< Olrhaepnah 13 >

1 Nang taengah tonghma neh mang aka man te ha poe tih miknoek neh kopoekrhai khaw nang taengah m'paek mai ni.
Ngati mneneri kapena wina aliyense amene amanena zamʼtsogolo mwa maloto atuluka pakati panu, nalengeza za chizindikiro chozizwitsa kapena chodabwitsa,
2 Tedae miknoek neh kopoekrhai te hang khuen tih nang ham a thui vaengah, “Na ming noek pawh pathen tloe hnukah vai uh sih lamtah amih taengah thothueng uh sih,” a ti ni.
chinthu nʼkuchitikadi, tsono iyeyo nʼkunena kuti, “Tiyeni titsatire milungu ina, tiyeni tiyipembedze,” (kunena milungu imene simunayidziwe),
3 Tonghma te khaw, mang aka man khaw a ol hnatun pah boeh. Na ming uh ham tah nangmih loh BOEIPA na Pathen aka noemcai rhung la na om uh ve. BOEIPA na Pathen te na thinko boeih na hinglu boeih neh lungnah lah.
musamumvere mneneriyo kapena wolotayo. Yehova Mulungu wanu afuna akuyeseni kuti aone ngati mumamukonda ndi mtima wanu wonse ndi moyo wanu wonse.
4 BOEIPA na Pathen hnuk te vai lamtah amah te rhih lah. A olpaek te ngaithuen lamtah a ol te hnatun lah. Amah taengah thothueng lamtah amah dongah hangdang lah.
Muyenera kutsatira Yehova Mulungu wanu, ndipo ndi Iyeyo amene muyenera kumuopa. Muzisunga malamulo ake ndi kumamumvera, muzimutumikira ndipo kumukangamira Iyeyo.
5 A khuiah pongpa ham na Pathen BOEIPA loh nang n'uen longpuei lamloh nangmih heh hamla, Egypt khohmuen lamloh nangmih aka khuen, sal imkhui lamloh nang aka lat, nangmih kah Pathen BOEIPA taengah koeknah aka thui tah, tonghma khaw, mang aka man khaw, duek saeh. Te dongah boethae te na khui lamloh khoe.
Mneneri kapena wolotayo ayenera kuphedwa, popeza analalikira zopandukira Yehova Mulungu wanu, amene anakutulutsani ku Igupto ndi kukupulumutsani ku dziko la ukapolo. Wolalikirayo anafuna kukupatutsani pa njira imene Yehova Mulungu wanu anakulamulirani kuti muyitsatire. Muzichotsa choyipa pakati panu.
6 Na nu pakhat kah a ca na manuca long khaw, na capa long khaw, na canu long khaw, na rhang dongkah na yuu long khaw, namah hinglu bangla na lungnah na hui mai long khaw yinhnuk ah nang m'vueh tih, “Cet uh sih lamtah namah neh na pa rhoek loh a ming mueh a tloe pathen,
Ngati mʼbale wanu weniweni kapena mwana wanu wamwamuna kapena wamkazi, kapena mkazi wanu wokondedwa, kapena mnzanu wapamtima akukakamizani mwachinsinsi, nʼkumati, “Tiyeni tipite tikapembedze milungu ina” (milungu imene inuyo kapena makolo anu sanayidziwe,
7 na kaepvai kah pilnam rhoek neh khohla khoyoei, kho bawt lamkah kho bawt patoeng loh a bawk pathen te thothueng uh sih,” a ti mai ni.
milungu ya anthu okuzungulirani, kaya ndi apafupi kapena akutali, kuchokera kumapeto mpaka kumapeto kwina kwa dziko lapansi),
8 Anih taengla bung boel lamtah a ol te hnatun pah boeh. Na mik long khaw anih te rhen boel saeh. Te dongah lungma ti boel lamtah anih te dah boeh.
musamugonjere kapena kumumvera. Musamumvere chisoni. Musamuleke kapena kumutchinjiriza.
9 Anih te na ngawn rhoe na ngawn ni. Na kut te anih ngawn ham lamhma kah bangla anih soah om saeh. Hmailong ah pilnam boeih kah a kut khaw om saeh.
Mumuphe ndithu. Dzanja lanu likhale loyambirira kumupha, kenaka manja a anthu ena onse.
10 Egypt kho neh sal imkhui lamkah nang aka khuen BOEIPA na Pathen taeng lamloh heh hamla nang aka mae te lungto neh dae lamtah duek saeh.
Mumuponye miyala mpaka kumupha, chifukwa anafuna kukupatutsani pa njira ya Yehova Mulungu amene anakutulutsani ku Igupto, dziko la ukapolo.
11 Te daengah ni Israel pum loh a yaak uh vaengah a rhih uh vetih nangmih taengah hebang hno thae saii hamla a khoep pawt eh.
Tsono Aisraeli onse adzamva nachita mantha, ndipo palibe mmodzi pakati panu amene adzachitenso choyipa chotere.
12 Na khopuei khuikah hlang khat khat loh, “Teah khosak sak ham BOEIPA na Pathen loh nang m'paek coeng,” a ti vaengah,
Ngati mumvetsedwa kuti ku umodzi mwa mizinda imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani kuti mukhalemo,
13 namah khui lamkah hlang muen ca rhoek neh khopuei kah khosa rhoek aka heh loh thoo uh tih, “Cet uh sih lamtah na ming noek pawh pathen tloe taengah thothueng uh sih,” a ti uh te na yaak atah,
kwapezeka anthu ena oyipa pakati panu ndipo asocheretsa anthu ambiri mʼmizinda yanu, pomanena kuti, “Tiyeni tikapembedze milungu ina” (milungu imene simunayidziwe),
14 Na cae vetih na khe ni. Tuektuek na dawt tih na khui ah tueilaehkoi hno a saii te oltak la a om atah,
mukuyenera kufunsa, kulondola ndi kufufuza bwino nkhaniyo. Ndipo ngati zitatsimikizikadi kuti ndi zoona kuti chinthu chonyansa chotere chachitikadi pakati panu,
15 Khopuei kah khosa boeih te na ngawn rhoe na ngawn ni. Te te cunghang ha neh thup lamtah a khuikah boeih neh a rhamsa khaw cunghang ha neh thup pah.
muyenera kuwapha onse okhala mu mzinda umenewo. Muwonongeretu kwathunthu mzindawo, anthu ake ndi ziweto zake zomwe.
16 A kutbuem boeih te a toltung khui la coi pah lamtah hmai neh hoeh pah. Khopuei neh a kutbuem boeih na BOEIPA Pathen ham boeih saeh. Te vaengah a khopuei te kumhal due imrhong la om saeh lamtah thoh voel boel saeh.
Katundu yense wa anthu mu mzindawo mumuwunjike pamodzi pakatikati pa bwalo losonkhanako ndipo mutenthe mzindawo pamodzi ndi katundu wake yense monga nsembe yathunthu yopsereza ya kwa Yehova Mulungu wanu. Mzinda umenewo ukhale bwinja mpaka muyaya, usadzamangidwenso.
17 Yaehtaboeih la aka om boeih tah na kut dongah kap boel saeh. Te daengah ni BOEIPA loh thintoek thinsa khui lamkah mael vetih nang taengah haidamnah a khueh eh. Te vaengah nang n'haidam vetih na pa rhoek taengkah a toemngam vanbangla na ping van ni.
Musapezeke ndi kanthu kalikonse koyenera kuwonongedwa kuti Yehova abweze mkwiyo wake wochititsa manthawu. Adzakuchitirani chifundo ndi kukumverani chisoni, ndipo adzakuchulukitsani monga analonjeza mwa lumbiro kwa makolo anu,
18 BOEIPA na Pathen kah ol te na ngai atah tihnin ah kai loh nang kang uen olpaek boeih ngaithuen. BOEIPA na Pathen kah mikhmuh ah a thuem ni saii ham a om.
chifukwa mumamvera Yehova Mulungu wanu, kusunga malamulo ake onse amene ndikukupatsani lero lino ndi kuchita zoyenera pamaso pake.

< Olrhaepnah 13 >