< Isaiah 32 >
1 Manghai tah duengnah neh manghai vetih mangpa rhoek loh a tiktam la boei uh ni.
Taonani, kudzakhala mfumu ina imene idzalamulira mwachilungamo, ndipo akalonga ake adzaweruza molungama.
2 Te vaengah tah khohli vaengkah congket conglong neh hlipuei vaengkah a huephael bangla, rhamrhae kah sokca tui bangla, buhmueh rhathih khohmuen kah thaelpang puei kah hlipkhup bangla boeih om ni.
Munthu aliyense adzakhala ngati pothawirapo mphepo ndi malo obisalirapo namondwe, adzakhala ngati mitsinje ya mʼchipululu, ngati mthunzi wa thanthwe lalikulu la mʼdziko lowuma.
3 Aka hmu rhoek loh a mik buem uh voel pawt vetih aka ya kah a hna long khaw hnatung uh pawn ni.
Ndipo maso a anthu openya sadzakhalanso otseka, ndipo makutu a anthu akumva adzamvetsetsa.
4 Thinko aka loe long khaw ming hamla a yakming ni. Ol khol khaw a loe la puk cal ni.
Anthu a mtima wopupuluma adzadziwa ndi kuchita zinthu mofatsa, ndipo anthu ovutika kuyankhula adzayankhula mosadodoma ndi momveka.
5 Hlang ang te hlangcong la khue voel pawt vetih ngukngak te hlang rhoeikhang ti nah mahpawh.
Chitsiru sichidzatchedwanso munthu waulemu wake ndipo munthu woyipa sadzalemekezedwa.
6 Lailak la saii ham neh BOEIPA te rholrhaknah thui ham, akaang loh boethaehalang a thui tih a lungbuei kah boethae a saii. Hlang kah hinglu te bungpong la a kaeng tih tuihalh khaw tui-ok loh a vaitah sak.
Pakuti munthu opusa amayankhula zauchitsiru, amaganiza kuchita zoyipa: Iye amachita zoyipira Mulungu, ndipo amafalitsa zolakwika zokhudza Yehova; anjala sawapatsa chakudya ndipo aludzu sawapatsa madzi.
7 Ngukngak loh a boethae hnopai te khonuen rhamtat la a khueh tih, khodaeng loh tiktam a thui vaengah pataeng kodo mangdaeng te a honghi ol neh vueinan hamla caai.
Munthu woyipa njira zake ndi zoyipanso, iye kwake nʼkulingalira zinthu zoyipa. Amalingalira zakuti awononge anthu aumphawi ndi mabodza ake ngakhale kuti waumphawiyo akuyankhula zoona.
8 Tedae hlangcong long tah moeihoeihnah neh a uen tih moeihoeihnah neh pai van.
Koma munthu wolemekezeka amalingaliranso kuchita zinthu zabwino, Iye amakhazikika pa zinthu zabwinozo.
9 Mongkawt nu rhoek thoo uh lamtah ka ol hnatun uh. Palyal tanu rhoek ka olthui he hnakaeng uh lah.
Khalani maso, inu akazi amene mukungokhala wopanda kulingalira kuti kunja kulinji ndipo imvani mawu anga. Inu akazi odzitama, imvani zimene ndikunena!
10 Palyal rhoek te kum at hnin at ah na tlai uh bitni. Misurbit loh n'khah vetih cangah khaw pha mahpawh.
Pakapita chaka ndi masiku pangʼono inu akazi amatama mudzanjenjemera; chifukwa mitengo ya mphesa idzakanika ndipo zipatso sizidzaoneka.
11 Mongkawt nu te lakueng saeh, palyal nu rhoek khaw tlai uh saeh. Hni te pit saeh lamtah a yal la a pumpu te vah saeh.
Nthunthumirani inu okhala mosatekesekanu; ndipo njenjemerani, inu akazi omadzikhulupirira nokhanu. Vulani zovala zanu, ndipo valani ziguduli mʼchiwuno mwanu.
12 Naidoeh lohma ham neh misur thaihsu ham te rhangsuk mah rhaengsae laeh.
Dzigugudeni pachifuwa mwachisoni chifukwa minda yachonde, ndi mphesa yawonongeka.
13 Hling neh lota he ka pilnam kah hmuenlung ham a yam pah coeng tih, khorha kah omthennah dongah aka yalpo imkhui boeih ham pai ni.
Mʼdziko la anthu anga mwamera minga ndi mkandankhuku. Zoona, mulilire nyumba zonse zachikondwerero ndi mzinda uno umene unali wachisangalalo.
14 Impuei te a phap vetih khopuei a lilup khaw a hnoo ni. Molpuei neh rhaltawt imsang te kohong marhang kah a omthennah neh tuping uemnah la poeh vetih kumhal due lungtokhui la om ni.
Nyumba yaufumu idzasiyidwa, mzinda waphokoso udzakhala wopanda anthu; malinga ndi nsanja zidzasanduka chipululu mpaka muyaya. Abulu adzasangalalamo ndipo ziweto zidzapezamo msipu.
15 Hmuensang lamkah Mueihla te mamih soah han kingling vaengah tah khosoek khaw cangphil cangngol la poeh tih khoham cangphil cangngol bangla a poek.
Yehova adzatipatsa mzimu wake, ndipo dziko lachipululu lidzasanduka munda wachonde, ndipo munda wachonde udzakhala ngati nkhalango.
16 Te vaengah tah khosoek ah tiktamnah loh kho a sak vetih, duengnah loh cangphil cangngol te a om thil ni.
Tsono mʼchipululu mudzakhala chiweruzo cholungama ndipo mʼminda yachonde mudzakhala chilungamo.
17 Duengnah kah a khoboe tah rhoepnah la, duengnah kah thohtatnah tah kumhal due mong vetih ngaikhuek la om ni.
Mtendere udzakhala chipatso chachilungamo; zotsatira za chilungamo zidzakhala bata ndi kudzidalira mpaka muyaya.
18 Ka pilnam long tah rhoepnah tolkhoeng neh pangtungnah tolhmuen ah duemnah neh a mongkawt la kho a sak ni.
Anthu anga adzakhala mʼmidzi yamtendere, mʼnyumba zodalirika, ndi malo osatekeseka a mpumulo.
19 Te dongah duup khaw rhael aka bo loh a hnaa vetih khopuei khaw tlarhoelnah la kunyun ni.
Ngakhale nkhalango idzawonongedwa ndi matalala ndipo mzinda udzagwetsedwa mpaka pansi,
20 Te dae tui kaeng te boeih aka tawn tih vaito neh laak kho neh aka tluek rhoek tah na yoethen uh.
inutu mudzakhala odalitsika ndithu. Mudzadzala mbewu zanu mʼmbali mwa mtsinje uliwonse, ndipo ngʼombe zanu ndi abulu anu zidzadya paliponse.