< Jeremiah 43 >

1 A taengah a tueih pah a BOEIPA Pathen kah ol cungkuem te pilnam pum taengah a thui. Te te Jeremiah loh a khah vaengah a BOEIPA Pathen loh amih ham a paek ol te cung.
Yeremiya atatsiriza kuwawuza anthuwo mawu onse a Yehova Mulungu wawo, amene Yehova anamutuma kuti akawawuze,
2 Te vaengah Hoshaiah capa Azariah neh Kareah capa Johanan neh thinlen hlang boeih loh Jeremiah te, “A honghi ni na thui, Egypt la caeh pawt ham neh bakuep pahoi pawt ham aka thui la mamih kah Pathen BOEIPA loh nang n'tueih moenih.
Azariya mwana wa Hosayia ndi Yohanani mwana wa Kareya pamodzi ndi anthu onse odzikuza anawuza Yeremiya kuti, “Ukunama iwe! Yehova Mulungu wathu sanakutume kuti unene kuti, ‘Musapite ku Igupto kukakhala kumeneko.’
3 Tedae kaimih he Khalden kut ah paek ham, kaimih duek sak ham neh kaimih he Babylon ah poelyoe ham ni kaimih voelah Neriah capa Barukh loh nang te m'vueh,” a ti nauh.
Koma ndi Baruki mwana wa Neriya amene akukulimbikitsa kuti utiletse zopita ku Igupto ndi kuti mʼmalo mwake tidzipereke mʼmanja mwa Ababuloni, kuti iwo atiphe kapena kutitenga ukapolo ku Babuloni.”
4 Judah khohmuen kah khosak ham dongah Kareah capa Johanan neh caem mangpa boeih neh pilnam pum loh BOEIPA ol te hnatun uh pawh.
Motero Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri onse a ankhondo pamodzi ndi anthu onse sanamvere lamulo la Yehova loti akhale mʼdziko la Yuda.
5 Kareah capa Johanan neh caem mangpa boeih loh, Judah khohmuen ah bakuep sak ham a heh nah namtom boeih lamloh aka mael Judah kah a meet te boeih a loh.
Mʼmalo mwake, Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri onse a ankhondo anatenga anthu onse otsala a ku Yuda amene anabwera kudzakhala mʼdziko la Yuda kuchokera ku mayiko onse kumene anabalakirako.
6 Tongpa, huta neh camoe, manghai canu rhoek neh Shaphan koca Ahikam capa Gedaliah neh imtawt boeiping Nebuzaradan loh a paih hinglu boeih khaw, tonghma Jeremiah neh Neriah capa Barukh te a khuen.
Mʼgulu la anthu otengedwalo munali amuna onse, akazi ndi ana, ana aakazi a mfumu, ndiponso anthu amene Nebuzaradani mtsogoleri wa asilikali olonda mfumu anawasiya kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu, mdzukulu wa Safani pamodzinso ndi mneneri Yeremiya ndi Baruki mwana wa Neriya.
7 Te dongah Egypt khohmuen te a pha uh dae BOEIPA ol te a hnatun uh pawt dongah Tahpanhes la pawk uh.
Kotero anthuwo analowa mʼdziko la Igupto chifukwa anakana kumvera Yehova, nakafika ku Tapanesi.
8 Tahpanhes ah Jeremiah taengla BOEIPA ol koep ha pawk tih,
Ndipo Yehova anayankhula ndi Yeremiya ku Tapanesi kuti,
9 “Na kut dongah lungto len lo lamtah Judah hlang rhoek kah mikhmuh ah Tahpanhes kah Pharaoh im thohka, taptlang laiting ah up.
“Tenga miyala inayi yayikulu ndipo uyikwirire mʼdothi pa chiwundo cha polowera ku nyumba yaufumu ya Farao ku Tapanesi. Uchite zimenezi Ayuda onse akuona.
10 Te phoeiah amih te thui pah. Israel Pathen caempuei BOEIPA loh he ni a thui. Ka sal Babylon manghai Nebukhanezar te ka tueih coeng dae ka loh pueng ni. He lungto ka up he anih kah ngolkhoel ka hol thil vetih a sokah amah po, amah po te a bueng thil ni.
Ndipo uwawuze kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti: Ndidzayitana mtumiki wanga Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni, ndipo adzakhazika mpando wake waufumu pa miyala imene ndayikwirira apayi. Iye adzafunyulula tenti yake yaufumu pa miyala imeneyi.
11 Egypt khohmuen la a pawk, a pawk vaengah dueknah ham tueng te dueknah neh, tamna ham tueng te tamna la, cunghang dongkah ham tueng te cunghang neh a ngawn ni.
Iye adzabwera kudzathira nkhondo Igupto. Iwo oyenera kufa ndi mliri adzafa ndi mliri, iwo oyenera kutengedwa ukapolo adzatengedwa ukapolo, ndipo iwo oyenera kufa ndi lupanga adzafa ndi lupanga.
12 Egypt pathen im te hmai ka hlup phoeiah a hoeh vetih amih te a sol ni. Boiva aka dawn loh a himbai neh a kulup bangla Egypt khohmuen neh kulup uh vetih te lamloh ngaimong la khoe uh ni.
Adzayatsa moto mʼnyumba zopembedzera milungu ya Igupto. Adzayeretsa dziko la Igupto monga momwe mʼbusa amayeretsera chovala chake pochotsamo nsabwe. Pambuyo pake adzachoka mʼdziko la Igupto mwa mtendere.
13 Egypt kho kah Bethshemesh kaam te a phaek pah vetih Egypt pathen im te hmai neh a hoeh ni,” a ti nah.
Ku Iguptoko adzagwetsa zipilala zachipembedzo za ku nyumba yopembedzera mulungu wa dzuwa. Adzatentha ndi moto nyumba za milungu ya ku Igupto.’”

< Jeremiah 43 >