< Olcueih 25 >

1 Tahae Solomon kah rhoek he Judah manghai Hezekiah kah hlang rhoek loh a puen uh bal.
Iyi ndi miyambo inanso ya Solomoni, imene anthu a Hezekiya mfumu ya ku Yuda analemba.
2 Pathen kah thangpomnah loh olka te a thuh tih, manghai kah thangpomnah long tah olka te a khe.
Ulemerero wa Mulungu uli pa kubisa zinthu; ulemerero wa mafumu uli pa kufufuza zinthuzo.
3 Buhuengpomnah he vaan ah, a laedil bal khaw diklai ah. Te dongah manghai rhoek kah lungbuei he khenah om pawh.
Monga momwe kwatalikira kumwamba ndi momwe kulili kuzama kwa dziko lapansi, ndi momwemonso alili maganizo a mfumu kusadziwika kwake.
4 Ngun te a aek met pah. Te daengah ni hnopai aka saii ham khaw a poeh pa eh.
Chotsa zoyipa mʼsiliva ndipo wosula adzapanga naye ziwiya.
5 Halang khaw manghai mikhmuh lamkah loh haek uh. Te daengah ni a ngolkhoel loh duengnah dongah a ngol eh.
Chotsa munthu woyipa pamaso pa mfumu; ndipo ufumu wake udzakhazikika mu chilungamo.
6 Manghai mikhmuh ah namah pom uh boeh, a hmuen tuenglue ah khaw pai boeh.
Usamadzikuze ukakhala pamaso pa mfumu, ndipo usamakhale pamalo pa anthu apamwamba;
7 Na mik loh a hmuh vanbangla, hlangcong mikhmuh ah na kunyun lakah, “Nang pahoi yoeng dae,” a ti te then ngai.
paja ndi bwino kuti mfumu ichite kukuwuza kuti, “Bwera pamwamba pano,” kulekana ndi kuti ikuchititse manyazi chifukwa cha wina wokuposa. Chimene wachiona ndi maso ako,
8 Toe koeloe ham khaw khuen boeh. Meltam khaw, na hui neh na hmai a thae vaengah a bawtnah ah na saii ve.
usafulumire kupita nacho ku bwalo la milandu nanga udzachita chiyani pa mapeto pake ngati mnansi wako adzakuchititsa manyazi?
9 Namah lamkah oelhtaihnah te na hui neh tuituk uh rhoi. Tedae baecenol he tah a tloe la puek sak boeh.
Kamba mlandu ndi mnansi wako, koma osawulula chinsinsi cha munthu wina
10 Uepom loh nang n'ya vetih nang taengah theetnah loh paa tlaih pawt ve.
kuopa kuti wina akamva mawu ako adzakuchititsa manyazi ndipo mbiri yako yoyipa sidzatha.
11 A buelhmaih la a thui olka tah cak ben dongkah sui thaihthawn la om.
Mawu amodzi woyankhulidwa moyenera ali ngati zokongoletsera zagolide mʼzotengera zasiliva.
12 Hlang cueih a tluung vaengah aka hnatun kah a hna dongah sui hnaii, sui himbai la a om pah.
Kwa munthu womvetsa bwino, kudzudzula kwa munthu wanzeru kuli ngati ndolo zagolide kapena chodzikongoletsera china cha golide wabwino kwambiri.
13 Cangah tue vaengkah vuelsong a dingsuek bangla, uepom laipai long tah amah aka tueih kung taeng neh a boei te khaw a hinglu a caih sak.
Wamthenga wodalirika ali ngati madzi ozizira pa nthawi yokolola kwa anthu amene amutuma; iye amaziziritsa mtima bwana wake.
14 Khomai neh khohli khaw om dae khonal a om pawt bangla, aka yan uh hlang kah kutdoe khaw a honghi ni.
Munthu wonyadira mphatso imene sayipereka ali ngati mitambo ndi mphepo yopanda mvula.
15 Thinsen rhangneh rhalboei a hloih thai tih, mongkawt ol loh songrhuh a khaem thai.
Kupirira ndiye kumagonjetsa mfumu, ndipo kufewa mʼkamwa kutha kumafatsitsa munthu wowuma mtima.
16 Khoitui na hmuh te a rhoeh ah na caak mako, n'lawt vetih na lok ve.
Ngati upeza uchi, ingodya okukwanira, kuopa ungakoledwe nawo ndi kuyamba kusanza.
17 Na kho te na hui im ah a rhoeh la hawn sak aih, nang n'hnuenah vetih namah te m'hmuhuet ve.
Uzipita kamodzikamodzi ku nyumba ya mnzako ukawirikiza kupita, udzadana naye.
18 A hui taengah a hong laipai la aka phoe hlang tah caemboh, cunghang neh thaltang aka haat bangla om.
Munthu wochitira mnzake umboni wonama, ali ngati chibonga kapena lupanga kapena muvi wakuthwa.
19 Citcai tue vaengah hnukpoh pangtungnah ngawn tah, no hom, kho aka haeh banghui pawn ni.
Kudalira munthu wosankhulupirika pa nthawi ya mavuto, kuli ngati dzino lobowoka kapena phazi lolumala.
20 Boethae lungbuei te laa neh aka hlai khaw, khosik tue vaengah himbai aka pit, a thuui dongah lunghuem bangla om.
Kuyimbira nyimbo munthu wachisoni kuli ngati kuvula zovala pa nyengo yozizira kapena kuthira mchere pa chilonda.
21 Na lunguet khaw a pongnaeng atah buh cah lamtah, a halh bal atah tui tul.
Ngati mdani wako ali ndi njala, mupatse chakudya kuti adye; ngati ali ndi ludzu mupatse madzi kuti amwe.
22 Te vaengah ni nang kah hmai-alh te a lu dongla poep uh coeng tih, BOEIPA loh nang yueng la a thuung ni.
Pochita izi, udzamusenzetsa makala a moto pa mutu pake, ndipo Yehova adzakupatsa mphotho.
23 Tlangpuei yilh loh khonal hang khuen. A huephael kah olka loh a mikhmuh ah kosi a sah.
Monga momwe mphepo yampoto imabweretsera mvula, chonchonso mjedu umadzetsa mkwiyo.
24 Imkhui ah huta kah olpungkacan neh hohmuhnah hloih dongkah lakah tah, imphu kah yael ah khosak he then ngai.
Nʼkwabwino kukhala pa ngodya ya denga kuposa kukhala mʼnyumba ndi mkazi wolongolola.
25 Khohla bangsang kho lamkah olthang then khaw buhmueh rhathih vaengkah hinglu ham tui ding bangla om.
Mthenga wabwino wochokera ku dziko lakutali ali ngati madzi ozizira kwa munthu waludzu.
26 Tuisih loh rhong tih thunsih loh a nu banghui la, aka dueng loh halang mikhmuh ah a yalh pah.
Munthu wolungama amene amagonjera munthu woyipa ali ngati kasupe wodzaza ndi matope kapena chitsime cha madzi oyipa.
27 Khoitui muep caak ham neh, thangpomnah loh a thangpomnah neh khenah he then pawh.
Sibwino kudya uchi wambiri, sibwinonso kudzifunira wekha ulemu.
28 Vongtung aka tal khopuei neh, a mueihla kah tungaepnah aka tal hlang tah sut rhawp.
Munthu amene samatha kudziretsa ali ngati mzinda umene adani awuthyola ndi kuwusiya wopanda malinga.

< Olcueih 25 >