< Isaiah 34 >
1 Namtom rhoek loh hnatun hamla ha mop lah. Namtu rhoek loh hnatung uh saeh lamtah diklai neh lunglai boeih neh a cadil cahma rhoek boeih loh yaa saeh.
Inu anthu a mitundu yonse, bwerani pafupi kuti mumve: tcherani khutu, inu anthu a mitundu ina yonse: Limvetsere dziko lapansi pamodzi ndi zonse zili mʼmenemo, dziko lonse pamodzi ndi zonse zochokera mʼmenemo!
2 BOEIPA kah a thinhul te namtom boeih taengah, a kosi te amih kah caempuei boeih taengla pawk. Amih te a thup vetih maeh la a voeih ni.
Yehova wayipidwa ndi anthu a mitundu yonse; wapsera mtima magulu awo onse ankhondo. Iye adzawawononga kotheratu, nawapereka kuti aphedwe.
3 Amih a ngawn te a voeih vaengah a rhok kah a bothae te rhim ni. Amih thii loh tlang a yut sak ni.
Anthu awo ophedwa adzatayidwa kunja, mitembo yawo idzawola ndi kununkha; mapiri adzafiira ndi magazi awo.
4 Vaan dong caempuei boeih te muei vetih vaan cabu bangla kolong uh ni. Amih kah caempuei boeih te misur hnah a hoo bangla, thaibu a hoo bangla hoo ni.
Dzuwa, mwezi ndi nyenyezi zidzasungunuka ndipo mlengalenga mudzakulungidwa ngati chipepala; nyenyezi zonse zidzayoyoka ngati masamba ofota a mphesa, ngati masamba onyala a mtengo wa mkuyu.
5 Ka cunghang loh vaan ah hmilhmal tih Edom a cuk thil. Pilnam te kamah kah yaehtaboeih loh laitloeknah neh a pha coeng.
Yehova akuti, “Lupanga langa lakhutiratu magazi kumwamba; taonani, likutsika kudzalanga anthu a ku Edomu, anthu amene ndawawononga kotheratu.”
6 BOEIPA kah cunghang tah a thii hah coeng. Bozrah kah BOEIPA hmueih neh Edom khohmuen kah maeh len kongah maehtha neh, tuca thii neh, kikong neh tutal kuel kah a tha loh a men sak.
Lupanga la Yehova lakhuta magazi, lakutidwa ndi mafuta; magazi a ana ankhosa onenepa ndi ambuzi, mafuta a ku impsyo za nkhosa zazimuna. Pakuti Yehova ali ndi nsembe mu Bozira ndiko kuphedwa kwa anthu ambiri mʼdziko la Edomu.
7 Cung neh vaito lueng khaw amih taengla suntla ni. Te vaengah a khohmuen te thii neh hmilhmal vetih a laipi khaw maehtha bangla men ni.
Pamodzi ndi anthuwo zidzaphedwanso njati, ngʼombe zazimuna zazingʼono ndi zazikulu zomwe. Dziko lawo lidzakhala magazi okhaokha, ndipo nthaka idzakutidwa ndi mafuta.
8 BOEIPA taengah phulohnah khohnin neh, Zion kah tuituknah te a sah kum khaw om.
Iyi ndi nthawi imene Yehova adzalipsira ndi kulanga adani a Ziyoni.
9 A soklong te kunhnai la, a laipi te kat la poeh ni. A khohmuen te kunhnai rhawm la poeh ni.
Madzi a mʼmitsinje ya Edomu adzasanduka phula, ndipo fumbi lake lidzasanduka sulufule; dziko lake lidzasanduka phula lamoto!
10 Khoyin khothaih kumhal duela thi mahpawh. A khu khaw cadilcahma lamkah cadilcahma patoeng taengla cet ni. A yoeyah kah a yoeyah la khap uh vetih te long te paan uh voel mahpawh.
Motowo sudzazimitsidwa usiku ndi usana; utsi wake udzafuka kosalekeza. Dzikolo lidzakhala chipululu pa mibado ndi mibado; palibe ndi mmodzi yemwe amene adzadutsemo.
11 Khosoek saelbu, kharhoeng neh saelbu loh a pang vetih vangak loh kho a sak thil ni. Rhilam te hinghong la, lungto he a hong la a toe uh.
Mʼdzikomo mudzakhala akabawi ndi anungu; amantchichi ndi akhwangwala adzapanga zisa zawo mʼmenemo. Mulungu adzatambalitsa pa Edomu chingwe choyezera cha chisokonezo ndi chingwe chowongolera cha chiwonongeko.
12 A hlangcoelh rhoek khaw a ram ah hah a khueh uh vetih a mangpa rhoek khaw a honghi la boeih om ni.
Anthu olemekezeka ake sadzatchedwanso mfumu kumeneko; akalonga ake onse adzachotsedwa.
13 A impuei te dohui hling loh, a hmuencak te mutlo hling loh a yam thil ni. Te vaengah pongui kah tolkhoeng la, tuirhuk vanu kah a bu la poeh ni.
Minga idzamera mʼnyumba zake zankhondo zotetezedwa, khwisa ndi mitungwi zidzamera mʼmalinga ake. Ankhandwe azidzadya mʼmenemo; malo okhalamo akadzidzi.
14 Te vaengah kohong neh sa-ui hum vetih maae loh a hui a khue ni. Vathae khaw pahoi paa vetih amah ham ngolbuel a hmuh ni.
Avumbwe adzakumana ndi afisi, ndipo zirombo za mʼchipululu zizidzayitanizana. Kumeneko kudzafikanso mizimu yoyipa ndi kupeza malo opumulirako.
15 Te ah valah loh bu a tuk vetih oi ni. A khae phoeiah tah a hlipkhup ah a ku thil ni. Te ah te valae rhoek khaw tingtun uh vetih a la te a paa cu ni.
Kadzidzi adzamangako chisa chake nʼkuyikirako mazira, adzaswa ana ake ndi kusamalira ana ake mu mthunzi wa mapiko ake; akamtema adzasonkhananso kumeneko, awiriawiri.
16 BOEIPA kah cabu dongah cae uh lamtah tae uh lah. Amih kah pakhat khaw hmaai mahpawh. A la pakhat khaw a paa vawt uh mahpawh. Ka ka loh a uen coeng dongah amih te BOEIPA kah a mueihla loh a coi ni.
Funafunani mʼbuku la Yehova ndi kuwerenga: mwa zolengedwazi palibe chimene chidzasowa; sipadzakhala nʼchimodzi chomwe chopanda chinzake. Pakuti Yehova walamula kuti zitero, ndipo Mzimu wake udzawasonkhanitsa pamodzi.
17 Amah loh amih ham hmulung a nan pah. A kut loh amih ham rhilam a suem pah te kumhal duela a pang uh ni. Cadilcahma phoeikah cadilcahma loh a khuiah kho a sak uh ni.
Yehova wagawa dziko lawo; wapatsa chilichonse chigawo chake. Dziko lidzakhala lawo mpaka muyaya ndipo zidzakhala mʼmenemo pa mibado yonse.