< 1 Kawrin 15 >

1 Hmaunawnghanaw, nangmouh koe ka pâpho awh e kamthang kahawi, nangmouh ni na coe awh teh na kangduekhai awh e, bout panue sak hanelah na ngaikhai awh.
Tsono abale, ndikufuna ndikukumbutseni za Uthenga Wabwino umene ndinakulalikirani. Munawulandira ndipo munawukhulupirira kolimba.
2 Nangmouh koe ka pâpho e lawk heh, kacaklah na kuen awh pawiteh, hote kamthang kahawi lahoi nangmouh rungngang e lah na o awh.
Inu munapulumutsidwa ndi Uthenga Wabwinowu, ngati mwasunga mawu amene ndinakulalikirani. Kupanda kutero, mwangokhulupirira pachabe.
3 Kai kama ni ka coe e patetlah nangmouh koe ahmaloe na poe awh e teh Cakathoung ni a dei e patetlah Khrih teh maimouh yon kecu dawk a due toe.
Pakuti chimene ndinalandira ndinapereka kwa inu monga chofunika kuposa zonse, kuti Khristu anafera zoyipa zathu monga mwa Malemba,
4 Pakawp hnukkhu Cakathoung ni a dei e patetlah apâthum hnin bout a thaw toe.
kuti anayikidwa mʼmanda, kuti anaukitsidwa tsiku lachitatu monga mwa Malemba;
5 Cephas ni Bawipa a hmu hnukkhu, hlaikahni touh e naw ni hai a hmu awh.
ndipo kuti anaonekera kwa Petro, ndipo kenaka kwa Atumwi khumi ndi awiriwo.
6 Hathnukkhu, hmaunawngha cum panga touh hlai koe bout a kamphawng pouh. Ahnimouh thung dawk a tangawn teh atu sittouh a hring awh rah. A tangawn naw teh a i awh toe.
Pambuyo pake, Iye anaonekera kwa anthu oposa 500 mwa abale pa nthawi imodzi, ndipo ambiri mwa iwo akanali ndi moyo ngakhale kuti ena anagona tulo.
7 Hat hoi, Jem koe a kamnue.
Kenaka anaonekeranso kwa Yakobo, kenaka kwa atumwi onse.
8 Hathnukkhu gunceinaw pueng koe a kamphawng pouh. A hnuktengpoung thapa kuep laipalah ka khe e patetlah kaawm e kai koehai a kamnue van.
Potsiriza pa onse anaonekeranso kwa ine, monga mwana wobadwa nthawi isanakwane.
9 Kai heh, alouke gunceinaw thung dawk kathoengpounge lah ka o teh, Cathut e kawhmoun ka pacekpahlek dawk, guncei ti hanelah kamcu hoeh.
Pakuti ine ndine wamngʼono kwa atumwi ndipo sindiyenera nʼkomwe kutchedwa mtumwi chifukwa ndinazunza mpingo wa Mulungu.
10 Hatei Cathut e lungmanae lahoi, kai teh kai lah ka o. Ka coe e a lungmanae hai ayawmyin ka coe hoeh. Hatdawkvah, alouke gunceinaw pueng hlak kai hoe kâyawmnae ka tawn. Hatei kai nahoeh. Kai dawk kaawm e Cathut lungmanae hoi doeh.
Koma mwachisomo cha Mulungu, ndili mmene ndililimu, ndipo chisomo chake kwa ine sichinali chopanda ntchito. Ndinagwira ntchito kuposa ena onse a iwo. Choncho sindine koma chisomo cha Mulungu chimene chinali ndi ine.
11 Kai ni hai ahnimouh ni hai het doeh a pâpho awh. Het doeh ka yuem awh.
Tsono kaya ndi ineyo kapena iwowo, izi ndi zomwe timalalikira, ndipo izi ndi zimene munakhulupirira.
12 Khrih teh duenae koehoi bout a thaw toe tie ka pâpho toung pawiteh, bangtelamaw a tangawn ni duenae koehoi boutthawnae awmhoeh na ti awh vaw.
Koma ngati timalalikira kuti Khristu anaukitsidwa kwa akufa, zikutheka bwanji kuti ena mwa inu azinena kuti kulibe kuuka kwa akufa?
13 Duenae koehoi boutthawnae awmhoeh pawiteh, Khrih hai duenae koehoi thaw van mahoeh.
Ngati kulibe kuuka kwa akufa, ndiye kuti ngakhale Khristu sanaukenso.
14 Khrih teh duenae koehoi bout thaw hoehpawiteh, kaimouh ni ka pâpho e ahrawnghrang lah awm vaiteh, nangmouh ni na yuemnae hai ahrawnghrang han doeh.
Ndipo ngati Khristu sanaukitsidwe, ndiye kuti kulalikira kwathu nʼkopanda ntchito, ndipo chikhulupiriro chanu nʼchopandanso ntchito.
15 Hothloilah kaimouh teh Cathut e thaw dawk kamsoumhoeh e kapanuekkhaikung lah doeh kaawm awh tih. Cathut ni kadout tangcoungnaw bout thaw sak hoehpawiteh, Cathut ni a thaw sak hoeh e Khrih hah Cathut ni a thaw sak toe telah laithoe ka dei e lah doeh awm awh tih.
Kuwonjezera pamenepa, ndiye kuti ndife mboni zabodza pa za Mulungu, pakuti tikuchita umboni kuti Mulungu anaukitsa Khristu kwa akufa. Ngati nʼzoona kuti akufa saukitsidwa, ndiye kuti Mulungu sanaukitsenso Khristu.
16 Bangtelah tetpawiteh, kadoutnaw boutthawnae awmhoeh pawiteh, Cathut ni Khrih hai thaw sak mahoeh.
Pakuti ngati akufa saukitsidwa, ndiye kuti nayenso Khristu sanaukitsidwe.
17 Khrih duenae koehoi bout thaw hoehpawiteh, nangmae yuemnae teh banglahai tho hoeh. Yonnae a rahim doeh na o a rah.
Ndipo ngati Khristu sanaukitsidwe, chikhulupiriro chanu nʼchopanda ntchito; mukanali mu machimo anu.
18 Telah pawiteh Khrih thung kaip tangcoungnaw hai kahmakata awh toe.
Ndiye kuti nawonso amene agona tulo mwa Ambuye ndi otayika.
19 Atu hring nahane dueng, Khrih thung ngaihawinae tawn pawiteh, tami pueng hlak pahren ka tho poung la doeh o awh.
Ngati kukanakhala kuti tili ndi chiyembekezo mwa Khristu mʼmoyo uno wokha, tikanakhala omvetsa chisoni kuposa anthu ena onse.
20 Atuteh Khrih duenae koehoi a thaw katang toung dawk kaipnaw thung dawk aluepaw lah ao.
Koma nʼzoonadi kuti Khristu anaukitsidwa kwa kufa, chipatso choyamba cha onse ogona tulo.
21 Hatdawkvah duenae teh tami buet touh koehoi a tho, boutthawnae hai tami buet touh dawk hoi a tho van,
Pakuti monga imfa inadza kudzera mwa munthu, kuuka kwa akufa kwabweranso kudzera mwa munthu.
22 Tami pueng Adam dawk hoi duenae koe pha awh e patetlah tami pueng Khrih thung hoi bout hringnae koe pha awh han.
Pakuti monga mwa Adamu onse amafa, chomwechonso mwa Khristu onse adzakhala ndi amoyo.
23 Hatei a taminaw pueng amamae atueng a pha torei a thaw awh han. Khrih teh aluepaw doeh. Hathnukkhu Khrih a tho toteh a taminaw bout thaw awh han.
Koma aliyense adzauka pa nthawi yake. Khristu ndiye woyambirira, pambuyo pake, pamene Khristu adzabwera, iwo amene ali ake adzauka.
24 Hathnukkhu a poutnae teh a pha han. Hattoteh Khrih ni uknae pueng, kâtawnnae pueng, hoi bahu pueng apout sak vaiteh, Cathut uknaeram hah Na pa koe a poe han.
Pamenepo chimaliziro chidzafika, pamene Iye adzapereka ufumu kwa Mulungu Atate, atathetsa ufumu wonse, ulamuliro wonse ndi mphamvu zonse.
25 A tarannaw pueng a khok rahim a hruek hoehroukrak Khrih ni a uk han.
Pakuti Iye ayenera kulamulira mpaka Mulungu atayika pansi pa mapazi ake adani ake onse.
26 A hnuktengpoung e taran tie duenae teh poutnae koe ka phat han.
Mdani wotsiriza kuwonongedwa ndi imfa.
27 Hno cawngca tami Capa e khok rahim a hruek toe telah Cakathoung dawk thut lah ao. Hno cawngca a khok rahim a hruek ti navah, hnocawngca khok rahim kahruengkung ama teh bawk hoeh tie a kamceng.
Pakuti Mulungu “wayika zinthu zonse pansi pa mapazi ake.” Ponena kuti wayika “zinthu zonse pansi pa mapazi ake,” nʼchodziwikiratu kuti sakuphatikizapo ndi Mulungu yemwe, amene anayika zinthu zonse pansi pa Khristu.
28 Hetnaw be a sak hnukkhu Cathut teh a cawngca dawk a cawngca lah ao thai nahan, hnocawngca pueng hah tami Capa e khok rahim ka tat pouh kung e uknae rahim vah Capa ma roeroe hai ao han.
Pamene adzatsiriza kuchita zimenezi, Mwana weniweniyo adzakhala pansi pa ulamuliro wa Iye amene anayika zinthu zonse pansi pake, kuti Mulungu akhale zonse mu zonse.
29 Kadout tangcoungnaw boutthawnae khoeroe awmhoeh pawiteh, kadoutnaw e yueng lah baptisma ka coe naw bangtelamaw ti han toung. Kadoutnaw e yueng lah bangkongmaw baptisma a coe a vaw.
Tsono ngati kulibe kuuka kwa akufa, kodi iwo amene akubatizidwa chifukwa cha akufa, adzatani? Ngati akufa saukitsidwa nʼkomwe, bwanji nanga anthu akubatizidwa mʼmalo mwawo?
30 Maimouh hai bangkongmaw hnintangkuem runae kâhmo a vaw.
Ndipo kwa ife, tikuyikiranji moyo wathu pachiswe nthawi ndi nthawi?
31 Hmaunawnghanaw maimae Bawipa Khrih Jisuh thung nangmouh kecu ka coe e kâoupnae lahoi hnintangkuem ka due telah ka dei.
Abale, ndimafa tsiku ndi tsiku, ndikunenetsa zimenezi, mongotsimikizira monga ndimakunyadirani mwa Khristu Yesu Ambuye athu.
32 Kadoutnaw boutthawnae awm hoehpawiteh, Efisa kho tami pouknae sarang taki ka tho poung hoi kâtuknae hai kai hanlah bangmaw aphu kaawm. Cat awh sei, net awh sei, tangtho due a han toe.
Ngati ndinalimbana ndi zirombo za kuthengo ku Efeso pa zifukwa za umunthu chabe, ndapindulanji? Ngati akufa sadzaukitsidwa, “Tiyeni tidye ndi kumwa, pakuti mawa tifa.”
33 Alouklah pouk awh hanh. Tami kahawihoehnaw hoi kamyawngnae lahoi nuen kahawi a rawk thai.
Musasocheretsedwe, “Kukhala mʼmagulu oyipa kumawononga makhalidwe abwino.”
34 Lannae koe lah yongvak awh haw. Yonnae sak awh hanh. Taminaw tangawn teh Cathut panuek a hoeh. Hottelah ka ti nah nangmouh kaya nahanelah doeh ka dei.
Ganizani bwino monga kuyenerera, ndiye lekani kuchimwa; pakuti pali ena amene sadziwa Mulungu. Ndikunena izi kuti muchite manyazi.
35 Tami tangawn ni, bangtelamaw tami kadout tangcoung e bout a thaw han. Bangpatetlae tak hoi maw a thaw han telah na pacei thai.
Koma wina akhoza kufunsa kuti, “Kodi akufa amaukitsidwa motani? Adzauka ndi thupi la mtundu wanji?”
36 Na pathu maw. Na patûe e cati ni dout hoehpawiteh hring mahoeh.
Wopusa iwe! Chimene mudzala sichikhala ndi moyo pokhapokha chitayamba chafa.
37 Na patûe nah a kung na patûe hoeh. Catun nakunghai, cang nakunghai, a mu roeroe doeh na patûe awh.
Mukadzala, simudzala thupi limene lidzamere, koma mbewu chabe, mwina ya tirigu kapena ya china chake.
38 Cathut ni a ngainae patetlah a kung a paw sak. Cati pueng hai amamouh phun patetlah a kung a paw sak.
Koma Mulungu amayipatsa thupi monga Iye wafunira, ku mbewu ya mtundu uliwonse amapereka thupi lakelake.
39 Moi pueng koung kâvan hoeh. Tami moi alouk, moithangnaw e moi alouk, tanga moi alouk, tava moi alouk, alouklouk lah ao awh.
Mnofu siwofanana. Anthu ali ndi mnofu wa mtundu wina, nyama zili ndi wina, mbalame zili ndi wina, nsomba zili ndi winanso.
40 Kalvan tak ao teh talai tak hai ao. Hatei, kalvan tak e bawilennae phun louk, talai e bawilennae hai phun louk lah ao.
Palinso matupi akumwamba ndipo palinso matupi a dziko lapansi; koma ulemerero wa matupi akumwamba ndi wina, ndi wa matupi a dziko lapansi ndi winanso.
41 Kanî e bawilennae alouk, thapa e bawilennae alouk, âsi e bawilennae alouk, alouklouk lah doeh ao awh. Âsi buet touh rip e a bawilennae hai kâvan hoeh.
Dzuwa lili ndi ulemerero wake, ndipo pali ulemerero wina wa mwezi, palinso ulemerero winanso wa nyenyezi. Ulemerero wa nyenyezi ndi wosiyanasiyana.
42 Hot patetvanlah kadoutnaw e boutthawnae teh ao. Tak teh patûe navah ka pawk thai e lah ao. Thaw toteh ka pawk thai hoeh e lah bout a thaw han.
Zidzaterenso pamene akufa adzauka. Thupi loyikidwa mʼnthaka ngati mbewu limavunda, koma likadzauka lidzakhala losavunda.
43 Patûe navah bari awm hoeh. Bout thaw toteh a bawilen. Patûe navah tha a youn, bout thaw toteh bahu a o.
Limayikidwa mʼmanda mopanda ulemu, koma likadzaukitsidwa lidzakhala ndi ulemerero. Limayikidwa mʼmanda lili lofowoka, koma likadzaukitsidwa lidzakhala ndi mphamvu.
44 Pakawp navah talai tak lah a o, bout thaw toteh muitha tak lah ao. Talai tak alouk, muitha tak alouklah ao.
Limayikidwa mʼmanda thupi la mnofu chabe, koma likadzaukitsidwa lidzakhala lauzimu. Ngati pali thupi la mnofu, palinso thupi lauzimu.
45 Cakathoung ni, apasueke tami Adam teh kahring e lah ao. A hnukteng e Adam teh kahringsakkung Muitha doeh.
Kwalembedwa kuti, “Munthu woyamba Adamu anakhala wamoyo,” Adamu wotsiriza anakhala wopatsa moyo.
46 Muitha tak ahmaloe awmhoeh. Talai tak hmaloe ao. Hathnukkhu muitha tak ao.
Zauzimu sizinabwere koyambirira, koma zachilengedwe, pambuyo pake zauzimu.
47 Ahmaloe e tami teh vaiphu hoi sak e talai tami doeh. Apâhni e tami teh kalvan kho hoi ka tho e Bawipa doeh.
Munthu woyamba anali wa dziko lapansi, wochokera mʼnthaka koma munthu wachiwiri anali wochokera kumwamba.
48 Vaiphu hoi sak e tami teh hote vaiphu tami patetlah ao awh. Kalvanlae taminaw teh hote kalvanlae tami patetlah ao awh han.
Monga analili munthu wa dziko lapansi, momwemonso anthu onse amene ndi a dziko lapansi. Ndipo monga alili munthu wakumwamba, momwemonso anthu onse amene ndi akumwamba.
49 Maimouh teh vaiphu tami e meilam sin e patetlah kalvanlae meilam hai sin van awh han.
Ndipo monga momwe tinabadwa ofanana ndi munthu wa dziko lapansi uja, momwemonso tidzakhala ofanana ndi munthu wakumwamba.
50 Hmaunawnghanaw, thi hoi tak ni Cathut uknaeram coe thai mahoeh. Ka pawk thai e ni ka pawk thai hoeh e coe thai van mahoeh.
Ndikunenetsa, abale, kuti thupi ndi magazi sizingathe kulowa mu ufumu wa Mulungu, ndipo zimene zimavunda sizingathe kulowa kumene zinthu sizivunda.
51 Hrolawk na dei pouh han, maimouh pueng koung ip a mahoeh.
Tamverani, ndikuwuzeni chinsinsi. Tonse sitidzagona tulo, koma tonse tidzasandulika.
52 Hatei, a hnukteng e mongka ueng torei teh, tawkkadekca dawk maimouh pueng teh mitpalap vah koung kâthung awh han. Mongka ueng lawk thai toteh kadout tangcoungnaw ka pawk thai hoeh e lah a thaw awh han. Maimouh pueng hai koung kâthung awh han.
Zidzachitika mwadzidzidzi, mʼkamphindi kochepa, monga ngati kuphethira kwa diso, pa lipenga lotsiriza. Pakuti lipenga lidzalira, akufa adzaukitsidwa opanda chovunda, ndipo ife tidzasandulika.
53 Atu ka pawk thai e ni ka pawk thai hoeh e a khohna han. Kadout thai e ni kadout thai hoeh e a kâmahrawk han.
Pakuti chovunda chiyenera kuvala chosavunda, ndi thupi ili lakufa liyenera kuvala losafa.
54 Ka pawk thai e ni ka pawk thai hoeh e lah, kadout thai e ni kadout thai hoeh e a kâmahrawk toteh, duenae teh tânae ni a payawp toe telah Cakathoung ni a dei e a kuep han.
Pamene thupi lovundali likadzasanduka losavunda, ndipo thupi lotha kufali likadzasanduka losatha kufa, pamenepo zidzakwaniritsidwa zimene zinalembedwa zakuti, “Imfa yogonjetsedwa kwathunthu.”
55 Oe duenae nange sue teh nâ ne. Oe phuen, nange tânae teh nâne ao. (Hadēs g86)
“Iwe imfa, kupambana kwako kuli kuti? Iwe imfa, ululu wako uli kuti?” (Hadēs g86)
56 Duenae sue teh yon doeh. Yon thaonae teh kâlawk doeh.
Ululu wa imfa ndi tchimo, ndipo mphamvu ya tchimo ndi lamulo.
57 Maimae Bawipa Jisuh Khrih dawk hoi, maimouh tânae na ka poe kung, Cathut teh pholen awh.
Koma tiyamike Mulungu amene amatipambanitsa mwa Ambuye athu Yesu Khristu.
58 Hatdawkvah, ka pahren e hmaunawnghanaw, Cathut thaw na tawk awh e aphu a talue poung tie na panue awh dawkvah, na lungcak sak awh. Rawm laipalah Cathut e thaw dawk thapatho nateh panki awh.
Choncho, abale anga okondedwa imani njii. Musasunthike ndi chilichonse. Nthawi zonse mudzipereke kwathunthu ku ntchito ya Ambuye, chifukwa mukudziwa kuti ntchito zanu mwa Ambuye sizili zopanda phindu.

< 1 Kawrin 15 >