< Olcueih 21 >
1 Manghai kah a lungbuei tah sokca tui bangla BOEIPA kut dongah om tih, a ngaih bangla boeih a hoihaeng.
Mtima wa mfumu uli ngati mtsinje wamadzi mʼdzanja la Yehova; Iye amautsongolera pa chilichonse chimene akufuna.
2 Longpuei boeih he hlang loh amah mikhmuh nen tah a thuem sak. Tedae BOEIPA long tah lungbuei ni a. khiing a lang.
Makhalidwe a munthu amaoneka olungama kwa mwini wakeyo, koma Yehova ndiye amayesa mtima wake.
3 Duengnah neh tiktamnah saii ham te BOEIPA loh hmueih lakah a ngaih.
Za chilungamo ndi zolondola ndi zomwe zimakondweretsa Yehova kuposa kupereka nsembe.
4 Mik dongkah buhuengpomnah neh lungbuei a mungkung he halang rhoek kah tholhnah hmaithoi ni.
Maso odzikuza ndi mtima wonyada, zimatsogolera anthu oyipa ngati nyale nʼchifukwa chake amachimwa.
5 Bi haam kah kopoek tah kumkonah la om yoeyah tih, aka cukhat boeih khaw tloelnah la om yoeyah.
Zolinga za munthu wakhama zimachulukitsa zinthu zake; koma aliyense wochita zinthu mofulumira amadzakhala wosauka.
6 A hong ol lamkah bisai neh thakvoh tah ahonghi la huu tih, dueknah ni kang a toem coeng.
Chuma chochipeza ndi mawu onyenga ndi chosakhalitsa ndipo chimakola anthu mu msampha wa imfa.
7 Halang loh a tiktam la saii ham a aal dongah, amamih kah a rhoelrhanah loh amamih a hmuh bitni.
Chiwawa cha anthu oyipa chidzawawononga, pakuti iwo amakana kuchita zolungama.
8 A ko aka boi hlang kah longpuei tah kawn dae, aka cil tah a bisai a thuem pah.
Njira ya munthu wolakwa ndi yokhotakhota, koma makhalidwe a munthu wosalakwa ndi olungama.
9 Hohmuhnah la aka om yuu neh hoilh aka khueh kah im lakah tah, imphu bangkil ah khosak te then ngai.
Nʼkwabwino kukhala wekha pa ngodya ya denga la nyumba, kuposa kukhala mʼnyumba pamodzi ndi mkazi wolongolola.
10 Halang kah a hinglu long tah boethae a ngaidam tih, a mikhmuh kah a hui te khaw rhen pawh.
Munthu woyipa amalakalaka zoyipa; sachitira chifundo mnansi wake wovutika.
11 Hmuiyoi loh lai a sah vaengah hlangyoe khaw cueih tih, a cueih hamla a cangbam vaengah mingnah khaw a dang.
Munthu wonyoza akalangidwa, anthu opusa amapeza nzeru; koma munthu wanzeru akalangizidwa, amapeza chidziwitso.
12 Hlang dueng long tah halang imkhui khaw a cangbam mai dae, halang rhoek long tah a thae la a paimaelh.
Zolingalira za munthu woyipa nʼzosabisika pamaso pa Yehova, ndipo Iye adzawononga woyipayo.
13 Tattloel kah a doek te a hna aka buem thil tah, amah a pang van vaengah doo uh mahpawh.
Amene atsekera mʼkhutu mwake wosauka akamalira, nayenso adzalira koma palibe adzamuyankhe.
14 A huephael kah kutdoe loh thintoek, a rhang dongkah kapbaih loh kosi aka tlung te a daeh sak.
Mphatso yoperekedwa mseri imathetsa mkwiyo, ndipo chiphuphu choperekedwa mobisa chimathetsa mphamvu ya ukali woopsa.
15 Hlang dueng hamtah tah a tiktamnah a saii te kohoenah la om tih, boethae aka saii rhoek ham tah porhaknah la om.
Chilungamo chikachitika anthu olungama amasangalala, koma anthu oyipa amaopsedwa nazo.
16 Hlang aka cangbam kah longpuei lamloh kho aka hmang hlang tah, sairhai kah hlangping lakli ah duem.
Munthu amene amachoka pa njira ya anthu anzeru adzapezeka mʼgulu la anthu akufa.
17 Kohoenah aka lungnah aih khaw hlang kah a tloelnah la poeh tih, misurtui neh situi aka lungnah khaw boei mahpawh.
Aliyense wokonda zisangalalo adzasanduka mʼmphawi, ndipo wokonda vinyo ndi mafuta sadzalemera.
18 Halang te hlang dueng ham, hnukpoh te aka thuem ham tlansum la om.
Anthu oyipa adzakhala chowombolera cha anthu olungama ndipo osakhulupirika chowombolera anthu olungama mtima.
19 Hohmuhnah, konoinah neh yuu taengah olpungkacan la om lakah tah, khosoek khohmuen ah khosak he then ngai.
Nʼkwabwino kukhala mʼchipululu kuposa kukhala ndi mkazi wolongolola ndi wopsa mtima msanga.
20 Hlang cueih tolkhoeng kah thakvoh neh situi tah a naikap dae, hlang ang long tah te te a yoop.
Munthu wanzeru samwaza chuma chake, koma wopusa amachiwononga.
21 Duengnah neh sitlohnah aka hloem long tah, duengnah neh thangpomnah dongkah hingnah te a dang ni.
Amene amatsata chilungamo ndi kukhulupirika, amapeza moyo ndi ulemerero.
22 Hlangrhalh rhoek kah khopuei te hlang cueih pakhat long ni a paan tih, a sarhi la a pangtungnah uh khaw a phil pah.
Munthu wanzeru amagonjetsa mzinda wa anthu amphamvu ndi kugwetsa linga limene iwo amalidalira.
23 A ol a ka aka tuem long tah, a hinglu te citcai khui lamkah a hoep a tlang.
Amene amagwira pakamwa pake ndi lilime lake sapeza mavuto.
24 Thinlen, moemlal, a ming ah hmuiyoi long tah, thinpom althanah neh a saii.
Munthu wonyada ndi wodzikuza amamutcha, “Mnyodoli,” iye amachita zinthu modzitama kwambiri.
25 A kut loh a saii ham a aal dongah kolhnaw kah hoehhamnah loh amah a duek sak ni.
Chilakolako cha munthu waulesi chidzamupha yekha chifukwa manja ake amangokhala goba osagwira ntchito.
26 Hnin takuem ah hoehhamnah te a ngaidam dae, aka dueng long tah a paek phoeiah khaw a hnaih moneih.
Tsiku lonse anthu oyipa amasirira zambiri, koma anthu olungama amapereka mowolowamanja.
27 Halang kah hmueih he tueilaehkoi ti bal vaengah, khonuen rhamtat la a khuen bal pueng.
Nsembe ya anthu oyipa imamunyansa Yehova, nanji akayipereka ndi cholinga choyipa!
28 Laithae kah laipai tah paltham vetih, aka hnatun hlang long ni a thui yoeyah eh.
Mboni yonama idzawonongeka, koma mawu a munthu wakumva adzakhala nthawi zonse.
29 Halang loh a mikhmuh dawk neh hlang a tanglue sak. Tedae aka thuem long tah a long, long ah a rhuep tih a yakming.
Munthu woyipa amafuna kudzionetsa ngati wolimba mtima, koma munthu wowongoka amaganizira njira zake.
30 BOEIPA aka tlai thil thai cueihnah khaw om pawh, lungcuei khaw om pawh, cilsuep khaw om thai pawh.
Palibe nzeru, palibe kumvetsa bwino, palibenso uphungu, zimene zingapambane Yehova.
31 Marhang khaw caemtloek hnin kah ham a tawn coeng dae, BOEIPA daengah ni loeihnah a dang.
Kavalo amamukonzera tsiku la nkhondo, koma ndi Yehova amene amapambanitsa.