< Johan 8 >
1 Cehlai Jesu taw Olive tlang na ce kai hy.
Koma Yesu anapita ku phiri la Olivi.
2 A khawngawi khaw a dai awh bawkim lut hy. Cawh thlang boeih a venna cun law bai usaw, ngawi nawh cekkhqi ce cawngpyi khqi hy.
Mmamawa Iye anaonekeranso ku Nyumba ya Mulungu kumene anthu onse anamuzungulira ndipo Iye anakhala pansi nawaphunzitsa.
3 Cawh caqeekungkhqi ingkaw Farasikhqi ing nu pynoet a samphaih huiawh tu unawh law pyi uhy. Thlangkhqi haiawh nu ce dyih sak unawh,
Aphunzitsi amalamulo ndi Afarisi anabweretsa mkazi amene anagwidwa akuchita chigololo. Iwo anamuyimiritsa patsogolo pa anthu ndipo
4 Jesu a venawh, “Cawngpyikung, vawhkaw nu ve a samphaih huiawh tu unyng.
anati kwa Yesu, “Aphunzitsi, mkazi uyu tinamugwira akuchita chigololo.
5 Mosi a anaa awi ingtaw vemyih a nu ve lung ing thlak mat aham ni a awm hy. Nang ingtaw ikawmyihna nak poek?” tina uhy.
Mʼmalamulo a Mose anatilamulira kuti akazi otere tiwagende ndi miyala. Tsopano Inu mukuti chiyani?”
6 Ce awidoetnaak ve amah thawlh amik puknaak thai aham cainaak ta unawh a mi doet ni. Cehlai Jesu ing koep nawh a kut ply ing dek awh ca qee hy.
Iwo anagwiritsa ntchito funsoli ngati msampha, ndi cholinga choti apeze chifukwa cha kumuneneza Iye. Koma Yesu anawerama pansi ndi kuyamba kulemba pa dothi ndi chala chake.
7 Cekkhqi ing ami doet khing awh tho nawh a mingmih a venawh, “Nangmih ak khuiawh amak thawlh khawi qoe ing vawhkaw nu ve lung ing thlak ma seh,” tinak khqi hy.
Pamene iwo anapitirira kumufunsa, Iye anaweramuka ndipo anawawuza kuti, “Ngati wina wa inu alipo wopanda tchimo, ayambe iyeyo kumugenda ndi miyala mkaziyu.”
8 Cekcoengawh nung koep tlaih nawh dek awh ca qee tlaih bai hy.
Iye anaweramanso pansi ndi kulemba pa dothi.
9 Ce ak awi ce aming zaak awh a hqamca awhkawng kqan nawh pynoet coeng pynoet cen bet bet uhy, a huna taw Jesu ingkaw cawh ak dyi nu doeng ce taang hy nih.
Iwo atamva izi anayamba kuchoka mmodzimmodzi, akuluakulu poyamba, mpaka Yesu anatsala yekha ndi mkaziyo atayimirira pomwepo.
10 Jesu ing dyi nawh nu a venawh, “Nu, hana nu ami ceh boeih? U ingawm amni thawlh sak nawh nu?” tina hy.
Yesu anaweramuka ndipo anamufunsa iye kuti, “Akuluakulu aja ali kuti? Kodi palibe amene wakutsutsa?”
11 Nu ing, “Bawipa, u ingawm amni thawlh sak hy,” tina hy. Cawh Jesu ing, “Cawhtaw kai ingawm amni thawlh sak lawt nyng. Cet nawhtaw thawlhnaak koeh sai voel moe,” tina hy.
Iye anati, “Ambuye, palibe ndi mmodzi yemwe.” “Inenso sindikukutsutsa iwe. Pita kuyambira tsopano usakachimwenso.”
12 Thlangkhqi venawh Jesu ing awi kqawn pek tlaih hy, “Kai taw khawmdek vangnaak na awm nyng. U awm ka hu awh ak law taw ityk awh awm thannaak ak khuiawh am cet kaw, cehlai hqingnaak ce ta kaw,” tinak khqi hy.
Yesu atayankhulanso kwa anthu, anati, “Ine ndine kuwunika kwa dziko lapansi. Aliyense amene anditsata Ine sadzayenda mu mdima, koma adzakhala ndi kuwala kotsogolera anthu ku moyo.”
13 Farasikhqi ing, “Nang ing namah ingkaw namah ni dyihthing na na awm hy; nang dyihpyinaak ve am thym hy,” tina uhy.
Afarisi anamutsutsa Iye nati, “Iwe ukudzichitira umboni wa Iwe mwini, umboni wako siwoona.”
14 Jesu ing cekkhqi ak awi ce vemyihna hlat khqi hy, “Kamah ingkaw kamah dyih qu pyi nyng seiawm, kang dyih qu pyinaak ve thym hy; kai taw hana kawng ka law nawh hana ka ceh hly tice sim nyng; cehlai nangmih ingtaw ka lawnaak ingkaw ka cehnaak hly am sim uhy ti.
Yesu anayankha kuti, “Ngakhale Ine ndidzichitire umboni, umboni wangawu ndi woona, pakuti Ine ndikudziwa kumene ndinachokera ndi kumene ndikupita. Koma inu simukudziwa ndi pangʼono pomwe kumene ndinachokera kapena kumene ndikupita.
15 Nangmih ing thlanghqing pumsa ing awideng uhyk ti; cehlai kai ingtaw u awm awi am deng nyng.
Inu mumaweruza potsata maganizo a anthu chabe. Ine sindiweruza munthu wina aliyense.
16 Awideng bai nyng seiawm, kamah doengna am ka awm awh kak awi tlypnaak ve thym hy. Kai anik tyikung Pa ingqawi kai taw dyi haih nyng.
Koma Ine ndikati ndiweruze, ndimaweruza molondola, chifukwa Ine sindili ndekha koma ndili ndi Atate amene anandituma.
17 Na mimah a anaa awi awh thlang pakhih ing a sim pyi awhtaw cawhkaw a simpyinaak ce thym hy tina awm hy.
Mʼmalamulo anu munalembedwa kuti umboni wa anthu awiri ndi wovomerezeka.
18 Kai ing kamah ce dyih qu pyi nyng; kai anik tyikung ak chang simpyikung taw Pa ni,” tinak khqi hy.
Ine ndikudzichitira ndekha umboni; ndipo mboni inanso ndi Atate amene anandituma.”
19 Cawh cekkhqi ing doet uhy, “Na pa ce hana nu a awm?” tina uhy. Jesu ing, “Nangmih ing kai amni sim u tiksaw ka Pa awm am sim utyk ti. Kai mah nami ni sim mantaw, ka Pa awm sim hly hlai uhyk ti,” tinak khqi hy.
Kenaka iwo anamufunsa Iye kuti, “Kodi Atate anuwo ali kuti?” Yesu anayankha kuti, “Inu simundidziwa Ine. Atate anganso simuwadziwa. Mukanandidziwa Ine, mukanawadziwanso Atate anga.”
20 Bawkim awh tangka amik channaak bawm a venawh a cawngpyi khqi awh ve ak awi ve kqawn pek khqi hy. A tym a pha hlan dawngawh u ingawm am tu hy.
Iye anayankhula mawu awa pamene amaphunzitsa Nyumba ya Mulungu pafupi ndi malo amene amaponyapo zopereka. Komabe palibe amene anamugwira Iye, chifukwa nthawi yake inali isanakwane.
21 Jesu ing a mingmih a venawh awi kqawn pek khqi tlaih bai hy, “Kai taw cet hly hawh nyng, nangmih ing kai ce ni sui kawm uk ti, cehlai nami thawlhnaak awh ce thi kawm uk ti. Kai ka cehnaak awh nangmih am law thai kawm uk ti,” tinak khqi hy.
Kenakanso Yesu anawawuza kuti, “Ine ndikupita, ndipo mudzandifunafuna, koma mudzafa muli mʼmachimo anu. Kumene ndikupita, inu simungabwereko.”
22 Cedawngawh Judahkhqi ce doet qu uhy, “Amah ingkaw amah him qu vang tinawh hy voei aw? Cawh aw, ‘Kai ka cehnaak awh nangmih am law thai kawm uk ti,’ a ti hy voei?” ti uhy.
Izi zinachititsa Ayuda kufunsa kuti, “Kodi adzadzipha yekha? Kodi ndicho chifukwa chake akuti, ‘Kumene ndikupita, inu simungabwereko?’”
23 Cehlai anih ing, “Ningmih taw ak kai nakawng ni nami law hy, kai taw khan benna kawng law nyng. Nangmih taw ve khawmdek a koena awm uhyk ti; kai taw ve khawmdek a koe na am awm nyng.
Koma Iye anapitiriza kuti, “Inu ndi ochokera pansi pano. Ine ndine wochokera kumwamba. Inu ndinu anthu a dziko la pansi. Ine sindine wa dziko lapansi lino.
24 Nami thawhlhnaak awh nangmih taw thi kawm uk ti, tice nik kqawn pek khqi hawh nyng; kai ve anih hawh ni, tinawh kak khypyi ve am namik cangnaak awhtaw nami thawlhnaak awh ce thi tang tang kawm uk ti,” tinak khqi hy.
Ine ndinakuwuzani kuti mudzafera mʼmachimo anu ngati simukhulupirira kuti Ine Ndine. Ndithu inu mudzafera mʼmachimo anu.”
25 Cekkhqi ing, “Nang ve a u nu?” tina uhy. Jesu ing, “Nik kqawn pek khqi khing hawh nyng kaw.
Iwo anafunsa kuti, “Ndinu ndani?” Yesu anayankha kuti, “Monga Ine ndakhala ndikunena nthawi yonseyi,
26 Nangmih awi ka ni dengnaak khqi awh ve awi khawzah kqawn ham ta nyng. Cehlai kai anik tyikung taw ypawm hy, anih a ven awhkaw, kang zaak ce ni khawmdek a venawh kak kqawm,” tinak khqi hy.
ndili ndi zambiri zoti ndinene zoweruza inu. Koma Iye amene anandituma ndi woona, ndipo chimene Ine ndamva kuchokera kwa Iye, ndi chimene ndimaliwuza dziko lapansi.”
27 A Pa akawng ak kqawn peekkhqi ce a mingmih ing am zasim uhy.
Iwo sanazindikire kuti Iye amawawuza za Atate ake.
28 Cedawngawh Jesu ing, “Nangmih ing Thlanghqing Capa ce nami tai awh, kai ve anih hawh ni, tice sim kawm u tiksaw, kamah poek awh ik-oeih am sai nyng saw Pa ing ani cawngpyi amyihna ni awi kak kqawn, tice sim kawm uk ti.
Choncho Yesu anati, “Inu mukadzapachika Mwana wa Munthu, pamenepo mudzadziwa kuti Ine Ndine. Mudzadziwa kuti sindichita kalikonse pa Ine ndekha koma ndimayankhula zokhazo zimene Atate anandiphunzitsa.
29 Kai a nik tyikung ce kai ak khuiawh awm hy; kamah doeng amni cehta hy, anih ak kawngaih ce ni kai ing ka sai poepa,” tinak khqi hy.
Iye amene anandituma Ine ali nane pamodzi. Iye sanandisiye ndekha popeza nthawi zonse ndimachita zomwe zimamukondweretsa Iye.”
30 Ve ak awikhqi ak kqawn awh thlang khawzah ing ak khanawh cangnaak ta uhy.
Pamene Iye ankayankhula zimenezi, ambiri anamukhulupirira.
31 Amah ak cangnaak Judahkhqi venawh Jesu ing, “Ka cawngpyinaak ve namim tu awhtaw, nangmih taw kai a hubat tang tang na awm uhyk ti.
Kwa Ayuda amene anamukhulupirira, Yesu anati, “Ngati inu mutsatira chiphunzitso changa, ndithu ndinu ophunzira anga.
32 Cawhtaw awitak ce sim kawm uk ti, Awitak ing nangmih ce ni loet sak khqi kaw,” tinak khqi hy.
Tsono mudzadziwa choonadi, ndipo choonadicho chidzakumasulani.”
33 A mingmih ing, “Kaimih ve Abraham a cadil na awm unyng saw, u a tamnaa na awm am awm khawi unyng. Ikawmyihna nang ing loet kawm uk ti, na ti?” tina uhy.
Iwo anamuyankha Iye kuti, “Ife ndife zidzukulu za Abrahamu ndipo sitinakhalepo akapolo a wina aliyense. Kodi mukunena bwanji kuti, ‘Ife tidzamasulidwa?’”
34 Jesu ing, “Awitak ka nik kqawn peek khqi, u awm thawlhnaak ak sai taw thawlhnaak a tamnaa na awm hy.
Yesu anayankha kuti, “Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense wochita tchimo ndi kapolo wa tchimolo.
35 Tamnaa ing ipkhui awh am awm poe thai hy, cehlai capa taw ang qui na ipkhui awh awm hy. (aiōn )
Pajatu kapolo alibe malo wokhazikika mʼbanja, koma mwana ndi wa mʼbanjamo nthawi zonse. (aiōn )
36 Cedawngawh Capa ing nangmih ce ani loet sak khqi awhtaw, loet tang tang kawm uk ti.
Nʼchifukwa chake ngati Mwana adzakumasulani, mudzakhala mfulu ndithu.
37 Nangmih Abraham a cadil na awm uhyk ti tice sim nyng. Cehlai nangmih ak khuiawh kak awi ama awm dawngawh, nangmih ing kai ce him aham ni ngaih uhyk ti,” tinak khqi hy.
Ine ndikudziwa kuti inu ndinu zidzukulu za Abrahamu. Chonsecho inu mwakonzeka kundipha Ine, chifukwa mawu anga alibe malo mwa inu.
38 Kai ing ka Pa haiawh ka huh ce nangmih a venawh kqawn law nyng, nangmih ingawm nami pa a venawh kaw naming zaak ce ni nami sai lawt hy,” tinak khqi hy.
Ine ndikukuwuzani zimene ndaziona pamaso pa Atate, ndipo inu mukuchita zimene mwazimva kwa abambo anu.”
39 Cekkhqi ing, “Abraham taw kaimih a Pa ni,” tina uhy. Jesu ing, “Abraham a ca khqi na nami awm awhtaw, Abraham ing a sai ce nami sai aham awm hlai ti maw.
Iwo anayankha kuti, “Ife abambo athu ndi Abrahamu.” Yesu anati, “Inu mukanakhala ana a Abrahamu, bwenzi mukuchita zinthu zimene Abrahamuyo ankachita.
40 Kai ing Khawsa venawh kaw kang zaak awitak ce nangmih a venawh kqawn law hlai nyng, nangmih ingtaw kai ve him ahamni teng uhyk ti. Abraham ingtaw cemyih ik-oeih ce am sai hy.
Koma mmene zililimu, inu mwatsimikiza kundipha Ine, munthu amene ndinakuwuzani choonadi chimene Ine ndinachimva kuchokera kwa Mulungu. Abrahamu sanachite zinthu zoterezi.
41 Nangmih ingtaw nami pakhqi ing ami sai ceni nami sai hy,” tinak khqi hy. Cekkhqi ing, “Kaimih ve caquk caqaikhqi amni. Pynoet doeng kami taak cetaw Khawsa amah ni,” tina uhy.
Inu mukuchita zinthu zimene abambo anu amachita.” Iwo anatsutsa kuti, “Ife si ana amʼchigololo, Atate amene tili nawo ndi Mulungu yekha.”
42 Jesu ing a mingmih a venawh, “Khawsa ce nangmih a Pa na a awm mantaw, kai ve ni lungna hly hlai uhyk ti, kai taw Khawsa venna kawng law nyng saw tuh vawh awm nyng. Kai kamah poek awh am law nyng; anih ing ni ani tyih hy.
Yesu anawawuza kuti, “Mulungu akanakhala Atate anu, inu mukanandikonda Ine, pakuti Ine ndinachokera kwa Mulungu ndipo tsopano ndili pano. Ine sindinabwere mwa Ine ndekha.
43 Ikawtih kak awi ve nangmih a venawh ama caih hy voei? Kak kqawn ve am naming zaak thai dawngawh ni.
Nʼchifukwa chiyani simukumvetsetsa mawu anga? Chifukwa chake nʼchakuti simungathe kumva zoyankhula zanga.
44 Nangmih ve nami pa qaai ak thlangkhqi ni. Cedawngawh nami pa ak kawngaih ce sai aham ngaih uhyk ti. Anih ce ak cykca awhkawng thlang ak him na awm nawh amah awh awitak ce ama awm dawngawh awitak ce am tuhy. Qaai awi ak kqawn awh, amah ingkaw amah ni ak kqawn qu kqoeng hy, qaai awi ak kqawn thlang na awm nawh qaai awi ak kqawn thlangkhqi a pa na awm lawt hy.
Inu ndinu ana a mdierekezi. Iye ndiye abambo anu ndipo mukufuna kuchita zimene abambo anuwo amakhumba. Iye anali wakupha kuyambira pachiyambi, sanasunge choonadi, pakuti mwa iye mulibe choonadi. Pamene Iye anena bodza, amayankhula chiyankhulo chobadwa nacho, popeza ndi wabodza ndipo ndi bambo wa mabodza.
45 Cehlai awitak ka nik kqawn peek khqi dawngawh, nangmih ing amnik cangna uhyk ti!
Koma chifukwa ndikuwuzani choonadi, inu simukundikhulupirira Ine!
46 Nangmih ak khuiawh u ing nu kai a thawlhnaak am tu law thai? Awitak ka nik kqawn peek khqi taw, Ikawtih am nami nik cangnaak?
Ndani mwa inu angatsimikize kuti ndine wochimwa? Ngati Ine ndikunena choonadi, nʼchifukwa chiyani simukundikhulupirira?
47 U awm Khawsa ak thlang ingtaw Khawsa ak awi ce za hy. Khawsa koe na am nami awm dawngawh ni ak awi awm am naming zaak thai hy,” tinak khqi hy.
Munthu wochokera kwa Mulungu amamva zimene Mulungu amanena. Chifukwa chimene simumvera nʼchakuti, inuyo sindinu ochokera kwa Mulungu.”
48 Judahkhqi ing, “Nang ve Samari thlang qaai ak ta ni, ka mi tive thym hy my?” tina uhy.
Ayuda anamuyankha Iye kuti, “Kodi ife sitikulondola ponena kuti Inu ndi Msamariya ndi wogwidwa ndi chiwanda?”
49 Jesu ing, “Qaai am ta nyng, kai ing ka Pa ni ka zoeksang, cehlai nangmih ing amni zoeksang uhyk ti.
Yesu anati, “Ine sindinagwidwe ndi chiwanda, koma ndimalemekeza Atate anga, koma inu mukundinyoza.
50 Kamah a zoeksangnaak am sui nyng; ce ak sui thlang pynoet awm hy, anih cetaw awi ak dengkung na awm hy.
Ine sindidzifunira ndekha ulemu; koma alipo wina amene amandifunira, ndipo Iyeyo ndiye woweruza.
51 Awitak ka nik kqawn peek khqi, u ingawm kak awi ve a khoem awhtaw, ityk awh awm anih ce am thi voel kaw,” tina hy. (aiōn )
Ine ndikukuwuzani choonadi, munthu akasunga mawu anga, sadzafa konse.” (aiōn )
52 Cawh Judahkhqi ing, “Tuh qaai ta hyk ti tice ni sim hawh unyng! Abraham ce thi hawh hy, cemyih lawt na tawnghakhqi awm thi hawh uhy, cehlai nang ingtaw, 'U awm kai ak awi ak khoem taw thihnaak am tan kaw,' ti hyk ti. (aiōn )
Pamenepo Ayuda anafuwula kuti, “Tsopano ife tadziwadi kuti Inu ndi wogwidwa ndi chiwanda! Abrahamu anafa ndiponso aneneri, koma Inu mukunena kuti, ‘Ngati munthu asunga mawu anga, sadzafa.’ (aiōn )
53 Nang ve kaimih a Pa Abraham anglakawh na bau khqoet nawh nu? Anih ce thi hawh hy, cemyih lawt na tawnghakhqi awm thi hawh uhy. Namah ingkaw namah ve ikaw na nu nang ngaih qu?” tina uhy.
Kodi ndinu wa mkulu kuposa abambo athu Abrahamu? Iye anafa, ndiponso aneneri onse. Inu mukuganiza kuti ndinu yani?”
54 Jesu ing, “Kamah ingkaw kamah ka zoeksang qu awhtaw, ka zoeksang qunaak ve kawna awm am awm kaw. Ka pa, nangmih ing nami Khawsa na nami taak ce, anih ing ni kai ve ani zoeksang hy.
Yesu anayankha kuti, “Ngati Ine ndidzilemekeza ndekha, ulemu wangawo ndi wosatanthauza kanthu. Atate anga amene inu mukuti ndi Mulungu wanu, ndiye amene amandilemekeza Ine.
55 Nangmih ing anih ce am sim hlai uhyk ti, kai ingtaw sim nyng. Am sim nyng ka ti mantaw kai awm nangmih amyihna a qaai ak kqawn na awm nyng, cehlai anih ce kai ing sim nyng saw, ak awi ce khoem nyng.
Ngakhale kuti inuyo simukumudziwa, Ineyo ndikumudziwa. Ngati Ine nditanena kuti sindikumudziwa, Ineyo nditha kukhala wabodza ngati inuyo, koma Ine ndimamudziwa ndipo ndimasunga mawu ake.
56 Nangmih a pa Abraham ing kai a khawnghi ve huh aham anak poek nawh ana zeel hy; hu nawh ak kaw zeel hy,” tinak khqi hy.
Abambo anu Abrahamu anakondwera poyembekezera kubwera kwanga. Iwo anandiona ndipo anasangalala.”
57 Judahkhqi ing, “Kum hakip za na law hlanawh, Abraham hu nyng e!” tina uhy.
Ayuda anati kwa Iye, “Inu sumunafike nʼkomwe zaka makumi asanu, ndipo mukuti munamuona Abrahamu!”
58 Jesu ing, “Awitak ka nik kqawn peek khqi, Abraham a thang hlanawh kai awm hawh nyng,” tinak khqi hy.
Yesu anayankha kuti, “Ine ndikukuwuzani choonadi, Abrahamu asanabadwe, Ine Ndine!”
59 Cawh, a mingmih ing khawng aham lung cung uhy, cehlai Jesu ing thuk taak khqi hy, bawkim kawngma awhkawng cekkhqi ce ak changna cehtaak khqi hy.
Pamenepo iwo anatola miyala kuti amugende, koma Yesu anabisala, nachoka mozemba mʼNyumba ya Mulungu.