< Thempu Dan 2 >
1 Nangman lhosohga Pathen maichama napeh tengleh, hiche lhosohga changbong neldisel chu nalhen doh ding, hiche changbong chunga chu Olive thao nasunkhuma, Bego toh nachap khum ding ahi.
“‘Munthu wina aliyense akabwera ndi nsembe ya chakudya kwa Yehova, chopereka chake chizikhala ufa wosalala. Ufawo ausakanize ndi mafuta ndi lubani,
2 Hichu Aaron chapate, Thempu ho koma nahin choi ding, Thempu ho chun changbong thaotwi toh kihalsa chu, khut a sip-kham khat ahamdoh ding, Bego namthei toh kihalsa changbong ho chengse chu maicham phunga ahal diu ahi. Hichu Pakaiya dia thilpeh pha leh gimnamtui tah hiding ahi.
ndipo apite nawo kwa ansembe, ana a Aaroni. Atapeko modzazitsa dzanja ufa wosalala uja kuti ukhale wachikumbutso pamodzi ndi mafuta ndi lubani ndipo atenthe zonsezi pa guwa lansembe kuti zilandiridwe ndi Yehova mʼmalo mwa chopereka chonse. Iyi ndi nsembe yotentha pa moto ndiponso fungo lokomera Yehova.
3 Gasoh maicham amoh chengse chu Aaron leh achapate jouse na hoppeh ding, hiche maicham thilpeh hi Pakai adia thilpeh athengpen leh aman lupen hiding ahi.
Zotsala za nsembe ya chakudyazo ndi za Aaroni pamodzi ndi ana ake. Chimenechi ndi chigawo chopatulika kwambiri chifukwa chatapidwa pa chopereka chotentha pa moto cha Yehova.
4 Na lhosohga thilto changlhah chu lhummeiya kisang minsa ahileh changlhah chu thao thengsel'a kikeng hi ding, chol kiso lou hi ding ahi.
“‘Ukabweretsa nsembe ya chakudya chophika mu uvuni, ikhale ya buledi wa ufa wosalala wopanda yisiti koma wosakaniza ndi mafuta, kapena timitanda ta buledi topyapyala, topanda yisiti koma topaka mafuta.
5 Na lhosohga maicham chu khangbela naken min ahijong leh changbong lah’a anel pen hiding, chule Olive thao naloi ding, hijong chu chol jao lou hiding ahi.
Ngati nsembe yako yachakudya ndi yophika pa chitsulo chamoto, ikhale ya buledi wa ufa wosalala wopanda yisiti koma wosakaniza ndi mafuta.
6 Hiche chang bong hose chu, atum tum in homkhen inlang chuteng Olive thao toh nuhel in, hichu lhosohga maicham ahi.
Umuduledule bulediyo ndi kumupaka mafuta; imeneyo ndi nsembe yachakudya.
7 Nangman lhosohga maicham anbela nahon teng, hiche changbong chu anelpen leh Olive thao ahoi pen toh kihel hi ding ahi.
Ngati nsembe yako yachakudya ndi yophikidwa pa chiwaya, ikhale ya buledi wa ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta.
8 Ipi lhosohga maicham hijong leh, iti kisem hijong leh thempupa koma hinpuiyun amapa chun maichama akatdoh ding ahi.
Munthu azibwera ndi nsembe za chakudya zimene wapanga ndi zinthu zimenezi. Atachipereka kwa wansembe, iyeyu adzipita nacho ku guwa.
9 Thempupa chun lhosohga maicham akatdoh chu, maicham chunga agovam ding ahi.
Wansembeyo atengeko gawo lina la nsembeyo kukhala ufa wachikumbutso kuti ilandiridwe ndi Yehova mʼmalo mwa nsembe yonse ndipo ayitenthe pa moto monga nsembe yopsereza ya fungo lokomera Yehova.
10 Hiche lhosohga maicham amoh chengse chu Aaron le achapate kipe ding amahon anneh chohnaa anei diu, hiche maicham chu atheng pen, ahoipen leh lunglhaina dimset Pakaiya dia kikat doh hiding ahi.
Zotsala za nsembe ya chakudyayo zikhale za Aaroni ndi ana ake. Chimenechi ndi chigawo chopatulika kwambiri chifukwa chatapidwa pa chopereka chotentha pa moto cha Yehova.
11 Nanghon lhosohga maicham nabol teng uleh chol kisolou changlhah jeng hiding, Pathen henga na pehdoh jouseu chu khoiju leh chol jaona ho chu maicham phunga na halvam theilou hel diu ahi.
“‘Nsembe ya chakudya chilichonse imene ubweretsa kwa Yehova ikhale yopanda yisiti, pakuti suyenera kupereka kwa Yehova nsembe yotentha pa moto imene ili ndi yisiti kapena uchi.
12 Theichang gathah ho jouse jong, Pakai angsunga thilto dia nahin choi thei ahinai, hinlah hiche ho vang chu maicham phunga ki gouvam theilou hel ding ahi.
Ziwirizi ungathe kubwera nazo kwa Yehova ngati chopereka cha zokolola zoyambirira. Koma usazitenthe pa guwa kuti zikhale fungo lokomera Yehova.
13 Na lousohga maicham todoh ding jouse chu chi-al toh na haltha cheh ding ahi. Hichu Pathen tonsot'a dia na kiteppi nau na geldoh jing nau hiding ahi.
Zopereka zako zonse zachakudya uzithire mchere. Usayiwale kuthira mchere pa chopereka chako popeza mcherewo ukusonyeza pangano pakati pa iwe ndi Mulungu wako. Tsono uzinthira mchere pa chopereka chako chilichonse.
14 Na lousohga amasa pen maicham nasem tengleh, changvui lah a ahinhoi apumchep ho chu meiya na hulgot a, Pakaiya dia nahin todoh thei ahi.
“‘Mukamapereka kwa Yehova chopereka cha chakudya choyamba kucha, choperekacho chikhale cha chipatso chatsopano chokazinga pa moto ndi chopunthapuntha.
15 Na anchang ho chu Olive thao sunkhum inlang Bego namthei toh hal in.
Uchithire mafuta ndi lubani pakuti ndi chopereka cha chakudya.
16 Thempu pan lousohga phasah khat chu alah a Olive thao asunkhuma, Bego toh ahal ding, chu teng Pathen adia thilto loupi hi ding meiya ahal vam ding ahi.
Tsono wansembe atenthe gawo la chopereka chopunthapuntha chija kuti chikhala ufa wachikumbutso ndi cha mafuta pamodzi ndi lubani yense kuti Yehova alandire mʼmalo mwa zopereka zonse. Ichi ndi chopereka chotentha pa moto cha Yehova.