< Tingtoeng 143 >
1 David kah Tingtoenglung. Aw BOEIPA, ka thangthuinah he hnatun lah. Na uepomnah dongah ka huithuinah he hnakaeng lamtah na duengnah neh kai n'doo lah.
Salimo la Davide. Yehova imvani pemphero langa, mvetserani kulira kwanga kopempha chifundo; mwa kukhulupirika kwanu ndi chilungamo chanu bwerani kudzandithandiza.
2 Tedae mulhing boeih he namah mikhmuh ah a tang oeh pawt dongah na sal he khaw laitloeknah khuila na thak moenih.
Musazenge mlandu mtumiki wanu, pakuti palibe munthu wamoyo amene ndi wolungama pamaso panu.
3 Thunkha loh ka hinglu a hloem tih ka hingnah diklai ah a phop. Khosuen kah aka duek bangla khohmuep ah kai kho n'sak sak.
Mdani akundithamangitsa, iye wandipondereza pansi; wachititsa kuti ndikhale mu mdima ngati munthu amene anafa kale.
4 Te dongah ka mueihla loh ka khuiah rhae tih ka lungbuei khaw ka khui ah pong coeng.
Choncho mzimu wanga ukufowoka mʼkati mwanga; mʼkati mwanga, mtima wanga uli ndi nkhawa.
5 Hlamat kah khohnin ka poek tih na bisai boeih te ka thuep vaengah na kut dongkah bitat te ka lolmang thil. (Selah)
Ndimakumbukira masiku amakedzana; ndimalingalira za ntchito yanu yonse, ndimaganizira zimene manja anu anachita.
6 Namah taengah ni ka kut ka phuel. Ka hinglu he bumueh rhathih hmuen kah bangla namah taengah om. (Selah)
Ndatambalitsa manja anga kwa Inu; moyo wanga uli ndi ludzu lofuna Inu monga nthaka yowuma. (Sela)
7 BOEIPA aw, ka mueihla a khum he tokthuet lamtah kai n'doo lah. Kai lamloh na maelhmai thuh boel mai. Tangrhom kah ka suntla banghui la ka om van ve.
Yehova ndiyankheni msanga; mzimu wanga ukufowoka. Musandibisire nkhope yanu, mwina ndidzakhala ngati iwo amene atsikira ku dzenje.
8 Namah dongah ka pangtung vanbangla na sitlohnah neh mincang ah kai n'hnatun lah. Ka caeh ham longpuei te kai ming sak lah. Ka hinglu he namah taengah kan tloeng coeng.
Lolani kuti mmawa ubweretse mawu achikondi chanu chosasinthika, pakuti ine ndimadalira Inu. Mundisonyeze njira yoti ndiyendemo, pakuti kwa Inu nditukulira moyo wanga.
9 BOEIPA namah dongah ka kuep vanbangla ka thunkha kut lamloh kai n'huul lah.
Pulumutseni kwa adani anga, Inu Yehova, pakuti ndimabisala mwa Inu.
10 Ka Pathen la na om dongah na kolonah saii ham kai n'tukkil lah. Na Mueihla then loh tlangkol diklai ah kai m'mawt saeh.
Phunzitseni kuchita chifuniro chanu, popeza ndinu Mulungu wanga; Mzimu wanu wabwino unditsogolere pa njira yanu yosalala.
11 BOEIPA namah ming ham ni na duengnah dongah kai nan hing sak. Ka hinglu khaw citcai lamkah ni na doek.
Sungani moyo wanga Inu Yehova chifukwa cha dzina lanu; mwa chilungamo chanu tulutseni mʼmasautso anga.
12 Te dongah ka thunkha khaw na sitlohnah neh na biit tih na sal kai ham tah ka hinglu aka daengdaeh boeih te na paltham sak.
Mwa chikondi chanu chosasinthika khalitsani chete adani anga; wonongani adani anga, pakuti ndine mtumiki wanu.