< Joba 30 >

1 Tedae a kum la kai lakah aka noe long khaw kai taengah luem uh coeng. Te rhoek kah a napa pataeng ka boiva kah ui taengah khueh ham ka hnawt lah mako.
“Koma tsopano akundinyoza, ana angʼonoangʼono kwa ine, anthu amene makolo awo sindikanawalola kuti azithandizana ndi agalu anga kuweta nkhosa zanga.
2 Amih kut dongkah thadueng khaw kai taengah metlam a om? Amih te a hminkhah lamni a paltham.
Kodi mphamvu zawo ndi za phindu lanji kwa ine, pakuti mphamvu zawo zinatha kale?
3 Vaitahnah neh khokha rhamling lamkah pumhong loh hlaem vaengah khohaeng neh imrhong kah rhamrhae te a cilh.
Anali atatheratu kuwonda ndi njala, ankayendayenda mʼdziko lopanda madzi, mʼchipululu usiku.
4 Tangpuem dongkah baekkoi te a hlaek uh tih a buh la hlingcet yung a khueh.
Ankathyola therere ndi masamba owawa, ndipo chakudya chawo chinali mizu ya mitengo ya masache.
5 A nam lamloh a haek uh tih amih taengah hlanghuen bangla a o uh.
Anapirikitsidwa pakati pa anthu anzawo, akuwakuwiza ngati kuti anali akuba.
6 Soklong cakhom kah laipi neh thaelsawk khui ah kho a sak.
Anawumirizidwa kukhala ku zigwembe za mitsinje yowuma, pakati pa matanthwe ndi mʼmaenje a mʼnthaka.
7 Tangpuem khuiah pang uh tih lota hmuiah poem uh.
Ankalira ngati nyama kuthengo ndipo ankawunjikana pamodzi pa ziyangoyango.
8 Aka ang ca rhoek neh ming mueh ca rhoek ni khohmuen lamloh a hawt uh.
Anali anthu achabechabe ndi wopanda dzina, anathamangitsidwa mʼdziko.
9 Te dongah amih kah rhotoeng la ka om coeng tih amih taengah ol la ka om.
“Ndipo tsopano ana awo akundiyimba nyimbo zachipongwe; ineyo ndasanduka chisudzo chawo.
10 Kai aka tuei rhoek tah kai lamloh lakhla uh tih ka mikhmuh ah timtui khaw tuem uh pawh.
Iwo amanyansidwa nane ndipo amandithawa; akandiona salephera kundilavulira mʼmaso mwangamu.
11 A lirhui lakah ka lirhui he pawl coeng. Te dongah kai he m'phaep tih ka mikhmuh ah kamrhui han tueih uh.
Tsopano pakuti Mulungu wakhwefula uta wanga ndipo wandisautsa, iwowo analekeratu kundiopa.
12 Ka bantang kah hlangyoe loh tlai ka kho a kalh. Amih kah rhainah caehlong te kai taengah a picai uh.
Ku dzanja langa lamanja anthu akulimbana nane; andikumbira dzenje loti ndigweremo ndikamayenda, andipangira mitumbira ya nkhondo kuti alimbane nane.
13 Ka talnah khuiah ka hawn a mak uh tih, amih aka bom pawt khaw hoeikhang uh.
Iwo anditsekera njira; akufuna kundichititsa ngozi, popanda wina aliyense wowaletsa.
14 A puut aka len bangla ael uh tih a khohli rhamrhael hmuiah paluet uh.
Akundithamangitsa ngati madzi olowera pa mpanda wobowoka, iwo akubwererabwerera pakati pa chipasupasu.
15 Kai soah mueirhih pai tih khohli bangla ka moeihoeihnah a hloem vaengah kai kah khangnah te khomai bangla a yah.
Zoopsa zandithetsa mphamvu; ulemu wanga wachita ngati wauluzika ndi mphepo, chuma changa chija chazimirira ngati mtambo.
16 Kai lamloh ka hinglu a kingling coeng tih phacip phabaem khohnin loh kai n'tuuk.
“Ndipo tsopano mtima wanga wachokamo; ndili mʼmasiku amasautso.
17 Khoyin ah ka rhuh te ka pum dong lamloh a cueh. Kai aka thuek he a dim moenih.
Mafupa anga akuphwanya usiku pakuti zowawa zanga sizikuleka.
18 Thadueng cungkuem dongah ka pueinak a phuelhthaih tih ka angkidung te rhawnmoep bangla ka vah.
Mʼmphamvu zake Mulungu wakhala ngati chovala changa; Iye wandigwira ngati chovala chondithina pa khosi.
19 Kai he dikpo khuila n'dong tih laipi neh hmaiphu bangla n'thuidoek.
Wandiponya mʼmatope, ndipo ndasanduka ngati fumbi ndi phulusa.
20 Na taengah bomnah kam bih dae kai nan doo moenih. Ka pai akhaw kai he nan yakming moenih.
“Inu Mulungu, ine ndikulirira kwa Inu, koma simukundiyankha; ndikayimirira, Inu simundiyangʼana nʼkomwe.
21 Kai soah a muen la na poeh tih na ban thaa neh kai nan konaeh thil.
Inuyo mumandichitira zankhanza; mumandizunza ndi dzanja lanu lamphamvu.
22 Kai he khohli dongah nan phueih. Kai nan ngol thil vaengah kai nan paci sak tih lungming cueihnah a yawn.
Mwandinyamulira ku mphepo ndipo mwandiwulutsa ndi mphepoyo; mwandiponya mʼmphepo ya mkuntho.
23 Mulhing boeih kah tingtunnah im la dueknah neh kai nan mael sak ham khaw ka ming.
Ndikudziwa kuti Inu mudzandifikitsa ku imfa, kumalo kumene amoyo onse adzapitako.
24 A yoethaenah khuiah bombihnah a yaak vaengah kut aka thueng he lairhok dongah a om moenih.
“Ndithudi palibe munthu amene amalanga munthu wosweka mtima, amene akupempha thandizo mʼmasautso ake.
25 Khohnin a mangkhak dongah ka rhap tih khodaeng dongah ka hinglu a omdam moenih.
Kodi ine sindinalire nawo iwo amene anali pamavuto? Kodi mtima wanga sunamvere chisoni anthu osauka?
26 A then ka lamtawn vaengah boethae ha pawk. Vangnah te ka ngaiuep vaengah a hmuep ha pai.
Koma pamene ndinkayembekezera zabwino, zoyipa ndiye zinandigwera; pamene ndinkafunafuna kuwala, mdima ndiye unandigwera.
27 Ka bung he tlawk tih a kuemsuem moenih. Kai he phacip phabaem khohnin loh n'doe.
Kuwawa kwa mʼkati mwanga sikukuleka; ndili mʼmasiku amasautso.
28 Khomik a tal dongah maelhmai a hmuep la ka cet. Hlangping neh ka pai tih ka pang.
Ndikuyenda wothimbirira, komatu osati ndi dzuwa; ndimayimirira pa msonkhano ndi kupempha chithandizo molira.
29 Pongui kah a manuca neh tuirhuk vanu kah a hui la ka om.
Ndasanduka mʼbale wa nkhandwe, mnzawo wa akadzidzi.
30 Ka vin khaw kamah dong lamloh mu tih ka rhuh khaw kholing neh tlum coeng.
Khungu langa layamba kuda ndipo likufunduka; thupi langa likutentha chifukwa cha kuphwanya kwa thupi.
31 Ka rhotoeng te nguekcoinah la, ka phavi rhah ol la poeh.
Pangwe wanga wasanduka woyimbira maliro, ndipo chitoliro changa chikuyimbira anthu olira.

< Joba 30 >