< Amos 3 >

1 Israel ca nangmih taeng neh Egypt khohmuen lamloh kang khuen van bangla, koca boeih taengah BOEIPA loh he ol a thui he hnatun uh.
Inu Aisraeli, imvani mawu awa amene Yehova wayankhula kutsutsana nanu, kutsutsana ndi banja lonse limene analitulutsa mu Igupto:
2 Diklai koca boeih lamloh nang bueng te kan ming. Te dongah namah kathaesainah boeih te namah taengah kan cawh ni.
“Inu nokha ndi amene ndinakusankhani pakati pa mabanja onse a dziko lapansi; nʼchifukwa chake ndidzakulangani chifukwa cha machimo anu onse.”
3 A tuentah pawt atah rhenten cet rhoi noek a?
Kodi anthu awiri nʼkuyendera limodzi asanapangane?
4 Duup kah sathueng a kawk vaengah amah ham maeh om het mahpawt nim? A khuisaek kah te a tuuk pawt atah sathueng loh a ol a huel bal nim?
Kodi mkango umabangula mʼnkhalango usanagwire nyama? Kodi msona wamkango umalira mʼphanga mwake pamene sunagwire kanthu?
5 Anih hamla hlaeh a om pawt lalah vaa ke diklai kah pael dongah tla aya? Diklai lamkah pael loh a boh phoeiah tah a tuuk rhoe a tuuk moenih a?
Kodi mbalame nʼkutera pa msampha pamene palibe nyambo yake? Kodi msampha umafwamphuka usanakole kanthu?
6 Khopuei ah tuki a ueng lalah pataeng pilnam he lakueng het mahpawt nim? Khopuei khuiah yoethae a pai lalah pataeng BOEIPA loh saii het mahpawt nim?” a ti.
Kodi pamene lipenga la nkhondo lalira mu mzinda, anthu sanjenjemera? Pamene tsoka lafika mu mzinda, kodi si Yehova amene wachititsa zimenezo?
7 A baecenol te a sal tonghma rhoek taengah a phoe mueh la ka Boeipa Yahovah loh hno a saii noek moenih.
Zoonadi Ambuye Yehova sachita kanthu asanawulule zimene akufuna kuchita kwa atumiki ake, aneneri.
8 Sathueng a kawk lalah ulong a rhih pawt eh? Ka Boeipa Yahovah loh a thui lalah unim aka tonghma pawt pai eh?
Mkango wabangula, ndani amene sachita mantha? Ambuye Yehova wayankhula, ndani amene sanganenere?
9 Ashdod kah impuei taeng neh Egypt khohmuen kah impuei taengah yaak sak. Te vaengah, “Samaria tlang ah tingtun uh,” ti nah. So uh lah, a khui kah soekloeknah neh a laklung kah hnaemtaeknah tah yet coeng.
Lengezani zimenezi ku nyumba zaufumu za ku Asidodi ndiponso ku nyumba zaufumu za ku Igupto: “Sonkhanani ku mapiri a ku Samariya; onani chisokonezo pakati pake ndiponso kuponderezana pakati pa anthu ake.”
10 BOEIPA kah olphong, oldueng vai ham khaw ming uh pawh. A impuei ah kuthlahnah neh rhoelrhanah a kael uh.
“Iwo sadziwa kuchita zolungama, ndipo amadzaza malo awo otetezedwa ndi zinthu zolanda ku nkhondo ndi zakuba,” akutero Yehova.
11 Te dongah ka Boeipa Yahovah loh he ni a thui. Rhal neh khohmuen kaepvai long khaw nang te n'suntlak thil vetih na sarhi neh na impuei te a poelyoe ni.
Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akunena izi: “Mdani adzalizungulira dzikoli; iye adzagwetsa malinga ako, ndi kufunkha nyumba zako zaufumu.”
12 BOEIPA loh he ni a thui. Boiva aka dawn long tah sathueng ka dongkah te a kho rhoi mai khaw, a hna vang mai khaw, a huul pah bangla Samaria kah baiphaih kil neh Damasku soengca ah aka ngol Israel ca rhoek te a huul uh van ni.
Yehova akuti, “Monga mʼbusa amalanditsa mʼkamwa mwa mkango miyendo iwiri yokha kapena msonga yokha ya khutu, moteronso ndimo mmene adzapulumukire Aisraeli amene amakhala mu Samariya pa msonga za mabedi awo, ndi ku Damasiko pa akakhutagona awo.”
13 Hnatun uh lamtah Jakob imkhui te rhalrhing sakuh. He tah ka Boeipa Yahovah, caempuei Pathen kah olphong ni.
“Imvani izi ndipo mupereke umboni wotsutsa nyumba ya Yakobo,” akutero Ambuye, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse.
14 A soah Israel kah boekoeknah ka cawh hnin ah ngawn tah Bethel hmueihtuk te ka cawh bal ni. Te vaengah hmueihtuk ki khaw tlawt vetih diklai la yalh ni.
“Pa tsiku limene ndidzalange Israeli chifukwa cha machimo ake, ndidzagumula maguwa ansembe a ku Beteli; nyanga za guwa zidzathyoka ndipo zidzagwa pansi.
15 Te phoeiah sikca im khaw khohal im neh ka top ni. Te vaengah vueino im rhoek te poo uh vetih im len rhoek khaw khoengvoep uh ni. He tah BOEIPA kah olphong coeng ni.
Ndidzagwetsa nyumba ya pa nthawi yozizira pamodzi ndi nyumba ya pa nthawi yotentha; nyumba zokongoletsedwa ndi minyanga ya njovu zidzawonongedwa ndipo nyumba zikuluzikulu zidzaphwasulidwa,” akutero Yehova.

< Amos 3 >