< Amos 2 >

1 BOEIPA loh he ni a thui. Moab kah boekoeknah pathum neh pali dongah anih te ka rhael mahpawh. Anih loh Edom manghai rhuh te lungbok la a tih dongah.
Yehova akuti, “Chifukwa anthu a ku Mowabu akunka nachimwirachimwira, Ine sindileka kuwalanga. Popeza anatentha mafupa a mfumu ya ku Edomu, mpaka kuwasandutsa phulusa,
2 Te dongah Moab soah hmai ka tueih vetih Kerioth impuei te a hlawp ni. Te vaengah Moab kah longlonah khuiah tamlung neh, tuki ol neh duek ni.
Ine ndidzatumiza moto pa Mowabu, umene udzanyeketsa nyumba zaufumu za ku Keriyoti. Mowabu adzafera pakati pa nkhondo yoopsa, mʼkati mwa mfuwu wa nkhondo ndi kuliza malipenga.
3 Te dongah, “A khui lamkah lai aka tloek te ka saii vetih a mangpa boeih te amah neh ka ngawn ni,” tila BOEIPA loh a thui.
Ndidzawononga wolamulira wake ndi kupha akuluakulu onse amene ali pamodzi ndi iye,” akutero Yehova.
4 BOEIPA loh he he ni a thui. Judah kah boekoeknah pathum neh pali dongah anih te ka rhael mahpawh. BOEIPA kah olkhueng te a hnawt tih a oltlueh te a tuem uh moenih. Amih te a napa rhoek kah a hnukah caeh hamla a laithae dongah kho a hmang uh.
Yehova akuti, “Chifukwa anthu a ku Yuda akunka nachimwirachimwira, Ine sindileka kuwalanga. Popeza iwo akana lamulo la Yehova ndipo sanasunge malangizo ake, popeza asocheretsedwa ndi milungu yabodza, milungu imene makolo awo ankayitsatira,
5 Te dongah Judah soah hmai ka tueih vetih Jerusalem kah impuei a hlawp ni.
Ine ndidzatumiza moto pa Yuda, umene udzanyeketsa nyumba zaufumu za ku Yerusalemu.”
6 BOEIPA loh he ni a thui. Israel kah boekoeknah pathum neh pali dongah anih te ka rhael mahpawh. Amih loh dueng te tangka la, khodaeng te khokhom la a yoih.
Yehova akuti, “Chifukwa anthu a ku Israeli akunka nachimwirachimwira, Ine sindileka kuwalanga. Iwo amagulitsa anthu olungama ndi siliva, ndi osauka ndi nsapato.
7 tattloel kah lu te diklai laipi dongah a thithut uh tih kodo kah longpuei te a mak uh. Tongpa neh a napa loh hula pakhat taengla a caeh thil dongah ka cimcaihnah ming he a poeih.
Amapondereza anthu osauka ngati akuponda fumbi, ndipo sawaweruza mwachilungamo anthu oponderezedwa. Abambo ndi mwana wawo amagonana ndi mtsikana mmodzi yemweyo, ndipo potero amanyozetsa dzina langa loyera.
8 Hmueihtuk boeih taengah laikoi himbai neh rhoel uh tih a Pathen im kah lai sah yu te a ok uh.
Anthuwo amakagonana mʼmbali mwa guwa lililonse la nsembe pa zovala zimene anatenga ngati chikole. Mʼnyumba ya mulungu wawo amamweramo vinyo amene analipiritsa anthu pa milandu.
9 Kai loh Amori te amih mikhmuh ah ka mitmoeng sak coeng. A sang te lamphai bangla sang tih thingnu bangla tlung sitoe cakhaw a soi kah a thaih neh a hmui kah a yung te ka mit sak.
“Ine ndinawononga Aamori pamaso pawo, ngakhale iwo anali anthu ataliatali ngati mikungudza ndiponso amphamvu ngati mitengo ya thundu. Ndinawononga zipatso zawo ndiponso mizu yawo.
10 Kai loh nangmih te Egypt khohmuen lamloh kang khuen tih Amori khohmuen pang sak hamla nangmih te khosoek ah kum sawmli kan pongpa puei.
“Ine ndinakutulutsani ku Igupto, ndipo ndinakutsogolerani mʼchipululu kwa zaka makumi anayi, kudzakupatsani dziko la Aamori.
11 Na ca rhoek lamloh tonghma la, na tongpang rhoek lamkah hlangcoelh la ka pai sak. Te khaw Israel ca kah moenih a? He tah BOEIPA kah olphong coeng ni.
Ine ndinawutsanso ena mwa ana ako kuti akhale aneneri, ndi ena mwa anyamata ako kuti akhale anaziri. Kodi si choncho, inu Aisraeli?” akutero Yehova.
12 Tedae hlangcoelh rhoek te misurtui na tul uh. Tonghma rhoek te khaw na uen uh tih, “Tonghma boeh ne,” na ti nauh.
“Koma inu munawamwetsa vinyo anaziri aja, ndipo munalamula aneneri kuti asanenere.
13 Cangpa a bae te leng loh a rhuelh bangla kai loh nangmih te kang rhuelh coeng ne.
“Tsono Ine ndidzakupsinjani monga imapsinjikira ngolo imene yadzaza ndi tirigu.
14 Kapyang lamloh thuhaelnah khaw bing vetih tlungluen kah a thadueng khaw caang mahpawh. Hlangrhalh long khaw a hinglu loeih sak mahpawh.
Munthu waliwiro sadzatha kuthawa, munthu wamphamvu sadzakhalanso ndi nyonga, wankhondo sadzapulumutsa moyo wake.
15 Lii aka muk khaw pai ngoeng pawt vetih a kap aka yanghoep khaw loeih mahpawh. Marhang dongkah aka ngol long khaw a hinglu loeih mahpawh.
Munthu wa uta sadzalimbika, msilikali wothamanga kwambiri sadzapulumuka, ndipo wokwera pa akavalo sadzapulumutsa moyo wake.
16 Hlangrhalh lakli kah a lungbuei aka rhapsat pataeng te khohnin ah tah pumtling la rhaelrham ni. He tah BOEIPA kah olphong ni.
Ngakhale asilikali olimba mtima kwambiri adzathawa ali maliseche pa tsikulo,” akutero Yehova.

< Amos 2 >