< Johan 14 >

1 “Na thinko thuen sak uh boeh. Pathen te tangnah uh lamtah Kai khaw n'tangnah uh.
“Mtima wanu usavutike. Khulupirirani Mulungu; khulupirirani Inenso.
2 A pa im ah hmuen muep om. Tedae om pawt koinih a om pawt te nangmih taengah ka thui ni. Nangmih ham hmuen rhoekbah ham ka cet.
Mʼnyumba mwa Atate anga muli zipinda zambiri. Kukanakhala kuti mulibemo ndikanakuwuzani. Ine ndikupita kumeneko kukakukonzerani malo.
3 Ka cet vetih nangmih ham hmuen ka rhoekbah atah koep ka lo vetih kamah taengla nangmih kan loh ni. Te daengah ni kai ka om nah ah na om uh van eh.
Ndipo ndikapita kukakukonzerani malo, ndidzabweranso kudzakutengani, kuti kumene kuli Ineko, inunso mukakhale komweko.
4 Ka caeh nah khaw longpuei te na ming uh,” a ti nah.
Inu mukudziwa njira ya kumene Ine ndikupita.”
5 Thomas loh, “Boeipa, mela na caeh khaw ka ming uh pawh. Longpuei te metlam ka ming uh thai eh?” a ti nah.
Tomasi anati kwa Iye, “Ambuye ife sitikudziwa kumene Inu mukupita, nanga tingadziwe bwanji njirayo?”
6 Jesuh loh anih te, “Kai tah longpuei, oltak neh hingnah la ka om. Kai lamkah pawt atah pa taengla a pha moenih.”
Yesu anayankha kuti, “Ine ndine njira, choonadi ndi moyo. Palibe munthu angafike kwa Atate popanda kudzera mwa Ine.
7 “Kai nan ming uh atah a pa te khaw na ming uh. Te dongah tahae lamkah tah amah na ming uh coeng tih na hmuh uh coeng,” a ti nah.
Mukanandidziwadi Ine, mukanadziwanso Atate anga. Kuyambira tsopano, mukuwadziwa ndipo mwawaona.”
8 Philip loh, “Boeipa, Pa te kaimih nan tueng atah kaimih ham rhoeh coeng,” a ti nah.
Filipo anati, “Ambuye, tionetseni Atatewo ndipo ife tikhutitsidwa.”
9 Jesuh loh, “Philip nangmih taengah kum he yet ka om dae kai nan ming pawt nim? Kai aka hmu loh pa te a hmuh coeng. Balae tih, ‘Pa te kaimih n'tueng lah,’ na ti mai?
Yesu anayankha kuti, “Kodi iwe Filipo, ndakhala pakati panu nthawi yonseyi ndipo iwe sukundidziwabe? Aliyense amene waona Ine, waonanso Atate. Tsono ukunena bwanji kuti, ‘Tionetseni Atate?’
10 Pa dongah ka om tih kai dongah pa om tila nan tangnah moenih a? Kai loh nangmih taengah olka ka thui te kamah lamkah ka thui moenih. Tedae kai ah aka om a pa loh amah bi te a saii.
Kodi sukukhulupirira kuti Ine ndili mwa Atate, ndipo Atate ali mwa Ine? Mawu amene Ine ndiyankhula kwa inu si mawu anga okha koma ndi mawu Atate wokhala mwa Ine, amene akugwira ntchito yake.
11 Pa ah ka om tih kai ah a pa a om te kai n'tangnah uh. Te pawt atah a bibi nen te tangnah uh.”
Khulupirirani Ine pamene ndi kuti Ine ndili mwa Atate ndipo Atate ali mwa Ine. Koma ngati si chomwecho, khulupiriranitu Ine chifukwa cha ntchito zanga zodabwitsa.
12 “Nangmih taengah rhep rhep ka thui kai pa taengla ka caeh ham coeng dongah kai aka tangnah loh kai kah bi saii te a saii vetih hekah lakah a len la a saii ni.
Zoonadi, Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene akhulupirira Ine adzachita zimene Ine ndakhala ndikuchita. Iye adzachita ngakhale zinthu zazikulu kuposa zimenezi, chifukwa ndikupita kwa Atate.
13 Kai ming neh na bih carhui te tah han saii bitni. Te daengah ni pa tah capa dongah a thangpom eh.
Ndipo Ine ndidzachita chilichonse chimene inu mudzapempha mʼdzina langa kuti Atate alemekezedwe mwa Mwana.
14 Khat khat long ni kai ming neh kai nan hloep uh atah kai loh kan saii ni.”
Ngati mudzapempha kanthu kalikonse mʼdzina langa, Ine ndidzachita.
15 “Kai nan lungnah uh atah kai kah olpaek te na tuem uh ni.
“Ngati mundikonda Ine, sungani malamulo anga.
16 Kai khaw pa taengah ka bih vetih nangmih taengah kumhal ah aka om ham a tloe baerhoep te nangmih m'paek ni. (aiōn g165)
Ine ndidzapempha Atate, ndipo adzakupatsani Nkhoswe ina kuti izikhala nanu nthawi zonse. (aiōn g165)
17 Oltak Mueihla te diklai loh so pawt tih a ming pawt dongah doe thai pawh. Tedae anih te nangmih taengah naeh tih nangmih khuiah a om ham dongah na ming uh.
Nkhosweyo ndiye Mzimu wachoonadi. Dziko lapansi silingalandire Nkhosweyi chifukwa samuona kapena kumudziwa. Koma inu mumamudziwa pakuti amakhala nanu ndipo adzakhala mwa inu.
18 Nangmih taengla ka pawk coeng dongah cadah la nangmih kan hnoo mahpawh.”
Ine sindikusiyani nokha kuti mukhale ana amasiye. Ine ndidzabweranso kwa inu.
19 “Kolkalh ah diklai loh kai m'hmuh mahpawh. Tedae nangmih loh kai nan hmuh uh. Kai ka hing dongah nangmih khaw na hing uh ni.
Patsala nthawi yochepa dziko lapansi silidzandionanso koma inu mudzandiona. Popeza kuti Ine ndili ndi moyo, inunso mudzakhala ndi moyo.
20 Tekah khohnin ah a pa dongah kai ka om tih nangmih khaw kai dongah, kai khaw nangmih dongah ka om te na ming uh ni.
Tsiku limenelo inu mudzazindikira kuti Ine ndili mwa Atate, ndipo inu muli mwa Ine, ndipo Ine ndili mwa inu.
21 Ka olpaek aka dang tih aka tuem tah kai aka lungnah la om. Te dongah kai aka lungnah tah a pa loh a lungnah ni. Kai long khaw anih ka lungnah vetih a taengah ka phoe ni,” a ti nah.
Iye amene amadziwa malamulo anga ndi kuwasunga ndiye amene amandikonda. Wokonda Ine adzakondedwa ndi Atate wanga ndipo Inenso ndidzamukonda ndikudzionetsa ndekha kwa iye.”
22 Judas [Iskariot moenih] loh, “Boeipa, kaimih taengah nang na phoe vetih diklai taengah na phoe pawt ham na cai te metlam a om?” a ti nah.
Kenaka Yudasi (osati Yudasi Isikarioti) anati, “Koma Ambuye, nʼchifukwa chiyani mukufuna kudzionetsa nokha kwa ife, osati ku dziko lapansi?”
23 Jesuh loh anih te a doo tih, “Khat khat long ni kai n'lungnah atah kai olka te a tuem ni. Anih te a pa loh a lungnah ni. Te vaengah amah taengla m'pha uh vetih anih taengah hmuen n'saii uh ni.
Yesu anamuyankha kuti, “Ngati wina aliyense andikonda Ine, adzasunga mawu anga. Atate wanga adzamukonda, ndipo Ife tidzabwera ndi kukhala naye.
24 Kai aka lungnah pawt loh kai ol te kuem pawh. Te dongah olka na yaak uh te kai kah olka la om pawt tih kai aka tueih a pa kah olka ni.
Iye amene sandikonda Ine sasunga mawu anga. Mawu awa amene mukumva si anga ndi a Atate amene anandituma Ine.
25 He rhoek he nangmih taengah ka om vaengah ka thui coeng.
“Ndayankhula zonsezi ndikanali nanu.
26 Tedae kai ming rhangneh a pa loh Mueihla cim te baerhoep la han tueih ni. Anih loh a cungkuem ah nangmih te n'thuituen vetih kai loh nangmih taengah ka thui boeih te nangmih n'thoelh sak ni.”
Koma Nkhosweyo, Mzimu Woyera, amene Atate adzamutumiza mʼdzina langa adzakuphunzitsani zinthu zonse, ndipo adzakukumbutsani zonse zimene ndinakuwuzani.
27 “Ngaimongnah nangmih taengah kan hlah. Ka ngaimongnah te nangmih kan paek. Kai loh nangmih kan paek he diklai loh a paek bang moenih. Nangmih thinko te thuen sak boeh, rhalyawp uh boeh.
Ine ndikukusiyirani mtendere. Ndikukupatsani mtendere wanga. Ine sindikukupatsani monga dziko lapansi limaperekera. Mtima wanu usavutike ndipo musachite mantha.
28 Nangmih ham ka thui te na yaak uh coeng. Ka cet vetih nangmih taengla koep ka pawk ni. Kai nan lungnah uh koinih pa taengla ka caeh te na omngaih pawn ko. Pa tah kai lakah tanglue la om ta.
“Inu munamva Ine ndikunena kuti, ‘Ine ndikupita ndipo ndidzabweranso kwa inu.’ Mukanandikonda, mukanasangalala kuti Ine ndikupita kwa Atate, pakuti Atate ndi wamkulu kuposa Ine.
29 A om hlankah nangmih ham ka thui coeng he. Te daengah ni a om vaengah na tangnah eh.
Ine ndakuwuzani tsopano zisanachitike, kuti zikadzachitika mudzakhulupirire.
30 Diklai boei tah ha pawk coeng dongah nangmih taengah muep ka cal mahpawh. Tedae kai soah saithainah a khueh loengloeng moenih.
Ine sindiyankhulanso nanu zambiri nthawi yayitali popeza wolamulira dziko lapansi akubwera. Iye alibe mphamvu pa Ine,
31 Tedae a pa ka lungnah te diklai loh ming kolo saeh. Pa loh n'uen bangla ka saii van coeng. Thoo uh, he lamkah khoe uh sih,” a ti nah.
koma kuti dziko lapansi lizindikire kuti Ine ndimakonda Atate ndi kuti ndimachita zokhazokha zimene Atate wandilamulira Ine. “Nyamukani; tizipita.”

< Johan 14 >