< Tingtoeng 98 >
1 Tingtoenglung BOEIPA te khobaerhambae a saii dongah laa thai neh hlai uh lah. A bantang kut neh a bantha cim te amah ham a khang coeng.
Salimo. Imbirani Yehova nyimbo yatsopano, pakuti Iyeyo wachita zinthu zodabwitsa; dzanja lake lamanja ndi mkono wake woyera zamuchitira chipulumutso.
2 BOEIPA loh amah kah khangnah te namtom kah mikhmuh ah a phoe tih a duengnah te a tueng sak.
Yehova waonetsa chipulumutso chake ndipo waulula chilungamo chake kwa anthu a mitundu ina.
3 Israel imkhui ham amah kah sitlohnah neh uepomnah te a thoelh pah dongah diklai khobawt loh mamih Pathen kah khangnah te boeih a hmuh uh.
Iye wakumbukira chikondi chake ndi kukhulupirika kwake pa Aisraeli; malekezero onse a dziko lapansi aona chipulumutso cha Mulungu wathu.
4 Diklai pum loh BOEIPA taengah yuhui uh lamtah tamhoe tingtoeng ol neh rhong uh lah.
Fuwulani mwachimwemwe kwa Yehova, dziko lonse lapansi, muyimbireni nyimbo mofuwula ndi mokondwera.
5 BOEIPA te rhotoeng neh, rhotoeng dongkah oldi ol nen khaw tingtoeng uh lah.
Imbirani Yehova nyimbo ndi zeze, ndi zeze ndi mawu a kuyimba,
6 BOEIPA Manghai mikhmuh ah olueng, tuki ol neh yuhui uh lah.
ndi malipenga ndi kuliza kwa nyanga ya nkhosa yayimuna fuwulani mwachimwemwe pamaso pa Yehova Mfumu.
7 Tuitunli neh a khuiah aka om boeih khaw, lunglai neh a khuikah khosa rhoek khaw pang uh lah.
Nyanja ikokome pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo, dziko lonse ndi onse amene amakhala mʼmenemo.
8 Tuiva rhoek loh kut tun paeng uh lamtah tlang boeih loh tamhoe uh saeh.
Mitsinje iwombe mʼmanja mwawo, mapiri ayimbe pamodzi mwachimwemwe;
9 BOEIPA mikhmuh ah diklai he laitloek thil ham halo dongah lunglai he duengnah neh, pilnam khaw vanatnah neh lai a tloek ni.
izo ziyimbe pamaso pa Yehova, pakuti Iye akubwera kudzaweruza dziko lapansi. Adzaweruza dziko lonse mwachilungamo, ndi mitundu ya anthu mosakondera.