< Awicyih 4 >
1 Ka capakhqi aw, pa a cawngpyinaak ce ngai unawh, zaaksimthainaak na mi taaknaak ham ngai lah uh;
Ananu, mverani malangizo a abambo anu; tcherani khutu kuti mupeze nzeru zodziwira zinthu.
2 Nami venawh ak leek soeih cawngpyinaak ka ni pekkhqi; ka cawngpyinaak koeh mangtak uh.
Zimene ndikukuphunzitsani ndi zabwino. Choncho musasiye malangizo anga.
3 Ka pa capa na awm nyng, Ka nu a ca, capa a lungnak soeih na awm nyng.
Paja ndinalinso mwana mʼnyumba mwa abambo anga; mwana mmodzi yekha wapamtima pa amayi anga.
4 Ni cawngpyi nawh, ka venawh, “Nak kawlung ing kak awikhqi ve kym poe sei taw; kak awipekkhqi ce haana nawh hqing pyi,” ti hy.
Ndipo abambo anandiphunzitsa ndi mawu akuti, “Ugwiritse mawu anga pa mtima pako, usunge malamulo anga kuti ukhale ndi moyo.
5 Cyihnaak thlai nawh, zaaksimnaak awm thlai. Koeh hilh nawh, kam kha awhkawng ak cawn law awiyynnaakkhqi ce seetnaak lam benna koeh mang taak.
Upeze nzeru, upeze nzeru zomvetsa zinthu; usayiwale mawu anga kapena kutayana nawo.
6 Koeh hawi taak nawh, nik chungkhoep kaw; lung na nawh, ni khoemdoen kaw.
Usasiye nzeru ndipo idzakusunga. Uziyikonda ndipo idzakuteteza.
7 Cyihnaak veni a kungpyi soeih hy; cemyihna awmsaw cyihnaak ce thlai; na khawhkhamkhqi boeih ingawm cyihnaak ce thlai.
Fundo yayikulu pa za nzeru ndi iyi: upeze nzeru. Kaya pali china chilichonse chimene ungapeze, koma upeze nzeru yomvetsa bwino zinthu.
8 Zoeksang nawh, anih ing ni zoeksang lawt kaw; na ym na lam awhtaw kqihchah kawi thlangna ning coeng sak kaw.
Uyilemekeze nzeruyo ndipo idzakukweza; ikumbatire nzeruyo ndipo idzakupatsa ulemu.
9 Na luu-awh mikhaileek lumyk ning byng sak kawm saw, dawnaak boei lumyk ni pe kaw.
Idzayika sangamutu yokongola yamaluwa pamutu pako; idzakupatsa chipewa chaufumu chaulemu.”
10 Ka capa, kak awi ngai nawh kym lah; Cawhtaw na hqing kum pung khqoet khqoet kaw.
Mwana wanga, umvere ndi kuvomereza zimene ndikunena, ndipo zaka za moyo wako zidzakhala zochuluka.
11 Cyihnaak lamawh ni cawngpyi nyng, dyngnaak lamawh ni sawi nyng.
Ndakuphunzitsa njira yake ya nzeru. Ndakutsogolera mʼnjira zolungama.
12 Na ceh huiawh nak khawkan ing zaang nawh, nang dawngawh awm am tawngtawh kawp ti.
Pamene ukuyenda, mapazi ako sadzawombana; ukamadzathamanga, sudzapunthwa.
13 Cawngpyinaak awh ak cakna tu nawh, koeh hlah; ak cakna tu, na hqingnaak ham ni.
Ugwiritse zimene ndikukuphunzitsazi osazitaya ayi. Uwasamale bwino pakuti moyo wako wagona pamenepa.
14 Thlakchekhqi cehnaak awh koeh plaa nawh, thlakhalangkhqi a cehnaak awh koeh cet.
Usayende mʼnjira za anthu oyipa kapena kuyenda mʼnjira ya anthu ochimwa.
15 Qei nawh taw, a vena koeh cet; mangtaak nawh loen taak.
Pewa njira zawo, usayende mʼmenemo; uzilambalala nʼkumangopita.
16 Kut a mamik thlak khui taw am ip thai kawm usaw, thlang ak khanawh seetnaak a mi sai hlan khui taw mik am kuu kaw.
Pakuti iwo sagona mpaka atachita zoyipa; tulo salipeza mpaka atapunthwitsa munthu wina.
17 Seetnaak phaipi ce ai unawh, them amak leek sainaak misurtui ce aw uhy.
Paja chakudya chawo ndicho kuchita zoyipa basi ndipo chakumwa chawo ndi chiwawa.
18 Thlakdyngkhqi a cehnaak lam taw khawkbee ang lakawh bee khqoet hy.
Koma njira ya anthu olungama ili ngati kuwala kwa mʼbandakucha kumene kumanka kuwalirawalira mpaka dzuwa litafika pa mutu.
19 Thlakchekhqi a cehnaak lam taw khawmthan amyihna ikawh a ming tawh am sim uhy.
Koma njira ya anthu oyipa ili ngati mdima wandiweyani; iwo sadziwa chomwe chimawapunthwitsa.
20 Ka capa, kak awi ngai nawh, kak awipek awh nang haa dun lah.
Mwana wanga, mvetsetsa zimene ndikunena; tchera khutu ku mawu anga.
21 Namik huh awhkawng koeh thoeng; nak kawlung khuiawh khoem.
Usayiwale malangizo angawa, koma uwasunge mu mtima mwako.
22 Ak hukhqi ham hqingnaak na awm nawh, a mi pumsa ham sadingnaak na awm hy.
Pakuti amapatsa moyo kwa aliyense amene awapeza ndipo amachiritsa thupi lake lonse.
23 Ak chang boeih ang lakawh nak kawlung ce doen, hqingnaak ak cawnnaak ni.
Ndipotu mtima wako uziwuyangʼanira bwino ndithu pakuti ndiwo magwero a moyo.
24 Nam khaawh awihche koeh cawn sak nawh, thlang koeh thailat na.
Usiyiretu kuyankhula zokhotakhota; ndipo ulekeretu kuyankhula zinthu zonyansa.
25 Na mik ing hailam dan nawh, ak leekna na hai lam toek.
Maso ako ayangʼane patsogolo; uziyangʼana kutsogolo molunjika.
26 Na khaw ham lamtlak ce chei nawh, na lampyi boeih ce cak sak.
Uzilingalira bwino kumene kupita mapazi ako ndipo njira zako zonse zidzakhala zosakayikitsa.
27 Nak tang ben mai aw, nak cawng ben mai awi koeh pleng; seetnaak awhkawng na khaw ce thoeih.
Usapatukire kumanja kapena kumanzere; usapite kumene kuli zoyipa.