabwa lililonse linali ndi zolumikizira ziwiri. Iwo anapanga maferemu onse a chihemacho ndi matabwa otere.
23 Lukkareiim hanelah tapang thingphek hah a sak teh, akalae tapang hanelah thingphek 20 touh a sak.
Anapanga maferemu makumi awiri a mbali yakummwera kwa chihemacho,
24 Hote thingphek 20 touh a kangdue nahanelah ngun pacawp 40 touh a sak. Thingphek buet touh dawk a khok kahni touh pâhung nahanelah pacawp kahni touh rip a sak.
ndiponso anapanga matsinde 40 asiliva ndipo anawayika pansi pa maferemuwo. Pansi pa feremu iliyonse anayika matsinde awiri ogwiriziza zolumikizira ziwiri zija.
25 Lukkareiim atunglae hanlah thingphek 20 touh hoi
Iwo anapanganso maferemu makumi awiri a mbali yakumpoto ya chihemacho,
26 ngun pacawp 40, thingphek buet touh hanelah pacawp kahni touh rip a sak.
ndiponso matsinde makumi anayi asiliva, awiri pansi pa feremu iliyonse.
27 Lukkareiim kanîloumlah hane thingphek 6 touh a sak.
Anapanganso maferemu asanu ndi imodzi a kumbuyo kwa tenti, kumbali yakumadzulo,
28 Lukkareiim hnuk lae takin koe hanelah thingphek kahni touh hai a sak.
ndiponso maferemu awiri a pa ngodya yakumbuyo kwenikweni kwa tenti.
29 A rahim hoi a lathueng lae laikaw totouh a kâkuetsak. A takin roi koe hot patetlah a sak.
Pa ngodya ziwirizi panali maferemu awiri, kuyambira pansi mpaka pamwamba atalumikizidwa pa ngowe imodzi. Maferemu onse anali ofanana.
30 Thingphek taroe touh, pâhung nahane ngun pacawp 16 touh hoi ao. Thingphek buet touh pâhung nahanelah pacawp kahni touh rip ao.
Choncho panali maferemu asanu ndi atatu ndiponso matsinde 16 asiliva, awiri anali pansi pa feremu iliyonse.
31 Hahoi lukkareiim tapang pangkhek hanelah anri thing panga touh,
Iwo anapanganso mitanda ya matabwa amtengo wa mkesha. Mitanda isanu inali ya maferemu a mbali imodzi ya chihema,
32 lukkareiim avanglah hane panga touh a sak.
mitanda isanu inanso inali ya maferemu a mbali inayo ndipo mitanda ina isanu ya mbali yakumadzulo, kumapeto kwenikweni kwa chihema.
33 A lungui e tarennae hah avoivang lae takin koe rek a pâcue sak.
Anapanga mtanda wapakati omwe umachokera pa maferemu a mbali ina mpaka mbali inanso.
34 Thingpheknaw hah sui hoi a hluk. Tarennae hrawt nahanelah sui laikaw hai a sak teh, tarennae naw hah sui hoi a hluk.
Iwo anakuta maferemuwo ndi golide ndiponso anapanga mphete zagolide zogwiriziza mitandayo. Ndipo mitandayonso anayikuta ndi golide.
35 Yaphni hanelah kamthim, âthi, paling, loukloukkaang e hni hoi cherubim meikahawicalah a sak.
Anapanga nsalu yokhala ndi mtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira ndipo nsaluyo inali yolukidwa bwino, yofewa ndi yosalala. Ndipo anthu aluso anapetapo zithunzi za Akerubi.
36 Hot hanelah anri thing khom pali touh a sak teh sui tui hoi a hluk. Hahoi a bangnae naw teh sui hoi sak e doeh. Hotnaw pâhung nahanelah ngun pacawp pali touh a hlun.
Iwo anapanga nsanamira zinayi zamtengo wa mkesha zokutidwa ndi golide. Anapanganso ngowe zagolide za nsanamirazo ndi matsinde asiliva anayi.
37 Hahoi lukkareiim takhang koe yap hanelah, kamthim, âthi, paling, Loukloukkaang e hoi carouk e kathoumnaw ni kahawicalah carouk e hoi a sak.
Anapanga nsalu ya pa chipata cholowera mu chihema, yamtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira yomwe inali yofewa ndi yosalala, yopetedwa bwino ndi amisiri aluso.
38 Hotnaw yap nahanelah khom panga touh, bang nahane naw hoi a sak. Hote khom a som kacoumnaw hoi yapnae khomnaw teh, sui tui hoi hluk e lah ao. Hotnaw pâhung nahanelah pacawp e panga touh hateh rahum hoi sak e doeh.
Anapanga nsanamira zisanu ndi ngowe zake. Anakuta pamwamba pa nsanamirazo ndi zomangira zake ndi golide, ndipo anapanganso matsinde asanu amkuwa.

< Tâconae 36 >