< Esther 10 >

1 Xerxes lengpa hin ama gamsung pumpi keo hilouva twikhanglen pang mun gamlatah a jong kai analah ahi.
Mfumu Ahasiwero anakhometsa msonkho mʼdziko lake lonse mpaka ku zilumba zonse.
2 Ama tohdoh thupitah tah hole, aman ana tunlet Mordecai nasatna hohi Media le Persia lengte thusimbu’a kijihlut’a ahi.
Ndipo ntchito zonse zochitika ndi mphamvu zake komanso ndi zonse zofotokoza za ukulu wa Mordekai, kukwezedwa kwake ndi mfumu, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a ku Mediya ndi Peresiya?
3 Judate mi Mordecai hi Xerxes lengpa bantah a thanei in apangin ahi. Amahi Judate te lah a mithupitah ahung hin chuleh jana sangtah anapeuvin ahi, ajehchu aman amite dingin thilpha anatong jingin chuleh khang nunungho changeija aphatna diuvin thu anaseijin ahi.
Pakuti Mordekai Myuda uja anali wachiwiri wa mfumu Ahasiwero. Kwa Ayuda onse Mordekai anali munthu wamkulu ndipo ankamukonda chifukwa ankachitira zabwino mtundu wake ndi kufunira mtendere abale ake.

< Esther 10 >