< Tingtoeng 31 >

1 David kah Tingtoenglung neh aka mawt ham. BOEIPA nang dongah ka ying tih kumhal duela yah sak boeh. Na duengnah neh kai n'hlawt lah.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mwa Inu Yehova, ine ndimathawiramo; musalole nʼkomwe kuti ndichititsidwe manyazi; mundipulumutse chifukwa cha chilungamo chanu.
2 Na hna te kai taengah rhep duen lamtah kai he tlek n'huul lah. Kai ham lunghim lungpang la, kai aka khang ham rhalvong im la om lah.
Tcherani khutu lanu kwa ine, bwerani msanga kudzandilanditsa; mukhale thanthwe langa lothawirapo, linga lolimba kundipulumutsa ine.
3 Nang tah ka thaelpang neh ka rhalvong ni. Te dongah namah ming ham kai nan mawt tih nan khool.
Popeza Inu ndinu thanthwe langa ndi linga langa, chifukwa cha dzina lanu tsogolereni ndi kundiwongolera.
4 Namah te ka lunghim coeng dongah kai ham a tung uh lawk lamkah te nan doek.
Ndimasuleni mu msampha umene anditchera pakuti ndinu pothawirapo panga.
5 Ka mueihla he na kut ah kan hlah tih oltak Pathen BOEIPA loh kai he nan lat.
Mʼmanja mwanu ndipereka mzimu wanga; womboleni Yehova Mulungu wachoonadi.
6 A poeyoek la a honghi aka ngaithuen khaw ka hmuhuet tih kai tah BOEIPA ni ka pangtung.
Koma ine ndimadana nawo amene amamamatira mafano achabechabe; ine ndimadalira Yehova.
7 Namah kah sitlohnah neh kai kah phacip phabaem te nan hmuh tih ka hinglu kah citcai te nan ming dongah ka omngaih vetih ka kohoe ni.
Ndidzakondwa ndi kusangalala mʼchikondi chanu popeza Inu munaona masautso anga ndipo mumadziwa kuwawa kwa moyo wanga.
8 Te dongah kai he thunkha kut ah nan tloeng mueh la ka kho he a hoengpoeknah ah nan sut.
Inu simunandipereke kwa mdani koma mwayika mapazi anga pa malo otakasuka.
9 Konoinah dongah ka mik, ka hinglu neh ka bungko hmawn tih puen ka cak dongah kai n'rhen dae BOEIPA.
Mundichitire chifundo Inu Yehova pakuti ndili pa mavuto; maso anga akulefuka ndi chisoni, mʼmoyo mwanga ndi mʼthupi mwanga momwe mukupweteka.
10 Ka hingnah he kothae loh a ngawn tih ka hueinah neh ka kum thok. Kamah kathaesainah dongah ka thadueng yaai tih ka rhuh hmawn. Te vaengah tol long ah kai aka hmu kamah hmaiben rhoek te kai lamloh birhihnah neh yong uh.
Moyo wanga ukunyeka chifukwa cha kuwawidwa mtima ndi zaka zanga chifukwa cha kubuwula; mphamvu zanga zatha chifuwa cha masautso, ndipo mafupa anga akulefuka.
11 Kamah puencak dongah hlang boeih neh ka imben kah kokhahnah la mat ka om.
Chifukwa cha adani anga onse, ndine wonyozeka kwambiri ndi anansi anga; ndine chochititsa manyazi kwa abwenzi anga. Iwo amene amandiona mu msewu amandithawa.
12 Duek tangtae bangla a lungbuei ah kai n'hnilh. Am poo bangla ka om.
Ine ndinayiwalika kwa iwo ngati kuti ndinamwalira; ndakhala ngati mʼphika wosweka.
13 theetnah he kaepvai ah rhihnah la muep ka yaak. Amih te kai soah tingtun tih, ka hinglu loh hamla a mangtaeng uh.
Pakuti ine ndamva zonena zoyipa za anthu ambiri; zoopsa zandizungulira mbali zonse; iwo akukonza chiwembu kuti alimbane nane, kuti atenge moyo wanga.
14 Tedae kai tah BOEIPA nang dongah ka pangtung tih nang te ka Pathen ni ka ti.
Koma ndikudalira Inu Yehova; ndikunena kuti, “Ndinu Mulungu wanga.”
15 Ka khohnin he na kut dongah om. Ka thunkha kut neh kai aka hloem kut lamkah kai n'huul lah.
Masiku anga ali mʼmanja mwanu; ndipulumutseni kwa adani anga ndi kwa iwo amene akundithamangitsa.
16 Na sal taengah na maelhmai te han sae sak lah. Na sitlohnah neh kai n'khang lah.
Walitsani nkhope yanu pa mtumiki wanu; pulumutseni mwa chikondi chanu chosatha.
17 BOEIPA nang kan khue vaengah yah m'poh sak boeh. Halang rhoek te yahpok saeh lamtah saelkhui la duem uh saeh. (Sheol h7585)
Yehova musalole kuti ndichite manyazi, pakuti ndalirira kwa Inu; koma oyipa achititsidwe manyazi ndipo agone chete mʼmanda. (Sheol h7585)
18 Hlang dueng te hoemnah neh nueihbu la a hong aka thui mangkhak rhoek loh a kam khom saeh.
Milomo yawo yabodzayo ikhale chete, pakuti chifukwa cha kunyada ayankhula modzikuza kutsutsana ndi wolungama.
19 Namah aka rhih rhoek ham na khoem pah tih hlang capa rhoek hmuh ah namah dongla aka ying rhoek ham na saii pah na thennah he bahoeng len.
Ndi waukulu ubwino wanu umene mwawasungira amene amakuopani, umene mumapereka anthu akuona kwa iwo amene amathawira kwa Inu.
20 Hlang kah tangkhuepnah lamkah na hmai kah a huephael ah amih te na thuh. Tuituknah ol lamkah pohlip ah amih te na khoem.
Mu mthunzi wa pamalo popezeka panu muwabisa, kuwateteza ku ziwembu za anthu; mʼmalo anu okhalamo mumawateteza kwa anthu owatsutsa.
21 Khopuei vongup khuiah kai ham a sitlohnah khobaerhambae la a tueng dongah BOEIPA tah a yoethen pai.
Matamando akhale kwa Yehova, pakuti anaonetsa chikondi chake chodabwitsa kwa ine pamene ndinali mu mzinda wozingidwa.
22 Te dongah ka tamto vaengah, “Na mikhmuh lamkah ka pat coeng,” ka ti. Tedae namah taengla ka pang vaengah ka huithuinah ol nan yaak.
Ndili mʼnkhawa zanga ndinati, “Ine ndachotsedwa pamaso panu!” Komabe Inu munamva kupempha chifundo kwanga pamene ndinapempha thandizo kwa Inu.
23 Amah kah hlangcim rhoek boeih loh BOEIPA te lungnah uh lah. Oltak te BOEIPA loh a kueinah tih hoemnah aka saii te a khawk la a thuung.
Kondani Yehova oyera mtima ake onse! Yehova amasunga wokhulupirika koma amalanga kwathunthu anthu odzikuza.
24 BOEIPA dongah aka ngaiuep boeih loh thahuel uh lamtah na thinko cak sakuh.
Khalani ndi nyonga ndipo limbani mtima, inu nonse amene mumayembekezera Yehova.

< Tingtoeng 31 >