< Tingtoeng 55 >

1 Rhotoeng neh aka mawt ham David kah hlohlai Aw Pathen, ka thangthuinah he hnatun lamtah ka lungmacil te rhael boeh.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Ndakatulo ya Davide. Pa zoyimbira za zingwe. Mvetserani pemphero langa, Inu Mulungu, musakufulatire kupempha kwanga,
2 Kai taengah hnatung lamtah kai n'doo dae. Ka kohuetnah neh ka van tih ka pang ka ngawl.
mverani ndipo mundiyankhe. Maganizo anga akundisautsa ndipo ndathedwa nzeru
3 Halang kah phaepnah hman ah thunkha kah ol loh kai sola boethae han sop uh tih thintoek neh kai taengah a konaeh uh.
chifukwa cha mawu a adani anga, chifukwa cha kupondereza kwa anthu oyipa; pakuti andidzetsera masautso ndipo akundizunza mu mkwiyo wawo.
4 Ka ko khuiah ka lungbuei loh phat tih dueknah mueirhih loh kai m'vuei khoep.
Mtima wanga ukupweteka mʼkati mwanga; mantha a imfa andigwera.
5 Kai taengah rhihnah neh thuennah halo tih, tuennah loh kai n'thing.
Mantha ndi kunjenjemera zandizinga; mantha aakulu andithetsa nzeru.
6 Te vaengah, “U long nim kai ham vahui bangla ka phae han khueh koinih ka ding vetih kho ka sak sue,” ka ti.
Ndinati, “Ndithu, ndikanakhala ndi mapiko ankhunda! Ndikanawulukira kutali ndi kukapuma.
7 Yaoe A hla la ka cet sui tih, khosoek ah ka rhaehba mai lah sue. (Selah)
Ndikanathawira kutali ndi kukakhala mʼchipululu.
8 Kai taengkah khohli khui lamloh, hlipuei a tloh khui lamloh kuepkolnah la ka tawn uh sue.
Ndikanathamangira kumalo anga a chitetezo; kutali ndi mphepo yaukali ndi yamkuntho.”
9 Ka Boeipa aw amih ol te haeh saeh lamtah dolh saeh, khopuei ah kuthlahnah neh tuituknah ni ka hmuh.
Sokonezani maganizo a oyipa, Inu Ambuye, tsutsani mawu awo; pakuti ine ndikuona chiwawa ndi mkangano mu mzinda.
10 Khoyin khothaih vongtung taengah vikvuek uh tih a ko khuiah boethae neh thakthaenah om.
Usana ndi usiku iwo akuzungulirazungulira pa makoma ake; nkhwidzi ndi kuzunza kuli mʼkati mwake.
11 Talnah loh a ko khuiah om tih, hnaephnapnah neh thailatnah loh toltung lamkah nong voelpawh.
Mphamvu zowononga zili pa ntchito mu mzinda; kuopseza ndi mabodza sizichoka mʼmisewu yake.
12 Kai aka veet he ka thunkha moenih, anih koinih ka phueih pawn ni. Kai taengah aka pomsang uh te ka lunguet moenih. Te koinih anih taeng lamloh ka thuh tak ni.
Akanakhala mdani akundinyoza, ine ndikanapirira; akanakhala mdani akudzikweza yekha kutsutsana nane, ndikanakabisala.
13 Tedae ka boeihlum neh ka thanat la ka hmaiben hlanghing khaw namah ni.
Koma iweyo mnzanga, mnzanga woyenda naye, bwenzi langa la pondaapanʼpondepo, ndi amene ukuchita zimenezi.
14 Baecenol neh tun ka tui uh tih, rhoihui neh Pathen im la ka cet uh coeng.
Mnzanga amene nthawi ina tinkasangalala pa chiyanjano chokoma ku nyumba ya Mulungu.
15 Amih ko khuiah khaw, a lampahnah ah khaw thae uh. Te dongah amih te dueknah loh dueknah neh phae saeh lamtah, a hingnah te saelkhui la suntla uh saeh. (Sheol h7585)
Mulole imfa itenge adani anga mwadzidzidzi; alowe mʼmanda ali amoyo pakuti choyipa chili pakati pawo. (Sheol h7585)
16 Pathen te kai loh ka khue tih BOEIPA loh kai n'khang.
Koma ine ndinafuwulira kwa Mulungu, ndipo Yehova anandipulumutsa.
17 Hlaem, mincang neh khothun ah ka lolmang tih ka ko vaengah ka ol han yaak.
Madzulo, mmawa ndi masana ndimalira mowawidwa mtima, ndipo Iye amamva mawu anga.
18 Kai taengkah aka om rhoek he a yet dongah ka hinglu he caemrhal lamkah sading la n'lat.
Iye amandiwombola ine osavulazidwa pa nkhondo imene yafika kulimbana nane, ngakhale kuti ndi ambiri amene akunditsutsa.
19 Hlamat lamkah kho aka sa Pathen loh a yaak vetih amih te a phaep ni. (Selah) Amih taengah thovaelnah a om pawt bangla Pathen khaw rhih uh pawh.
Mulungu amene ali pa mpando wake kwamuyaya, adzandimenyera nkhondo; adzawatsitsa adani anga, chifukwa safuna kusintha njira zawo zoyipa ndipo saopa Mulungu.
20 A ngaimongnah taengah a kut a hlah tih, a paipi a poeih.
Mnzanga woyenda naye wathira nkhondo abwenzi ake; iye akuphwanya pangano ake.
21 A ka te maehtha bangla hnal dae a lungbuei tah caemrhal la om. A olka te situi lakah yaai dae tumca a mukuh.
Mawu ake ndi osalala kuposa batala komabe nkhondo ili mu mtima mwake; mawu ake ndi osalala kwambiri kuposa mafuta, komatu mawuwo ndi malupanga osololoka.
22 Na thinrhih te BOEIPA taengah hal lamtah amah loh nang n'cangbam bitni. Aka dueng te kumhal ah bung sak mahpawh.
Tulani nkhawa zanu kwa Yehova ndipo Iye adzakulimbitsani; Iye sadzalola kuti wolungama agwe.
23 Tedae Pathen nang loh pocinah rhom khuila amih te na hlak ni. Hlang thii aka ngaih neh hlangthai palat kah khohnin te paekboe pah pawtnim? Kai long tah nang dongah ka pangtung ni.
Koma Inu Mulungu mudzawatsitsa anthu oyipa kulowa mʼdzenje lachiwonongeko; anthu okhetsa magazi ndi anthu achinyengo sadzakhala moyo theka la masiku awo, koma ine ndimadalira Inu.

< Tingtoeng 55 >