< Tingtoeng 50 >
1 Asaph kah Tingtoenglung Pathen, BOEIPA Pathen loh a thui tih, khocuk lamkah khotlak duela, diklai a tuentah.
Salimo la Asafu. Wamphamvuyo, Yehova Mulungu, akuyankhula ndi kuyitanitsa dziko lapansi kuyambira kotulukira dzuwa mpaka kumene limalowera.
2 Pathen kah a sakthen a soepnah loh Zion lamkah ha sae.
Kuchokera ku Ziyoni, mokongola kwambiri Mulungu akuwala.
3 Mamih kah Pathen te halo tih omlip pawh. A hmai ah hmai loh a hlawp tih a taengvai ah boehoeng khohli.
Mulungu wathu akubwera ndipo sadzakhala chete; moto ukunyeketsa patsogolo pake, ndipo pomuzungulira pali mphepo yamkuntho
4 A pilnam te laitloek ham a sosang kah vaan rhoek neh diklai te a tuentah.
Iye akuyitanitsa zamumlengalenga ndi za pa dziko lapansi kuti aweruze anthu ake.
5 Hmueih neh ka paipi aka saii, ka hlangcim rhoek kai taengla tingtun uh lah.
Mundisonkhanitsire okhulupirika anga, amene anachita pangano ndi ine pochita nsembe.
6 Pathen amah loh lai a tloek dongah a duengnah te vaan rhoek long khaw a thui uh. (Selah)
Ndipo mayiko akumwamba akulengeza chilungamo chake, pakuti Mulungu mwini ndi woweruza.
7 Ka pilnam aw ya van lah. Israel taengah ka voek vetih Pathen kamah, nangmih kah Pathen loh nangmih taengah ka laipai ni.
Imvani inu anthu anga, ndipo Ine ndidzayankhula, iwe Israeli, ndipo Ine ndidzayankhula mokutsutsa; ndine Mulungu, Mulungu wako.
8 Nang kah hmueih neh na hmueihhlutnah dongah nang kan tluung moenih. Ka hmai ah om taitu ngawn.
Sindikudzudzula chifukwa cha nsembe zako, kapena nsembe zako zopsereza zimene zili pamaso panga nthawi zonse.
9 Na im kah vaitotal khaw, na vongtung kah kikong khaw ka doe moenih.
Ine sindikufuna ngʼombe yayimuna kuchokera mʼkhola lako kapena mbuzi za mʼkhola lako,
10 Duup kah mulhing boeih neh tlang thawngkhat kah rhamsa boeih ke kamah koe ni.
pakuti nyama iliyonse yakunkhalango ndi yanga ndiponso ngʼombe za ku mapiri ochuluka.
11 Tlang kah vaa boeih te ka ming tih kohong kah satlung khaw kamah taengah om coeng.
Ine ndimadziwa mbalame iliyonse mʼmapiri ndiponso zolengedwa zonse zakutchire ndi zanga.
12 Lunglai neh a khuikah boeih te kamah taengah om tih ka lamlum cakhaw nang taengah ka thui mahpawh.
Ndikanakhala ndi njala sindikanakuwuzani, pakuti dziko lonse ndi zonse zimene zili mʼmenemo ndi zanga.
13 Vaito lueng saa te ka caak vetih kikong thii te ka ok aya?
Kodi ndimadya nyama ya ngʼombe zazimuna kapena kumwa magazi a mbuzi?
14 Uemonah te Pathen taengah nawn lamtah na olcaeng te Khohni taengah thuung lah.
“Pereka nsembe zachiyamiko kwa Mulungu, kwaniritsa malonjezo ako kwa Wammwambamwamba.
15 Te dongah citcai tue vaengah kai n'khue lah. Nang kan pumcum vetih kai nan thangpom ni.
Ndipo undiyitane pa tsiku lako la masautso; Ine ndidzakulanditsa, ndipo udzandilemekeza.”
16 Tedae Pathen loh halang te, “Ka oltlueh aka tae ham neh na ka dongah ka paipi aka khuen nang te bahamlae?
Koma kwa woyipa, Mulungu akuti, “Kodi uli ndi mphamvu yanji kuti uzinena malamulo anga kapena kutenga pangano langa pa milomo yako?
17 Thuituennah na hmuhuet tih ka ol he na hnukla na voeih.
Iwe umadana ndi malangizo anga ndipo umaponyera kumbuyo kwako mawu anga.
18 Hlanghuen na hmuh vaengah, anih taeng neh na hamsum dongkah, samphaih rhoek taengah na ngaingaih.
Ukaona wakuba umamutsatira, umachita maere ako pamodzi ndi achigololo
19 Boethae ham na ka na hnonah tih na lai kah thailatnah neh na sun.
Umagwiritsa ntchito pakamwa pako pa zinthu zoyipa ndipo umakonza lilime lako kuchita chinyengo.
20 Na pacaboeina taengah na ngol tih na cal van dae na manu ca te boekoekthingka na paek.
Nthawi zonse umayankhula motsutsana ndi mʼbale wako ndipo umasinjirira mwana wa amayi ako enieni.
21 Hekah he na saii vaengah ka omlip hatah namah bangla om khaw om ni tila na poek. Nang te kan tluung vetih na mikhmuh ah kan yan ni.
Wachita zimenezi ndipo Ine ndinali chete; umaganiza kuti ndine wofanana nawe koma ndidzakudzudzula ndipo ndidzakutsutsa pamaso pako.
22 He he Pathen aka hnilh rhoek loh yakming uh laeh. Kam poel vetih aka huul om pawt ve.
“Ganizira izi, iwe amene umayiwala Mulungu kuti ndingakukadzule popanda wokupulumutsa:
23 Uemonah aka nawn loh kai n'thangpom tih longpuei a rhoek a bah dongah Pathen kah daemnah te anih ka tueng ni,” a ti.
Iye amene amapereka nsembe yamayamiko amandilemekeza, ndipo amakonza njira zake kuti ndimuonetse chipulumutso cha Mulungu.”