< Isaiah 63 >

1 Bozrah himbai a thimduk neh Edom lamkah aka pawk he nim? A pueinak nen mah a hiin coeng. Amah kah thadueng cungkuem neh aka khuum mai te. Khang khungdaeng ham khaw kamah long ni duengnah neh ka thui.
Kodi ndani uyo akubwera kuchokera ku Edomu, atavala zovala za ku Bozira za madontho ofiira? Kodi uyu ndani, amene wavala zovala zokongola, akuyenda mwa mphamvu zake? “Ndi Ineyo, woyankhula zachilungamo ndiponso wamphamvu zopulumutsa.”
2 Balae tih na pueinak te a thim? Na himbai khaw misur rhom khuiah a nook bangla.
Nanga bwanji zovala zanu zili psuu, ngati za munthu wofinya mphesa?
3 Sum khaw kamah bueng long ni ka huelh. Pilnam pakhat khaw kai taengah nuen pawh. Ka thintoek ah amih a neet tih ka kosi neh amih ka taelh. A thii loh ka himbai a haeh tih ka hnicu he a pum la ka nok.
“Ndapondereza ndekha anthu a mitundu ina ngati mphesa, palibe ndi mmodzi yemwe anali nane. Ndinawapondereza ndili wokwiya ndipo ndinawapondereza ndili ndi ukali; magazi awo anadothera pa zovala zanga, ndipo zovala zanga zonse zinathimbirira.
4 Phulohnah hnin ham te ka lungbuei ah hing cakhaw kai ham tlannah kum ha pai coeng.
Pakuti ndinatsimikiza mu mtima mwanga kuti lafika tsiku lolipsira anthu anga; ndipo chaka cha kuwomboledwa kwanga chafika.
5 Ka paelki van akhaw aka bom om pawh. Ka pong bal akhaw aka talong om pawh. Ka bantha loh kamah ham a khang tih ka kosi loh amah la kai n'duel.
Ndinayangʼana ndipo panalibe munthu wondithandiza. Ndinadabwa kwambiri kuti panalibe wondichirikiza; choncho ndinapambana ndi mphamvu zanga, ndipo mkwiyo wanga unandilimbitsa.
6 Ka thintoek ah pilnam ka suntlae tih ka kosi neh amih ka rhuihmil sak. Amih thii te diklai dongah ka tlak sak.
Ndinapondereza mitundu ya anthu ndili wokwiya; ndipo ndinawasakaza ndipo ndinathira magazi awo pansi.”
7 BOEIPA loh mamih ham boeih a thuung van bangla BOEIPA kah sitlohnah neh BOEIPA koehnah ni ka thui eh. Amih kah haidamnah bangla amah kah sitlohnah cangpai neh Israel imkhui te thennah neh muep a thuung.
Ndidzafotokoza za kukoma mtima kwa Yehova, ntchito zimene Iye ayenera kutamandidwa. Ndidzatamanda Yehova chifukwa cha zonse zimene watichitira. Inde, mwa chifundo ndi kukoma mtima kwake Yehova wachitira nyumba ya Israeli zinthu zabwino zambiri.
8 “Amih ka pilnam he tah camoe khaw rhilat mahpawh,” a ti coeng dongah BOEIPA tah amih aka khang la om coeng.
Yehova anati, “Ndithu awa ndi anthu anga, ana anga amene sadzandinyenga Ine.” Choncho anawapulumutsa.
9 Amih kah citcai boeih dongah BOEIPAamah ham khaw khobing sut. A mikhmuh kah puencawn loh amih te a khang. A lungnah neh a thinphatnah dongah amih te a tlan. Khosuen lamkah hnin takuem amih te a poeh tih amih te a ludoeng.
Iyenso anasautsidwa mʼmasautso awo onse, ndipo mngelo wochokera kwa Iye anawapulumutsa. Mwa chikondi ndi chifundo chake iye anawapulumutsa, anawanyamula ndikuwatenga kuyambira kale lomwe.
10 Tedae amih loh amah kah Mueihla cim te a koek tih kothae a paekuh. Te dongah amih taengla mael tih thunkha bangla amih te amah loh a vathoh thil.
Komabe iwo anawukira ndi kumvetsa chisoni Mzimu Woyera. Motero Yehova anatembenuka nakhala mdani wawo ndipo Iye mwini anamenyana nawo.
11 Khosuen tue kah a pilnam Moses a thoelh. Amih te a boiva aka dawn neh tuipuei lamloh aka khuen te melae? A kotak ah a Mueihla Cim te aka khueh te melae?
Pamenepo anthu ake anakumbukira masiku amakedzana, masiku a Mose mtumiki wake; ndipo anafunsa kuti, “Ali kuti Yehova amene anawawolotsa pa nyanja, pamodzi ndi Mose mʼbusa wawo? Ali kuti Iye amene anayika Mzimu Woyera pakati pawo?
12 Amah kah boeimang bantha te Moses bantang ah aka pongpa sak, amah kah kumhal ming dang sak ham amih mikhmuh lamkah tui aka phih.
Ali kuti amene anachita zinthu zodabwitsa ndi mphamvu zake zazikulu kudzera mwa Mose? Ali kuti amene anagawa madzi pa nyanja anthu ake akuona, kuti dzina lake limveke mpaka muyaya,
13 Amih te khosoek ah marhang bangla tuidung longah a mawt dae paloe uh pawh.
amene anawayendetsa pa nyanja yozama? Monga kavalo woyendayenda mʼchipululu, iwo sanapunthwe;
14 Kolbawn la aka suntla rhamsa bangla BOEIPA Mueihla loh anih a duem sak. Boeimang ming te namah hut la khueh ham ni na pilnam khaw na hmaithawn tangloeng.
Mzimu Woyera unawapumulitsa ngati mmene ngʼombe zimapumulira. Umu ndi mmene Inu munatsogolera anthu anu kuti dzina lanu lilemekezeke.”
15 Vaan lamloh paelki lamtah na imhmuen cim lamloh hmuh lah. Na boeimang neh na thatlainah na thayung thamal melae? Na ko a hah neh na haidamnah he kai taengah thiim uh.
Inu Yehova amene muli kumwambako, pa mpando wanu wolemekezeka, wopatulika ndi waulemerero, tiyangʼaneni ife. Kodi changu chanu ndi mphamvu zanu zili kuti? Simukutionetsanso kukoma mtima kwanu ndi chifundo chanu.
16 Kaimih napa tah namah pai ni. Abraham loh kaimih m'ming moenih. Israel long khaw kaimih m'hmat moenih. Kaimih napa he Yahovah namah ni. Khosuen lamloh kaimih aka tlan khaw namah ming ni.
Koma Inu ndinu Atate athu, ngakhale Abrahamu satidziwa kapena Israeli kutivomereza ife; Inu Yehova, ndinu Atate athu, kuyambira kale dzina lanu ndinu Mpulumutsi wathu.
17 BOEIPA aw balae tih na longpuei lamloh kaimih kho nan hmang sak. Namah hinyahnah lamloh kaimih lungbuei na hit sak. Na rho koca na sal rhoek ham ha mael laeh.
Chifukwa chiyani, Inu Yehova, mukutisocheretsa pa njira zanu? Bwanji mukutilola kuti tikhale owuma mitima kotero kuti sitikukuopaninso? Bwererani chifukwa cha atumiki anu; mafuko a anthu amene ali cholowa chanu.
18 Namah kah pilnam cim kolkalh a pang uh vaengah kaimih kah rhal rhoek loh na rhokso te a suntlae uh.
Anthu anu atangokhala pa malo anu opatulika pa kanthawi kochepa, adani athu anasakaza malo anu opatulika.
19 Khosuen lamkah ka om uh coeng dae amih soah na taemrhai pawt dongah amih taengah na ming te khue van pawh. Vaan ke na phen koinih na mikhmuh ah na suntlak sak vetih tlang rhoek khaw moelh uh sue.
Ife tili ngati anthu amene simunawalamulirepo ngati iwo amene sanakhalepo anthu anu.

< Isaiah 63 >