< Jeremiah 14 >
1 Khokang ol dongah BOEIPA ol he Jeremiah taengla pawk.
Awa ndi mawu amene Yehova anamuwuza Yeremiya onena za chilala:
2 Judah te nguekcoi tih a vongka khaw tahah coeng. Khohmuen ham khaw kopang uh tih Jerusalem kah henah tah luei coeng.
“Yuda akulira, mizinda yake ikuvutika; anthu ake adzigwetsa pansi mwachisoni, kulira kwa Yerusalemu kwakula.
3 Amih khuikah aka khuet rhoek loh a canoi rhoek te tui taengla a tueih uh. Tuito taengla pawk uh dae tui hmu uh pawh. A am hong neh a mael uh vaengah yak uh tih a hmaithae neh a lu a yil uh.
Anthu awo wolemekezeka akutuma antchito awo kuti akatunge madzi. Apita ku zitsime osapezako madzi. Choncho amabwerera ndi mitsuko yopanda madzi. Amanyazi ndi othedwa nzeru adziphimba kumaso.
4 Diklai ah khonal om pawt tih lai a yawk kong ah, lopho rhoek yak uh tih a lu a yil uh.
Popeza pansi pawumiratu chifukwa kulibe madzi, alimi ali ndi manyazi ndipo amphimba nkhope zawo.
5 Sayuk rhuinu long pataeng khaw lohma ah ca a cun dae baelhing a om pawt dongah a hnoo.
Ngakhale mbawala yayikazi ikusiya mwana wake wakhanda ku thengo chifukwa kulibe msipu.
6 Kohong marhang rhoek caphoei cuk ah pai uh tih pongui bangla yilh a mam. Baelhing om pawt tih a mik kha uh.
Mbidzi zikuyima pa zitunda zopanda kanthu nʼkumapuma wefuwefu ngati nkhandwe; maso awo achita chidima chifukwa chosowa msipu.”
7 Kaimih kathaesainah loh kaimih taengah n'doo uh cakhaw BOEIPA aw namah taengah ka hnuknong uh khing tih ka tholh uh dongah he na ming ham mah saii mai.
Anthu akuti, “Ngakhale machimo athu akutitsutsa, koma Inu Yehova chitanipo kanthu chifukwa cha dzina lanu. Pakuti kusakhulupirika kwathu nʼkwakukulu; ife takuchimwirani.
8 Israel kah ngaiuepnah neh citcai tue vaengah anih kah khangkung aw, balae tih diklai ah yinlai neh rhaeh hamla aka rhaehba yiin bangla na om.
Inu Yehova amene Aisraeli amakukhulupirirani ndi amene mumawapulumutsa pa nthawi ya masautso, chifukwa chiyani mukukhala ngati mlendo mʼdziko muno? Chifukwa chiyani muli ngati wapaulendo amene akungogona tsiku limodzi?
9 BOEIPA kaimih lakli ah tah namah khaw balae tih hlang ingang bangla, khang ham aka coeng pawh hlangrhalh bangla na om? Tedae kaimih taengah na ming a khue dongah kaimih nan hnoo moenih.
Chifukwa chiyani muli ngati munthu amene wadzidzimutsidwa, kapena ngati wankhondo amene alibe mphamvu yopulumutsa? Komabe Inu Yehova, muli pakati pathu, ndipo tikudziwika ndi dzina lanu; musatitaye ife!”
10 BOEIPA loh he pilnam ham he ni a. thui. Amih kho tah poengdoe ham a lungnah uh tangloeng tih tuemsoem uh pawh. BOEIPA loh amih a moeithen pawt dongah amih kathaesainah te a poek vetih a tholhnah te a cawh pawn ni.
Zimene Yehova akunena za anthuwa ndi izi: “Iwo amakonda kuyendayenda kwambiri; samatha kudziretsa. Nʼchifukwa chake Ine Yehova sindingawalandire, ndipo tsopano ndidzakumbukira zoyipa zawo ndi kuwalanga chifukwa cha machimo awo.”
11 Tedae BOEIPA loh kai taengah, “Hnothen ham akhaw he pilnam ham tah thangthui boeh.
Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Usawapempherere anthu awa kuti zinthu ziwayendere bwino.
12 A yaeh uh vaengkah a tamlung te ka hnatun moenih. Hmueihhlutnah neh khocang a khuen uh vaengah amih te ka moeithen moenih. Tedae amih te cunghang neh, khokha neh, duektahaw neh ka khah,” a ti.
Ngakhale asale zakudya, Ine sindidzamva kulira kwawo; ngakhale apereke nsembe zopsereza ndi chopereka cha chakudya, sindidzazilandira. Mʼmalo mwake, ndidzawapha ndi lupanga, njala ndi mliri.”
13 Tedae, “Ya-oe, ka Boeipa Yahovah, amih taengah cunghang na hmu pawt vetih nangmih taengah khokha pai mahpawh, he hmuen ah nangmih ham ngaimongnah oltak kam paek ni, ' aka ti tonghma aih ke,” ka ti nah.
Koma ine ndinati, “Aa, Ambuye Yehova, aneneri amawawuza anthuwo kuti, sadzaphedwa ndi lupanga kapena kuvutika ndi njala. Koma kuti Inu mudzawapatsa mtendere wokhawokha pamalo pano.”
14 Te dongah BOEIPA loh kamah taengah, “Laithae tonghma rhoek loh ka ming neh tonghma uh. Amih te ka tueih pawt tih amih te ka uen moenih. Laithae mangthui neh olhong bihma, a huep mueirhol, amih te ka thui pah moenih. Tedae amih loh amamih lungbuei kah a huep nen ni nangmih taengah a tonghma uh,” a ti.
Ndipo Yehova anandiwuza kuti, “Ndi zabodza kuti aneneriwa akunenera mʼdzina langa. Ine sindinawatume kapena kuwasankha kapenanso kuyankhula nawo. Iwo amakuwuzani zinthu zabodza zomwe amati anaziona mʼmasomphenya, kapena pogwiritsa ntchito mawula achabechabe. Zimene amayankhula ndi zongopeka mʼmutu mwawo.
15 Te dongah BOEIPA loh he ni a. thui. Ka ming neh aka tonghma, tonghma rhoek, amih te ka tueih moenih. Tedae amih loh, 'He diklai ah cunghang neh khokha om mahpawh,’ a ti uh. Tekah tonghma rhoek tah cunghang neh, khokha neh cung bitni.
Nʼchifukwa chake Ine Yehova ndikuti aneneri amenewa akulosera mʼdzina langa pamene Ine sindinawatume. Iwo amati simudzafa pa nkhondo kapena ndi njala mʼdziko muno. Koma tsono ndi iwowo, aneneriwa amene adzafe pa nkhondo kapena ndi njala.
16 Pilnam loh amih taengah aka tonghma rhoek Jerusalem vongvoel kah a voeih rhoek la om uh ni. Khokha neh cunghang dongah amih te aka up khaw om mahpawh. Amih te a yuu rhoek khaw, a capa rhoek khaw, a canu rhoek te khaw amamih kah boethae te amamih soah ka lun ni.
Ndipo anthu amene anawaloserawo adzaponyedwa mʼmisewu ya mu Yerusalemu atafa ndi njala ndi lupanga. Sipadzapezeka wowayika mʼmanda popeza iwowo, akazi awo, ana awo aamuna, onse adzakhala atafa. Ine ndidzawagwetsera chilango chowayenera.
17 He ol he amih taengah thui pah. Ka mik dongkah mikphi he khoyin khothaih suntla saeh lamtah kak boel saeh. Ka pilnam tanu oila tah, hma puei dongah khaem coeng tih hmasoe la nue khungdaeng coeng.
“Awuze mawu awa: “‘Maso anga akugwetsa misozi kosalekeza usana ndi usiku; chifukwa anthu anga okondedwa apwetekeka kwambiri, akanthidwa kwambiri.
18 Khohmuen te ka paan vaengah nim cunghang dongkah rhok hoeng ni ke. Khopuei la ka caeh bal nim te khokha kah tlohtat hoeng ni ke. Tonghma neh khosoih loh diklai ah a thimpom rhoi akhaw a ming rhoi moenih.
Ndikapita kuthengo, ndikuona amene aphedwa ndi lupanga; ndikapita mu mzinda, ndikuona amene asakazidwa ndi njala. Ngakhale aneneri pamodzi ndi ansembe onse atengedwa.’”
19 Judah te na hnawt na hnawt tih Zion te na hinglu loh a tuei nama? Balae tih kaimih taengah hoeihnah om pawt ham kaimih nan ngawn? Sadingnah te lamtawn dae then voel pawh. Te dongah hoeihnah tue te khaw letnah coeng ni he.
Kodi anthu a ku Yuda mwawakana kwathunthu? Kodi mtima wanu wanyansidwa nawo anthu a ku Ziyoni? Chifukwa chiyani mwatikantha chotere kuti sitingathenso kuchira? Ife tinayembekezera mtendere koma palibe chabwino chomwe chabwera, tinayembekezera kuchira koma panali kuopsezedwa kokhakokha.
20 BOEIPA aw kaimih kah halangnah neh a pa rhoek kathaesainah neh namah taengah ka tholh uh te ka ming uh.
Inu Yehova, ife tikuvomereza kuyipa kwathu ndiponso kulakwa kwa makolo athu; ndithu ife tinakuchimwiranidi.
21 Na ming ham tah tlaitlaek boeh, na thangpomnah ngolkhoel te tahah sak boeh. Poek van lah, kaimih taengkah na paipi te phae boeh.
Musatikane kuopa kuti dzina lanu linganyozedwe; musanyoze mpando wanu waufumu waulemerero. Kumbukirani pangano lanu ndi ife ndipo musachiphwanye.
22 Namtom kah a honghi taengah kho nal om tih vaan long khaw mueitui a paek nim? Kaimih kah BOEIPA Pathen amah khaw nang moenih a? Te dongah nang soah kan lamtawn uh tih he boeih he namah ham ni na saii.
Mwa milungu yachabechabe ya anthu a mitundu ina, kodi pali mulungu amene angagwetse mvula? Ife chikhulupiriro chathu chili pa Inu, popeza Inu nokha ndinu Yehova Mulungu wathu amene mukhoza kuchita zimenezi.