< Daniel 4 >

1 Nebukhadnezzar manghai loh namtu pilnam boeih neh olcom olcae neh, diklai pum kah khosa, khosa te, “Nangmih kah ngaimongnah he pungtai saeh.
Mfumu Nebukadinezara anatumiza mawu awa kwa anthu a mitundu yonse, ndi chiyankhulo chilichonse, amene amakhala pa dziko lonse lapansi: Mtendere uchuluke pakati panu!
2 Khohni kah Khohni Pathen loh kai hamla miknoek neh khobae rhambae te a tueng sak tih kai taengah thui hamla a huem.
Chandikomera kukuwuzani zizindikiro zozizwitsa ndi zodabwitsa zimene Mulungu Wammwambamwamba wandichitira.
3 A miknoek te metluk lam lae boeilen tih amah khobae rhambae he metluk lam lae a tlungluen. A ram he kumhal kah ram tih a khohung khaw thawnpuei lamloh cadilcahma taengah om ni.
Zizindikiro zake ndi zazikulu,
4 Kai Nebukhadnezzar tah ka im kah thayoei nen khaw, ka bawkim kah hnothen nen khaw ka om.
Ine Nebukadinezara, ndinali kwathu mʼnyumba yanga yaufumu, mwa mtendere ndipo ndinali wokhutitsidwa.
5 Mang ka man vaengah kai n'hihham tih ka thingkong dongah poeknah neh ka lu dongkah mangthui loh kai n'cahawh.
Ndili chigonere pa bedi langa, ndinalota maloto amene anandichititsa mantha. Zinthu ndi masomphenya zimene ndinaziona zinandiopsa.
6 Ka mang kah thuingaihnah te thui saeh tila Babylon hlang cueih boeih te kamah taengah khuen hamla kai lamloh saithainah a paek coeng.
Choncho ndinalamula kuti anthu onse a nzeru a ku Babuloni abwere pa maso panga kunditanthauzira malotowo.
7 Hmayuep rhoek, rhaitonghma rhoek, Khalden rhoek neh aisi aka suep khaw ha pai, ha pai vaengah mang he amih taengah ka thui dae a thuingaihnah te kai taengah a ming uh moenih.
Pamene amatsenga, owombeza, alawuli ndi amawula anabwera, ndinawafotokozera maloto, koma sanathe kunditanthauzira.
8 Tedae a hnukkhueng la Daniel he kai taengla ha pai. Anih te ka pathen ming bangla Belteshazzar a ming nah. Anih tah a khuiah khaw Pathen Mueihla cim a om dongah a taengah mang ka thui pah.
Potsiriza, anabwera Danieli uja amatchedwa Belitesezara, potsata dzina la mulungu wanga, ndipo mzimu wa milungu yoyera uli mwa iye. Iyeyu ndinamufotokozera malotowo.
9 Belteshazzar tah hmayuep boei pai ni. Na khui ah Pathen kah mueihla cim om tih oldung boeih khaw nang hamla kuel pawh tila ka ming. Ka mang ah mangthui ka hmuh tih a thuingaihnah khaw a thui.
Ndinati, “Belitesezara, mkulu wa amatsenga, ndikudziwa kuti mzimu wa milungu yoyera uli mwa iwe, ndipo palibe chinsinsi chomwe sungachidziwe. Awa ndi maloto anga; unditanthauzire.
10 Ka thingkong dongah ka lu kah mangthui ka hmuh. Te vaengah diklai laklung kah thing tah a sang khaw muep sang he.
Awa ndi masomphenya amene ine ndinaona pamene ndinali kugona pa bedi: Ndinaona, mtengo wautali kwambiri utayima pakati pa dziko lapansi.
11 Thing te rhoeng tih a hlul dongah a sang loh vaan duela a pha. Te dongah a mueimae he diklai pum kah khobawt duela tueng.
Mtengowo unakula ndi kulimba ndipo msonga yake inafika mpaka mlengalenga; umaonekera pa dziko lonse lapansi.
12 A hnah te then tih a thaih khaw yet. Te dongah a soah a cungkuem ham buh om tih a hmui ah kohong rhamsa loh hlipying uh. A bu dongah vaan kah vaa loh kho a sak tih te lamloh pumsa boeih a cah.
Masamba ake anali okongola, zipatso zinali zochuluka, ndipo mu mtengomo munali chakudya chokwanira anthu onse. Zirombo zakuthengo zimapeza mthunzi mʼmunsi mwake, ndipo mbalame zamlengalenga zimakhala pa nthambi zake: Cholengedwa chilichonse chinkadya za mu mtengowu.
13 “Ka thingkong dongah ka lu dongkah mangthui ka hmuh tih ka om vaengah vaan lamkah thinghla cim tah ha rhum.
“Ndikanali chigonere ndinaona mʼmasomphenya mngelo atayima pamaso panga, woyera, atatsika kuchokera kumwamba.
14 Thadueng neh pang tih, ‘Thing te vung lamtah, a bu te saih pah, a hnah te hae pah lamtah a thaih haeh pah. A hmui lamkah rhamsa neh a bu dongkah vaa khaw nong saeh.
Anayankhula mofuwula kuti, ‘Gwetsa mtengo ndi kusadza nthambi zake; yoyola masamba ake kuti nyama zakuthengo zithawe pa mthunzi pake ndi mbalame zithawe pa nthambi zake.
15 Tedae a yung a ngo tah diklai ah ngol saeh lamtah thi neh rhohum kah pinnah neh kohong baeldaih khui ah om saeh. Te dongah vaan kah buem loh saep saeh lamtah a hamsum rhamsa neh diklai baelhing lakli ah om saeh.
Koma musiye tsinde ndi mizu yake mʼnthaka. Tsindelo mulimange maunyolo a chitsulo ndi mkuwa, zikhalebe mʼnthaka, nʼkudya udzu mʼmunda. “‘Mumulole iye anyowe ndi mame akumwamba, ndipo iye akhale ndi nyama pakati pa zomera za mʼnthaka.
16 Tekah hlang tah a thinko te hlang lamloh poehlip saeh lamtah anih te rhamsa thinko pae saeh. Te vaengah anih ham kum rhih thok pah saeh.
Maganizo ake a umunthu asinthidwe ndipo apatsidwe maganizo a nyama ya kuthengo, mpaka zaka zisanu ndi ziwiri zitadutsa.
17 He kong dongkah thinghla kah saithainah ol neh a cim olpaek oltloek rhangneh a sangkoek lakah a sangkoek loh hlang kah ram neh hlang khaw a hung te mulhing rhoek loh ming uh saeh. Te dongah te te a ngaih sarhui taengah a paek tih mathoe hlang rhoek te a so, a so ah a pai sak,’ a ti.
“‘Angelo oyera ndiwo akutsimikiza chilangochi. Tsono anthu adziwe kuti Mulungu Wammwambamwamba ali ndi mphamvu yolamulira maufumu onse, ndipo amawapereka kwa aliyense akumufuna, ngakhale munthu wamba kuti alamulire.’
18 Kai manghai Nebukhadnezzar loh mang loh ka man he Belteshazzar nang, namah loh a thuingaihnah thui laeh. Te kong dongah ka ram kah hlang cueih boeih loh kai taengah a thuingaihnah thuicaih ham a noeng uh moenih. Nang, namah tah na khuikah Pathen mueihla cim rhangneh na noeng coeng,” a ti.
“Amenewa ndi maloto amene ine, mfumu Nebukadinezara, ndinalota. Tsopano Belitesezara, undifotokozere tanthauzo lake, popeza palibe mwa anthu anzeru a mu ufumu wanga amene angathe kunditanthauzira. Koma iwe ukhoza, chifukwa mzimu wa milungu yoyera uli mwa iwe.”
19 Te dongah Belteshazzar aka ming nah Daniel tah khonoek pakhat khuiah hit sut. A poeknah loh amah a cahawh. Te dongah manghai loh a voek tih, “Belteshazzar, mang neh a thuingaihnah nang te let boeh,” a ti nah. Belteshazzar loh a doo tih, “Ka boeipa aw, ka boeipa na saeh, mang te na lunguet, na lunguet ham tih a thuingaihnah tah na rhal, na rhal ham ni.
Pamenepo Danieli, amene amatchedwa Belitesezara, anavutika mu mtima kwambiri kwa kanthawi, ndipo anasautsidwa mʼmaganizo ake. Choncho mfumu inati, “Belitesezara usalole malotowa kapena tanthauzo lake likuopse.” Belitesezara anayankha kuti, “Mbuye wanga, ndikanakonda malotowa akanakhudza adani anu okha, ndi tanthauzo lake kwa iwo okusautsani!
20 Na hmuh bangla thing te rhoeng tih hlul. Te dongah a sang vaan duela a pha tih a mueimae te diklai pum ah tueng.
Mtengo munawuona uja, umene unkakulirakulira kwambiri ndi kulimba, ndi msonga yake inafika mlengalenga, ndi kuonekera ku dziko lonse lapansi,
21 A hnah then tih a thaih yet. A soah a cungkuem ham buh om tih a hmui ah kohong rhamsa loh kho a sak. A bu dongah vaan kah vaa loh kho a sak.
mtengo umene masamba ake anali okongola ndiponso unali ndi zipatso zochuluka zokwanira kudya anthu onse a dziko lapansi. Mtengowu unkapereka mthunzi ku zirombo zonse zakuthengo, ndipo mbalame zamlengalenga zinayika zisa pa nthambi zake.
22 Manghai nang namah tah na rhoeng tih na hlul dongah na lennah khaw vaan a pha duela rhoeng na. Na khohung loh diklai khobawt duela a pha.
Inu mfumu, ndinu mtengo umenewo! Inu mwakhala wamkulu ndi wamphamvu; ukulu wanu wakula mpaka wakhudza mlengalenga, ndipo ufumu wanu wafika mpaka ku malo akutali a dziko lapansi.
23 Manghai aw, a tueng bangla, thinghla cim tah vaan lamloh rhum tih, ‘Thing te vung uh lamtah palet uh. A yung a ngo tah diklai ah hlun uh lamtah thi neh rhohum kah pinnah neh kohong baeldaih khuiah om saeh. Te vaengah vaan kah buem neh saep saeh lamtah anih te kum rhih a thok duela amah hamsum kohong rhamsa taengah om saeh,’ a ti.
“Inu mfumu munaona mthenga woyera, akuchokera kumwamba ndipo anati, ‘Gwetsani mtengo ndipo muwuwononge, koma musiye tsinde ndi mizu yake. Tsindelo mulimange ndi unyolo wa chitsulo ndi mkuwa ndipo mulisiye pakati pa udzu wa mʼmunda. Mulole kuti linyowe ndi mame akumwamba. Likhale ngati nyama zakuthengo, mpaka zaka zidutse zisanu ndi ziwiri.’
24 Manghai aw a thuingaihnah he tah a sangkoek a sangkoek kah saithainah ni. He he ka boeipa neh ka boeipa manghai taengah pai coeng.
“Tanthauzo lake ndi ili mfumu, izi ndi zimene Mulungu Wammwambamwamba watsimikiza kuti zikugwereni mbuye wanga mfumu:
25 Nang te hlang taeng lamloh m'vai uh vetih kohong rhamsa taengah ni na khosaknah a om eh. Baelhing te vaito bangla na caak vetih vaan kah buem neh nang te n'saep ni. A sangkoek kah a sangkoek loh hlang kah ram soah a hung tih te te a ngaih sarhui taengah a paek tila na ming hil nang hamla kum rhih thok ni.
Inu mudzachotsedwa pakati pa anthu ndipo mudzakhala ndi nyama zakuthengo; mudzadya udzu monga ngʼombe ndi kunyowa ndi mame akumwamba. Zaka zisanu ndi ziwiri zidzadutsa mpaka mudzavomereze kuti Mulungu Wammwambamwamba ndiye mwini ulamuliro pa ma ufumu a anthu, ndipo amawapereka kwa aliyense amene Iye wafuna.
26 Thing kah a yung a ngo hlun ham a thui bangla vaan aka hung te na ming van lamloh na ram te namah taengla cak ni.
Lamulo losiya tsinde la mtengo ndi mizu yake litanthauza kuti ufumu wanu udzabwezeredwa kwa inu mukadzavomereza kuti Mulungu ndiye amalamulira.
27 Te dongah manghai aw, kai poeknah he namah taengah na doe mai mako. Na tholhnah te duengnah neh phaeh lamtah hlanghnaem pataek na rhen nen te na halangnah hnawt laeh. Na ommongnah te a congnah a om khaming,” a ti nah.
Nʼchifukwa chake mfumu, chikukomereni kulandira malangizo anga: Lekani machimo ndipo muzichita zabwino, lekani mphulupulu zanu ndipo muzikomera mtima anthu opsinjika. Nʼkutheka kuti mtendere wanu udzapitirira.”
28 Te boeih te Nebukhadnezzar manghai taengah a pai pah.
Zonsezi zinamuchitikira mfumu Nebukadinezara.
29 Hla hlai nit a bawtnah dongah tah Babylon ram kah bawkim ah om tih pongpa.
Itapita miyezi khumi ndi iwiri, pamene mfumu inkayenda pa denga la nyumba ya ufumu ya ku Babuloni,
30 Te vaengah manghai te cal tih, “Babylon he a boeilen moenih a? He te kai loh ka thadueng sarhi neh kamah kah hinyahnah, thangpomnah ham ram kah im la ka sak,” a ti.
iye anati, “Kodi Babuloni si mzinda wamphamvu ndi wokongola umene ndinamanga ndi mphamvu zanga ngati nyumba yanga yaufumu, kuonetsera ulemerero wa ufumu wanga?”
31 Manghai ka dongah ol a cal li vaengah vaan lamkah ol cet tih, “Manghai Nebukhadnezzar nang hamla a thui tih ram he nang lamloh nong coeng.
Akuyankhulabe izi mawu anamveka kuchokera kumwamba kuti, “Imvani izi, mfumu Nebukadinezara: Ufumu wako wachotsedwa.
32 Nang te hlang taeng lamloh m'vai coeng tih na khosaknah he kohong rhamsa nen ni a om. Nang te vaito bangla rham n'cah vetih a sangkoek kah a sangkoek loh hlang kah ram soah a hung tih te te a ngaih taengah a paek tila na ming hil nang hamla kum rhih thok ni,” a ti nah.
Udzachotsedwa pakati pa anthu ndipo udzakhala ndi zirombo zakuthengo; udzadya udzu monga ngʼombe. Zaka zisanu ndi ziwiri zidzadutsa mpaka iwe utavomereza kuti Wammwambamwamba ndiye mwini ulamuliro pa maufumu a anthu ndipo amawupereka kwa aliyense amene iye afuna.”
33 Amah ol a bangli vaengah Nebukhadnezzar soah a pha tih hlang taeng lamloh a vai uh. Te vaengah vaito bangla rham a caak tih a sam te atha bangla, a kuttin te vaa bangla a saii hil a pum te vaan kah buem loh a saep.
Nthawi yomweyo zonse zimene zinanenedwa zokhudza Nebukadinezara zinakwaniritsidwa. Iye anachotsedwa pakati pa anthu ndipo ankadya udzu ngati ngʼombe. Thupi lake linanyowa ndi mame akumwamba mpaka tsitsi lake linakula ngati nthenga za chiwombankhanga ndi zikhadabo ngati zikhadabo za mbalame.
34 A tue bawtnah dongah tah, kai Nebukhadnezzar loh ka mik he vaan la ka huel hatah ka mingnah he ka taengla ha mael. Te dongah a sangkoek Khohni te ka koeh tih kumhal kah mulhing te ka oep tih ka hinyah nah. A khohung te dungyan kah khohung tih a ram kah thawnpuei lamloh cadilcahma duela cak.
Pomaliza pa zaka zimenezo ine, Nebukadinezara ndinakweza maso anga kumwamba, ndipo nzeru zanga zinabwereramo. Kenaka ndinatamanda Wammwambamwamba; ndinamupatsa ulemu ndi kumulemekeza Iye amene akhala nthawi zonse.
35 Diklai khosa, khosa boeih tah aka om pawt bangla a ngai tih diklai khosa, khosa rhoek te vaan thadueng neh a ngaih bangla a saii. A kut te aka doek pa tih a taengah “Balae na saii?” aka ti nah te a om moenih.
Anthu onse a dziko lapansi
36 Ka mingnah loh ka taengah a mael tue vaengah, ka ram kah thangpomnah, kai hinyahnah neh ka aa ka taengla ha mael. Kai he ka olrhoep neh ka boei ka na rhoek loh n'toem uh. Ka ram he pai tih lennah kai taengah muep a thap.
Pa nthawi yomweyo nzeru zanga zinabwereramo. Ndinalandiranso ulemu wanga ndi ufumu wanga. Nduna ndi akalonga anga anandilandiranso. Ndipo anandibwezera ufumu wanga ndi kukhalanso wamphamvu kuposa kale.
37 Kai Nebukhadnezzar tah n'oep tih m'pacuet coeng. Te dongah vaan kah manghai tah hinyah pai saeh. A bibi boeih he oltak tih a longpuei khaw tiktam. Te dongah koevoeinah neh aka pongpa te kunyun sak ham a noeng.
Tsopano ine Nebukadinezara, ndikutamanda, kukweza ndi kulemekeza Mfumu yakumwamba chifukwa zonse zimene amachita ndi zoyenera ndipo njira zake zonse ndi zachilungamo. Ndipo onse amene amayenda modzikuza adzawatsitsa.

< Daniel 4 >