< Ezekiel 8 >
1 Kum rhuk kum hla rhuk dongkah hnin nga a lo vaengah kamah im ah ka ngol tih kamah mikhmuh ah Judah kah patong rhoek khaw ngol uh. Te vaengah ka Boeipa Yahovah kah kut he kai sola pahoi ha tla.
Tsiku lachisanu la mwezi wachisanu ndi chimodzi, mʼchaka chachisanu ndi chimodzi, ndinakhala mʼnyumba mwanga pamodzi ndi akuluakulu a ku Yuda. Tsono mphamvu za Ambuye Yehova zinandifikira.
2 Ka sawt vaengah hmai kah a mueimae bangla phek om he. A mueimae te a cinghen lamloh a dang due hmai bangla om. A cinghen lamloh a so duela rhohumbok kah a pang neh khophaa kah mueimae bangla om.
Nditayangʼana ndinangoona chinthu chooneka ngati munthu. Kuchokera pamene pamaoneka ngati chiwuno chake kumatsika mʼmunsi anali ngati moto, ndipo kuchokera mʼchiwuno kukwera mmwamba amaoneka mowala ngati mkuwa wonyezimira.
3 Kut kah muei bang te a thueng tih ka lu samtoel ah kai n'doek. Te vaengah mueihla loh kai he diklai laklo neh vaan laklo la m'pom. Te phoeiah kai te Pathen kah mangthui khuiah tlangpuei la aka mael Jerusalem khui kah vongka thohka la ng'khuen. Te te thatlainah mueimae neh aka thatlai kah tolrhum ni.
Iye anatambasula chinthu chooneka ngati dzanja ndipo anagwira tsitsi la pamutu panga. Nthawi yomweyo Mzimu unandikweza mlengalenga. Tsono ndikumachita ngati ndikuona Mulungu kutulo, Mzimu uja unapita nane ku Yerusalemu nundiyika pa khomo la chipata chamʼkati choyangʼana kumpoto. Kumeneko kunali fano limene limaputa mkwiyo wa Mulungu.
4 Te vaengah Israel Pathen kah thangpomnah he kolbawn ah a mueimae la pahoi ka hmuh coeng he.
Kumeneko ndinaona ulemerero wa Mulungu wa Israeli ngati momwe ndinaonera mʼmasomphenya mʼchigwa muja.
5 Te phoeiah kai taengah, “Hlang capa aw, tlangpuei longpuei la na mik huel laeh,” a ti. Ka mik he tlangpuei longpuei la ka huel tangloeng hatah thatlainah mueimae kah hmueihtuk vongka te tlangpuei ah kak ka hmuh. Te te thohkaeng ah ni a om.
Tsono Yehova anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, tayangʼana kumpoto.” Choncho ndinayangʼana kumpoto ndipo ndinaona pa khomo la chipata pafupi ndi guwa lansembe ndinaona fano loputa mkwiyo wa Mulungu lija.
6 Te phoeiah kai taengah, “Hlang capa, amih te na hmuh nama? Amih loh tueilaehkoi a saii uh khungdaeng coeng te. Ka rhokso lamloh lakhla ham he Israel imkhui long ni a saii. Tedae koep na mael vetih tueilaehkoi khaw muep na hmuh bitni,” a ti.
Ndipo Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi ukuona zimene akuchitazi, zonyansa zazikulu zimene Aisraeli akuchita kuno, zinthu zondichotsa Ine kumalo anga opatulika? Koma iwe udzaona zinthu zimene zili zonyansa kwambiri.”
7 Te phoeiah kai te vongup thohka la ng'khuen hatah pangbueng dongah a khui pakhat te lawt ka hmuh.
Kenaka Iye anandipititsa ku khomo lolowera ku bwalo la Nyumba ya Mulungu. Nditayangʼanitsitsa ndinangoona dzenje pa khomapo.
8 Te vaengah kai taengah, “Hlang capa, pangbueng te thuk laeh,” a ti. Te dongah pangbueng te ka thuk hatah thohka pakhat lawt ka hmuh.
Yehova anandiwuza kuti, “Iwe mwana wa munthu, tsopano bowola pa khomapo.” Ndinabowoladi pa khomapo ndipo ndinapezapo khomo.
9 Te phoeiah kai taengah, “Paan lamtah boethae rhoek kah tueilaehkoi te so lah, te te amih long ni he ah he a saii uh,” a ti.
Ndipo Yehova anandiwuza kuti, “Lowa, ndipo ona zinthu zonyansa zimene akuchita pamenepa.”
10 Ka kun vaengah rhulcai muei cungkuem neh konawhnah rhamsa kah mueirhol boeih khaw kak ka hmuh. Te te Israel im ah pangbueng kah a kaep a kaep ah a vuel.
Motero Ine ndinalowa ndi kuyangʼana, ndipo ndinaona pa makoma onse zithunzi za zinthu zosiyanasiyana zokwawa pansi, za nyama zonyansa ndiponso za mafano onse amene Aisraeli ankapembedza.
11 Amih lakli ah Israel imkhui kah patong hlang sawmrhih neh Shaphan capa Jaazaniah khaw pai. Amih hmai ah aka pai hlang loh a kut dongah hmaibael te a pom. Te vaengah bo-ul kah a hu a thah la khu.
Patsogolo pa zimenezi panayima akuluakulu makumi asanu ndi awiri a Aisraeli, ndipo Yaazaniya mwana wa Safani anali atayima pakati pawo. Aliyense wa iwo anali ndi chofukizira lubani mʼdzanja lake ndipo utsi wa fungo lokoma la lubani unkafuka.
12 Te phoeiah kai taengah, “Hlang capa, Israel im kah patong rhoek loh a ngaihlih imkhui kah hlang neh hmaisuep ah a saii te na hmuh nama? 'BOEIPA loh mamih m'hmuh pawt tih khohmuen he BOEIPA loh a hnoo coeng,” a ti uh,” a ti.
Tsono Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi waona zimene akuluakulu a Aisraeli akuchita mu mdima, aliyense akupembedza fano lakelake mʼnyumbamo? Iwo akuti, ‘Yehova sakutiona; Yehova walisiya dziko!’
13 Te phoeiah kai taengah, “Koep na mael vaengah amih loh tueilaehkoi a tanglue a saii uh te na hmuh bitni,” a ti.
Iye anandiwuzanso kuti, ‘Iwe udzawaonanso akuchita zinthu zonyansa kwambiri.’”
14 Te dongah kai te tlangpuei kah BOEIPA im vongka kah thohka la m'pawk puei. Te vaengah manu tarha ana ngol pahoi tih Tammuz te a rhah uh.
Kenaka anapita nane pa khomo la ku khomo la chipata cha Nyumba ya Mulungu choyangʼana kumpoto, ndipo kumeneko ndinaona akazi ena atakhala pansi, akulira mulungu wawo wotchedwa Tamuzi.
15 Te vaengah kai taengah, “Hlang capa na hmuh coeng nama? Koep na mael vaengah he lakah a nah la tueilaehkoi na hmuh ni,” a ti.
Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi ukuziona zimenezi? Iwe udzaona zinthu zimene zili zonyansa kwambiri kuposa izi.”
16 Te phoeiah kai te BOEIPA im vongup khui la m'pawk puei. Te vaengah BOEIPA bawkim thohka kah ngalha laklo neh hmueihtuk laklo ah hlang pakul panga tluk ana om. BOEIPA bawkim te a hnuk la a rhoe uh tih a maelhmai khothoeng la a khuehuh. Amih loh khothoeng kah khomik te a bawk uh.
Kenaka Iye anapita nane mʼkati mwa bwalo la Nyumba ya Yehova. Kumeneko ku khomo lolowera ku Nyumba ya Yehova pakati pa khonde ndi guwa lansembe, panali amuna 25. Anafulatira Nyumba ya Mulungu wa Yehova ndipo nkhope zawo zinaloza kummawa, ndipo ankapembedza dzuwa choyangʼana kummawa.
17 Te vaengah kai taengah, “Hlang capa na hmuh coeng nama? Judah imkhui loh tueilaehkoi a saii te phoeng a? Khohmuen te kuthlahnah neh cung sak kuekluek ham ni a saii uh he. Kai veet ham ni mael uh tih amih loh a hnarhong te thingluei a hu thil lah ko te.
Yehova anandifunsa kuti, “Iwe mwana wa munthu, kodi waziona zimenezi? Kodi nʼchinthu chopepuka kuti anthu a ku Yuda azichita zonyansa zimene akuchitazi pano? Kodi afike mpaka pomafalitsa za ndewu mʼdziko lonse? Iwotu akuwutsa ukali wanga. Akundipsetsa mtima ndi zochita zawo!
18 Te dongah kai loh kosi neh ka saii ni. Ka mik loh rhen pawt vetih lungma ka ti mahpawh. Ka hna ah ol ue la ng'khue uh cakhaw amih ol ka hnatun mahpawh,” a ti.
Choncho Ine ndidzawalanga ndili wokwiya. Sindidzawamvera chisoni kapena kuwaleka. Ngakhale atandifuwulira mʼmakutu mwanga sindidzawamvera.”