< Tingtoeng 103 >

1 David kah Aw ka hinglu, BOEIPA te uem lamtah, ka kotak boeih loh a ming cim te uem lah.
Salimo la Davide. Tamanda Yehova, iwe moyo wanga; ndi zonse zamʼkati mwanga zitamande dzina lake loyera.
2 Aw ka hinglu, BOEIPA te uem lamtah amah kah a thaphu paek boeih te hnilh boeh.
Tamanda Yehova, iwe moyo wanga, ndipo usayiwale zabwino zake zonse.
3 Nang kathaesainah boeih te khodawk han ngai tih, na tlohtat boeih aka hoeih sak,
Amene amakhululuka machimo ako onse ndi kuchiritsa nthenda zako zonse,
4 Na hingnah vaam khui lamkah aka tlan tih sitlohnah neh haidamnah te nang aka khuem sak loh,
amene awombola moyo wako ku dzenje ndi kukuveka chikondi ndi chifundo chake ngati chipewa chaufumu,
5 Na kamrhui te hnothen neh a kum sak tih na camoe tue te atha bangla a thahuel sak.
amene akwaniritsa zokhumba zako ndi zinthu zabwino, kotero kuti umakhala wamphamvu zatsopano ngati mphungu.
6 Hlang kah hnaemtaek aka yok rhoek boeih ham BOEIPA loh duengnah neh tiktamnah a saii pah.
Yehova amachita chilungamo ndipo amaweruza molungama onse opsinjika.
7 Moses taengah amah khosing, Israel ca rhoek taengah a khoboe te a tueng.
Iye anadziwitsa Mose njira zake, ntchito zake kwa Aisraeli.
8 Thinphoei neh lungvatnah BOEIPA loh thintoek a ueh tih sitlohnah neh baetawt.
Yehova ndi wachifundo ndi wokoma mtima, wosakwiya msanga ndi wachikondi chochuluka.
9 A yoeyah la ho pawt vetih, kumhal duela lunguen mahpawh.
Iye sadzatsutsa nthawi zonse, kapena kusunga mkwiyo wake kwamuyaya;
10 Mamih kah tholhnah bangla mamih taengah saii pawt tih mamih kathaesainah bangla mamih taengah han suk moenih.
satichitira molingana ndi machimo athu, kapena kutibwezera molingana ndi mphulupulu zathu.
11 Diklai soah vaan a sang bangla amah aka rhih rhoek ham a sitlohnah khaw len.
Pakuti monga kumwamba kuli kutali ndi dziko lapansi, koteronso chikondi chake nʼchachikulu kwa iwo amene amamuopa;
12 Khocuk lamkah khotlak a lakhla bangla mamih kah boekoeknah te mamih taeng lamkah a lakhla sak coeng.
monga kummawa kutalikirana ndi kumadzulo, koteronso Iye watichotsera mphulupulu zathu kuti zikhale kutali nafe.
13 A nap a loh camoe rhoek te a haidam bangla amah aka rhih rhoek te BOEIPA loh a haidam.
Monga bambo amachitira chifundo ana ake, choncho Yehova ali ndi chifundo ndi iwo amene amamuopa;
14 Amah loh mamih kah benbonah he a ming tih mamih he laipi ni tila a poek.
pakuti Iye amadziwa momwe tinawumbidwira, amakumbukira kuti ndife fumbi.
15 Hlanghing kah a tue sulrham bangla om tih khohmuen tamlaep bangla khooi van mai.
Kunena za munthu, masiku ake ali ngati udzu, amaphuka ngati duwa la mʼmunda;
16 Khohli loh anih a pah tih a hmata atah amah hmuen hmat voel pawh.
koma mphepo imawombapo ndipo silionekanso ndipo malo ake sakumbukirikanso.
17 Tedae BOEIPA kah sitlohnah tah amah aka rhih rhoek taengah khosuen lamkah kumhal duela om tih a duengnah a ca rhoek kah a ca rhoek patoeng taengah,
Koma kuchokera muyaya mpaka muyaya chikondi cha Yehova chili ndi iwo amene amamuopa, ndi chilungamo chake chili ndi ana a ana awo;
18 a paipi aka tuem tih a olrhi vai ham aka thoelh rhoek taengah om.
iwo amene amasunga pangano lake ndi kukumbukira kumvera malangizo ake.
19 BOEIPA loh vaan ah a ngolkhoel a hol tih a ram a cungkuem te a taemrhai.
Yehova wakhazikitsa mpando wake waufumu mmwamba ndipo ufumu wake umalamulira onse.
20 A olthui ol ngai ham amah kah olka bangla aka saii, thadueng puencawn, hlangrhalh rhoek loh BOEIPA te uem uh lah.
Tamandani Yehova, inu angelo ake, amphamvu inu amene mumachita zimene amalamula, amene mumamvera mawu ake.
21 Amah kah caempuei boeih loh BOEIPA te uem uh lamtah amah kah bibi boeih loh a kolonah te saii uh lah.
Tamandani Yehova, zolengedwa zonse zakumwamba, inu atumiki ake amene mumachita chifuniro chake.
22 A khohung hmuen boeih kah a kutngo boeih BOEIPA te uem uh lah. Aw ka hinglu, BOEIPA te uem lah.
Tamandani Yehova, ntchito yake yonse kulikonse mu ulamuliro wake. Tamanda Yehova, iwe moyo wanga.

< Tingtoeng 103 >