< Joshua 15 >
1 Judah ca rhoek neh a hui a ko tarahing ah tuithim kah Zin khosoek Edom khorhi, tuithim khobawt te amih koca kah hmulung la a om pah.
Chigawo cha dzikolo chimene mabanja a fuko la Yuda analandira chinafika ku malire ndi Edomu mpaka ku chipululu cha Zini kummwera kwenikweni.
2 Te dongah lungkaeh li hmoi lamloh tuithim la aka hooi uh longken khaw, amih kah tuithim la om.
Malire awo a kummwera anayambira kummwera kwenikweni kwa Nyanja ya Mchere,
3 Akrabbim kham tuithim ah a khuen tih Zin la kat. Te phoeiah Kadeshbarnea tuithim la cet tih Khetsron la a kat sak. Te lamkah loh Addar te a paan tih Karka la mael.
kudutsa cha kummwera ku Akirabimu, nʼkupitirira mpaka ku Zini. Kuchokera pamenepo nʼkumapita cha kummwera kwa Kadesi Barinea, kudutsa Hezironi mpaka ku Adari ndi kutembenuka mpaka ku Karika.
4 Te phoeiah Azmon la kat phai tih Egypt soklong te a doo. Te lamkah te tuili rhi kah longrhael ah aka om aka om tah nangmih ham tuithim khorhi la om.
Anapitirira mpaka ku Azimoni motsata mtsinje umene uli malire a Igupto mpaka ku nyanja. Awa ndiwo malire awo a kummwera.
5 Lungkaeh li lamkah loh Jordan tuikung due khothoeng khorhi la om tih tuili longken lamloh Jordan tuikung ah tlangpuei ben kah khorhi la om.
Malire a kummawa anali Nyanja Yakufa mpaka kumene Yorodani amathira mu Nyanja ya Mchere. Malire a kumpoto anayambira kumene Yorodani amathirira nyanjayo,
6 Te phoeiah Bethhoglah khorhi la luei hang tih Bethkolken tlangpuei a paan phoeiah Reuben capa Bohan kah lungto rhi la luei.
napitirira mpaka ku Beti-Hogila ndi kupitirira kumpoto mpaka ku Beti-Araba. Anapitirira mpaka anakafika ku Mwala wa Bohani.
7 Te phoeiah Akor kol lamloh Debir khorhi la luei bal tih soklong tuithim kah Adummim kham dan Gilgal ah tlangpuei la hooi uh. Te phoeiah khorhi loh Enshemesh tui te a paan tih Enrogel ah a bawtnah om.
Ndipo malirewo anachokeranso ku chigwa cha Akori mpaka ku Debri, kuchokera ku chigwa cha Akori ndi kutembenukira kumpoto ku Giligala, dera limene linayangʼanana ndi msewu wa Adumimu kummwera kwa chigwa. Anapitirira mpaka ku madzi a ku Eni Semesi ndi kutulukira ku Eni Rogeli.
8 Kolrhawk khorhi tuithim kah Jebusi tlanghlaep ah Jerusalem la yong. Te phoeiah khorhi te tlangpuei kah Rapha kol hmoi, khotlak kolrhawk dan kah tlang soi la luei.
Ndipo anapitirira mpaka ku chigwa cha Hinomu mbali ya kummwera kwa mzinda wa Ayebusi (mzinda wa Yerusalemu). Kuchokera kumeneko anakwera mpaka pamwamba pa phiri kumadzulo kwa chigwa cha Hinomu cha kumpoto kwenikweni kwa chigwa cha Refaimu.
9 Te phoeiah khorhi te tlang so lamloh Nephtoah tuisih tui la ngooi thuk tih Ephron tlang kah khopuei rhoek te a paan phoeiah Kiriathjearim kah Baalah khorhi la rhum.
Ndipo anachokeranso pamwamba pa phiri, kukafika mpaka ku akasupe a ku Nepitowa, nadzatulukira ku mizinda ya phiri la Efroni, ndi kutsikira ku Baalahi (ndiye Kiriati Yearimu).
10 Baalah khotlak lamkah khorhi te Seir tlang la a ken bal tih Kesalon tlangpuei kah Jearim tlang hlaep la yong. Te phoeiah Bethshemesh la suntla tih Timnah la kat.
Kuchokera kumeneko anazungulira cha kumadzulo ku Baalahi mpaka ku phiri la Seiri. Anapitirira cha kumpoto kutsata phiri la Yearimu (lomwe ndi Kesaloni). Anapitirirabe kutsika ku Beti Semesi ndi kuwolokera ku Timna.
11 Te phoeiah khorhi te tlangpuei kah Ekron hlaep la pawk tih Shikkron khorhi ngooi. Te phoeiah Baalah tlang a pah tih Jabneel a pha phoeiah tuitun rhi ah a bawtnah om.
Malirewo anapitirira kumatsitso a mapiri chakumpoto kwa Ekroni, ndi kukhotera ku Sikeroni. Malirewo anadutsa phiri la Baalahi ndi kufika ku Yabineeli. Malirewo anathera ku nyanja.
12 Te dongah khotlak tuili puei khorhi neh Judah ca rhoek kah khorhi he, amah huiko rhoek loh a vael khorhi la om.
Malire a mbali ya kumadzulo anali Nyanja Yayikulu. Awa ndi malire ozungulira malo amene anapatsidwa kwa mabanja a fuko la Yuda.
13 BOEIPA kah olpaek vanbangla Joshua loh Judah koca lakli ah Jephuneh capa Kaleb ham Anakim napa Kiriatharba kah Hebron te khoyo la a phaeng.
Potsata lamulo la Yehova, Yoswa anapereka kwa Kalebe mwana wa Yefune gawo lina la dziko la Yuda dera la Kiriati Ariba, limene ndi Hebroni. (Ariba anali gogo wa Aanaki).
14 Te lamkah Anak koca pathum Sheshai, Ahiman neh Anakim cahlah Talmai te Kaleb loh a haek.
Kuchokera ku Hebroni, Kalebe anathamangitsamo mafuko a Aanaki awa: Sesai, Ahimani ndi Talimai, zidzukulu za Aanaki.
15 Te lamloh Debir khosa rhoek khaw a khoong thil. Debir kah a ming rhuem tah Kiriathsepher ni.
Kuchokera kumeneko, Kalebe anakathira nkhondo anthu amene ankakhala ku Debri (mzindawu poyamba unkatchedwa Kiriati Seferi).
16 Te vaengah Kaleb loh, “Kiriathsepher aka tloek tih aka lo te tah ka canu Akcah he a yuu la ka paek ni,” a ti.
Tsono Kalebe anati, “Munthu amene angathire nkhondo mzinda wa Kiriati Seferi ndi kuwulanda, ndidzamupatsa mwana wanga Akisa kuti akhale mkazi wake.”
17 Te dongah Kiriathsepher te Kaleb kah a manuca Kenaz capa Othniel loh a loh tih anih yuu la a canu Akcah te a paek.
Otanieli, mwana wa mʼbale wa Kalebe, Kenazi, ndiye anawulanda. Choncho Kalebe anamupatsa mwana wake Akisa kuti akhale mkazi wake.
18 Huta loh ham paan vaengah a napa taengkah khohmuen bih hamla a va te a vueh tih laak dong lamloh pawlh bit uh. Te dongah anih te Kaleb loh, “Nang tahh balae na ngaih,” a ti nah.
Tsiku lina atafika Akisayo, Otanieli anamuwumiriza mkazi wakeyo kuti apemphe munda kwa Kalebe abambo ake. Pamene Akisa anatsika pa bulu wake, Kalebe anamufunsa kuti, “Kodi ukufuna ndikuchitire chiyani.”
19 Te dongah, “Kai ham khaw yoethennah nan khueh atah tuithim khohmuen ke kai m'pae lamtah tuidueh tui khaw kai ham na khueh bal mako,” a ti nah. Te dongah anih te a siip tuidueh neh a hnawt tuidueh rhoek te a paek.
Iye anayankha kuti “Mundikomere mtima. Popeza mwandipatsa ku Negevi, kumalo kumene kulibe madzi, mundipatsenso akasupe amadzi.” Choncho Kalebe anamupatsa akasupe a kumtunda ndi a kumunsi.
20 He tah Judah ca rhoek loh amah koca khuiah a cako rhoek kah rho ni.
Dziko limene mabanja a fuko la Yuda analandira ngati cholowa chawo ndi ili:
21 Tuithim Edom khorhi kah Kabzeel, Eder, Jagur,
Mizinda yakummwera kwenikweni kwa fuko la Yuda yoyandikana ndi malire a Edomu anali: Kabizeeli, Ederi, Yaguri
22 Kinah, Dimonah, Adanah,
Kina, Dimona, Adada
23 Kedesh, Hazor, Ithnan,
Kedesi, Hazori, Itinani
25 Hazorhadattah neh Hazor kah Kerioth Khetsron,
Hazori-Hadata, Keriyoti Hezironi (ndiye kuti Hazori)
27 Hazargaddah, Heshmon, Bethpelet,
Hazari-Gada, Hesimoni, Beti-Peleti
28 Hazarshual, Beersheba, Biziothiah,
Hazari-Suwali, Beeriseba, Biziotiya,
30 Eltolad, Kesil, Hormah,
Elitoladi, Kesili, Horima
31 Ziklag, Madmannah, Sansannah,
Zikilagi, Madimena, Sanisana,
32 Lebaoth, Shilhim, Ayin, Rimmon, khopuei pakul pako neh vangca boeih he Judah ca rhoek neh amih koca kah khobawt ah aka om khopuei rhoek ni.
Lebaoti, Silihimu, Aini ndi Rimoni. Mizinda yonse inalipo 29 pamodzi ndi midzi yake yozungulira.
33 Kolrhawk ah khaw Eshtaol, Zorah, Ashnah,
Mizinda ya ku chigwa cha kumadzulo ndi iyi: Esitaoli, Zora, Asina
34 Zanoah, Engannim, Tapuah, Enam,
Zanowa, Eni-Ganimu, Tapuwa, Enamu,
35 Jarmuth, Adullam, Sokoh, Azekah,
Yarimuti, Adulamu, Soko, Azeka,
36 Shaaraim, Adithaim, Grderah, Gederothaim, khopuei hlai li neh amih kah vangca rhoek.
Saaraimu, Aditaimu, ndi Gederi (kapena Gederotaimu). Mizinda yonse inalipo 14 pamodzi ndi midzi yake yozungulira.
37 Zenan, Hadashad, Migdalgad,
Mizinda ina inali iyi: Zenani, Hadasa, Migidali-Gadi,
38 Dilean, Mizpeh, Joktheel,
Dileani, Mizipa, Yokiteeli,
39 Lakhish, Bozkath, Eglon,
Lakisi, Bozikati, Egiloni,
40 Kabbon, Lahmas, Kitlish,
Kaboni, Lahimasi, Kitilisi,
41 Gederoth, Bethdagon, Naamah, Makkedah, khopuei hlai rhuk neh amih kah vangca rhoek.
Gederoti, Beti-Dagoni, Naama ndi Makeda. Mizinda yonse pamodzi inalipo 16 pamodzi ndi midzi yake yozungulira.
Mizinda ina inali iyi: Libina, Eteri, Asani,
43 Jephthah, Ashnah, Nezib,
Ifita, Asina, Nezibu,
44 Keilah, Akhzib, Mareshah, khopuei pako neh amih kah vangca rhoek,
Keila, Akizibu ndi Maresa, mizinda isanu ndi inayi pamodzi ndi midzi yake.
45 Ekron, anih kah khobuel neh vangca rhoek,
Panalinso Ekroni pamodzi ndi midzi yake;
46 Ekron lamloh tuitun kah Ashdod ngoe boeih neh amih kah vangca rhoek,
komanso yonse imene inali mʼmbali mwa Asidodi ndi midzi yake kuyambira ku Ekroni mpaka ku Nyanja Yayikulu.
47 Ashdod khobuel rhoek neh a vangca rhoek. Gaza khobuel rhoek neh anih kah vangca rhoek, Egypt soklong neh tuipuei rhi kah rhi puei duela om.
Panalinso mizinda ya Asidodi ndi Gaza pamodzi ndi midzi yawo. Malire ake anafika ku mtsinje wa Igupto mpaka ku Nyanja Yayikulu.
48 Tlang kah, Shamir, Jattir, Sokoh,
Mizinda ya kumapiri inali: Samiri, Yatiri, Soko,
49 Dannah, Kiriathsannah Debir
Dana, Kiriati-Sana, (ndiye kuti Debri)
51 Goshen, Holon, Giloh, khopuei hlai khat neh amih kah vangca rhoek,
Goseni, Holoni ndi Gilo. Mizinda yonse pamodzi inali khumi ndi umodzi pamodzi ndi midzi yake.
Analandiranso mizinda iyi: Arabu, Duma, Esani,
53 Janim, Bethtappuah, Aphekah,
Yanumu, Beti-Tapuwa, Afeki
54 Humtah, Kiriatharba Hebron Zior khopuei pako neh amih kah vangca rhoek khaw om.
Humita, Kiriati-Ariba (ndiye kuti Hebroni) ndi Ziori, mizinda isanu ndi inayi pamodzi ndi midzi yake.
55 Maon Karmel, Ziph, Juttah,
Panalinso Maoni, Karimeli, Zifi, Yuta
56 Jezreel, Jokdeam, Zanoah,
Yezireeli, Yokideamu, Zanowa,
57 Kain, Geba, Timnah khopuei parha neh amih kah vangca rhoek,
Kaini, Gibeya ndi Timna, mizinda khumi ndi midzi yake.
58 Halhul, Bethzur, Gedor,
Mizinda ina inali: Halihuli, Beti Zuri, Gedori,
59 Maarath, Bethanoth, Eltekon, khopuei parhuk neh amih kah vangca rhoek,
Maarati, Beti-Anoti ndi Elitekoni, mizinda isanu ndi umodzi pamodzi ndi midzi yake
60 Kiriathbaal Kiriathjearim, Rabbah khopuei panit neh amih kah vangca rhoek,
Panalinso Kiriati Baala (ndiye kuti Kiriati Yearimu) ndi Raba; mizinda iwiri pamodzi ndi midzi yake.
61 Khosoek kah Bethkolken Middin neh Sekakah,
Mizinda ya ku chipululu inali iyi: Beti-Araba, Midini, Sekaka,
62 Nibshan, Lungkaeh khopuei, Engedi khopuei parhuk neh amih kah vangca rhoek khaw om.
Nibisani, Mzinda wa Mchere ndi Eni Gedi, mizinda isanu ndi umodzi pamodzi ndi midzi yake.
63 Tedae Jerusalem kah aka om Jebusi rhoek tah Judah ca rhoek loh a haek ham coeng rhoe la coeng pawh. Te dongah Jebusi neh Judah ca rhoek he tihnin due Jerusalem ah hmaih omuh.
Koma Yuda sanathe kuthamangitsa Ayebusi amene amakhala ku Yerusalemu, ndipo mpaka lero Ayebusi akukhala komweko pamodzi ndi Ayudawo.