< 2 Samuel 22 >

1 A thunkha cungkuem kut lamkah oe, Saul kut lamkah BOEIPA loh anih a huul hnin vaengah, David loh BOEIPA taengah hekah laa lung he a thui.
Davide anayimbira Yehova nyimbo iyi pamene Yehovayo anamupulumutsa mʼdzanja la adani ake onse ndiponso mʼdzanja la Sauli.
2 Te vaengah, “BOEIPA tah ka thaelpang neh ka rhalvong neh kai ham tah kai aka hlawt la om.
Iye anati, “Yehova ndiye thanthwe langa, chitetezo changa ndi mpulumutsi wanga.
3 Ka lungpang Pathen amah dongah ni ka ying, ka photling neh khangnah ki, ka imsang neh ka thuhaelnah, khangkung loh kai he kuthlahnah lamloh nan khang.
Mulungu wanga ndiye thanthwe langa, mʼmene ndimathawiramo, chishango changa ndi ndodo yachipulumutso changa. Iye ndi linga langa, pothawirapo panga ndi mpulumutsi wanga. Munandipulumutsa mʼmanja mwa anthu ankhanza.
4 Thangthen ham tueng BOEIPA te ka khue dongah ka thunkha rhoek taeng lamloh ng'khang.
“Ndimayitana Yehova amene ndi woyenera matamando, ndipo ndapulumutsidwa kwa adani anga.
5 Dueknah tuiphu loh kai n'li tih, aka muen soklong loh n'let sak he.
“Mafunde a imfa anandizinga; mitsinje yothamanga yachiwonongeko inandiopsa kwambiri.
6 Saelkhui kah rhui loh kai m'ven tih, dueknah hlaeh loh kai m'mah. (Sheol h7585)
Anandimanga ndi zingwe za ku manda; misampha ya imfa inalimbana nane. (Sheol h7585)
7 Ka kho a bing vaengah BOEIPA te ka khue tih ka Pathen taengah ka pang. Te vaengah ka pang ol te a bawkim lamloh a hna neh a yaak.
“Mʼmasautso anga ndinapemphera kwa Yehova; ndinapemphera kwa Mulungu wanga. Iye ali mʼnyumba yake, anamva mawu anga; kulira kwanga kunafika mʼmakutu ake.
8 Te vaengah diklai te tuen la tuen tih hinghuen. Anih taengah a sai dongah vaan kah a yung te tlai tih tuen.
“Dziko lapansi linanjenjemera ndi kuchita chivomerezi, maziko a miyamba anagwedezeka; ananjenjemera chifukwa Iye anakwiya.
9 A hnarhong lamkah hmaikhu thoeng tih, a ka lamkah hmai loh a laeh vaengah hmai-alh khaw tak.
Mʼmphuno mwake munatuluka utsi; moto wonyeketsa unatuluka mʼkamwa mwake, makala amoto anali lawilawi mʼkamwa mwake.
10 Te phoeiah vaan a koiloep tih, a suntlak vaengah yinnah tah a kho hmuila pawk.
Iye anangʼamba thambo natsika pansi; pansi pa mapazi ake panali mitambo yakuda.
11 Cherub dongah ngol bal tih a ding vaengah khohli phae sola phoe.
Iye anakwera pa Kerubi ndi kuwuluka; nawuluka ndi mphepo mwaliwiro.
12 A kaepvai khohmuep neh khomong khomai dongkah tui tun te dungtlungim la a khueh.
Iye anapanga mdima kukhala chofunda chake, mitambo yakuda ya mlengalenga.
13 Amah hmaikah a aa loh a hmai-alh te a dom.
Mʼkuwala kumene kunali pamaso pake munkachokera makala amoto alawilawi.
14 BOEIPA te vaan lamloh a kawk vaengah Khohni loh a ol a huel.
Yehova anabangula kumwamba ngati bingu, mawu a Wammwambamwamba anamveka ponseponse.
15 Thaltang a kah tih amih te a taekyak phoeiah, amih te rhaek neh a khawkkhek la a khawkkhek.
Iye anaponya mivi yake, nabalalitsa adani ake, ndi zingʼaningʼani zake anawagonjetsa.
16 BOEIPA kah tluungnah neh a hiil dongkah a thintoek yilh loh lunglai kah yung hoep tih sokca tuipuei khaw tueng.
Zigwa za mʼnyanja zinaonekera poyera, ndipo maziko a dziko lapansi anakhala poyera, Yehova atabangula mwaukali, pamene mpweya wamphamvu unatuluka mʼmphuno mwake.
17 A sang lamloh yueng uh tih tui dueng khui lamkah kai he n'tuuk tih n'doek.
“Ali kumwamba, Iye anatambalitsa dzanja lake ndipo anandigwira; anandivuwula mʼmadzi ozama.
18 Kai ham tah tlung uh dae ka thunkha hlangtlung neh ka lunguet taeng lamkah kai n'huul.
Anandipulumutsa kwa mdani wanga wamphamvu, adani anga amene anali amphamvu kuposa ine.
19 Ka rhainah hnin ah kai m'mah uh cakhaw BOEIPA tah kai ham tukcawt longkhawn la om.
Adaniwo analimbana nane pamene ndinali pa mavuto, koma Yehova anali thandizo langa.
20 Kai khuiah a naep dongah kai he hoengpoeknah la kai n'khuen tih n'pumcum sak.
Iye anandipititsa kumalo otakasuka; anandipulumutsa chifukwa amakondwera nane.
21 Ka duengnah bangla BOEIPA loh kai n'thung tih, ka kut kah a cimcaihnah vanbangla kamah taengla ham mael coeng.
“Yehova wandithandiza molingana ndi chilungamo changa; molingana ndi makhalidwe anga abwino, Iye wandipulumutsa.
22 BOEIPA kah longpuei te ka ngaithuen tih ka Pathen taeng lamloh ka poehlip van pawh.
Pakuti ine ndinatsata njira za Yehova; ndilibe mlandu wochoka pamaso pa Mulungu wanga.
23 Amah kah laitloeknah boeih te tah a laitloeknah bangla ka hmaiah ka khueh tih a khosing lamloh ka phael pawh.
Malamulo ake onse ali pamaso panga, sindinasiye malangizo ake.
24 A hmaiah cuemthuek la ka om tih ka thaesainah lamkah khaw ka cue uh.
Ndakhala moyo wosalakwa pamaso pake ndipo ndakhala ndi kupewa tchimo.
25 A mikhmuh kah ka duengnah, ka cimcaihnah vanbangla BOEIPA loh ka taengah han thuung coeng.
Yehova wandipatsa mphotho molingana ndi chilungamo changa, molingana ndi makhalidwe anga abwino pamaso pake.
26 Hingcim taengah uepom la na om tih, cuemthuek hlangrhalh taengah na cungkuem coeng.
“Kwa wokhulupirika, Inu mumaonetsa kukhulupirika kwanu, kwa anthu amakhalidwe abwino, Inu mumaonetsanso makhalidwe abwino,
27 Aka meet uh taengah na meet uh tih, voeldak te tah na hnueih.
Kwa woyera mtima, Inu mumaonetsa kuyera mtima kwanu, koma kwa anthu achinyengo mumaonetsanso kunyansidwa nawo.
28 Pilnam mangdaeng te na khang tih, na mikhmuh kah aka pomsang rhoek te na hlak.
Inu mumapulumutsa anthu odzichepetsa, koma maso anu amatsutsana ndi odzikuza ndipo mumawatsitsa.
29 BOEIPA namah tah ka hmaithoi la na om tih, ka hmaisuep khaw BOEIPA loh a tue coeng.
Inu Yehova, ndinu nyale yanga; Yehova wasandutsa mdima wanga kukhala kuwunika.
30 Namah nen tah caem khaw ka poeng tih, ka Pathen nen tah pangbueng khaw ka poe thai.
Ndi thandizo lanu nditha kulimbana ndi gulu la ankhondo, ndi Mulungu wanga nditha kuchita zosatheka ndi munthu.
31 Pathen tah a longpuei khangmai tih, BOEIPA kah olthui a cimcaih dongah anih khuiah aka ying boeih ham tah photling la a om pah.
“Kunena za Mulungu, zochita zake ndi zangwiro; mawu a Yehova alibe cholakwika. Iye ndi chishango kwa onse amene amathawira kwa iye.
32 BOEIPA phoeikah Pathen te unim? Mamih kah Pathen phoeiah tah unim lungpang bal?
Mulungu wina ndi uti wofanana nanu Yehova? Ndipo ndani amene ndi Thanthwe kupatula Mulungu wathu?
33 Ka lunghim Pathen tah ka thadueng la om tih, a longpuei te ka longpuei ham khangmai la a khueh.
Ndi Mulungu amene anandipatsa mphamvu ndi kulungamitsa njira yanga.
34 Ka kho sayuk kho bangla a khueh tih, ka hmuensang ah kai m'pai sak.
Iye amasandutsa mapazi anga kukhala ngati ambawala yayikazi; Iye amandithandiza kuyimirira pamwamba pa mapiri.
35 Ka kut he caemtloek ham a cang tih ka ban loh rhohum lii khaw a phuk thai.
Iye amaphunzitsa manja anga kuchita nkhondo; manja anga amatha kuthyola uta wachitsulo.
36 Namah kah daemnah photling te ka taengah nam paek tih, namah kah kodonah neh kai nan ping sak.
Inu mundipatsa ine chishango chanu cha chigonjetso; mumawerama kuti mundikweze.
37 Ka kungdak kah ka kholaeh khaw na aeh dongah ka kho paloe pawh.
Inu mwalimbitsa njira yanga kuti ndiyende bwino, kuti mapazi anga asaterereke.
38 Ka thunkha rhoek te ka hloem tih, ka mitmoeng sak vaengah amih ka khah hlanah ka balkhong moenih.
“Ine ndinathamangitsa adani anga ndi kuwakantha; sindinabwerere mpaka iwo atawonongedwa.
39 Amih te ka khah tih ka phop daengah ni thoo uh thai pawt tih ka kho tangah a bakop uh.
Ndinawakantha kotheratu, ndipo sanathe kudzukanso; Iwo anagwera pansi pa mapazi anga.
40 Caemtloek ham khaw kai he thadueng nan vah sak tih, kai aka tlai thil rhoek te kamah hmuila na koisu.
Inu munandipatsa ine mphamvu yochitira nkhondo; munagwaditsa adani anga pa mapazi anga.
41 Te dongah ka thunkha rhoek te kai taengah a rhawn na duen sak tih, ka lunguet khaw ka biit.
Inu muchititsa kuti adani anga atembenuke ndi kuthawa; ndipo ndinawononga adani anga.
42 BOEIPA taengah khaw pang uh coeng dae khang voel pawt tih, amih te doo voel pawh.
Iwo anafuwula kupempha thandizo, koma panalibe ndi mmodzi yemwe owapulumutsa. Analirira kwa Yehova, koma sanawayankhe.
43 Te dongah amih te diklai laipi bangla ka neet tih, long kah tangnong bangla ka tip sak phoeiah ka nulh.
Ine ndinawaperesa ngati fumbi la pa dziko lapansi; ndinawasinja ndipo ndinawapondaponda ngati matope a mʼmisewu.
44 Ka pilnam kah tuituknah khui lamkah khaw kai nan hlawt. Namtom kah a lu la kai nan hloe dongah ming pawt pilnam loh kai taengah thotat.
“Inu mwandipulumutsa mʼmanja mwa mitundu ya anthu; Inu mwandisunga kuti ndikhale mtsogoleri wa anthu a mitundu ina. Anthu amene sindikuwadziwa ali pansi pa ulamuliro wanga.
45 Kholong ca rhoek loh kai taengah mai a tum uh tih, a hna neh a yaak hamla ka ol a hnatun uh.
Alendo amadzipereka okha pamaso panga; akangomva za ine, amandigonjera.
46 Kholong ca rhoek loh tahah uh tih, a vongtung khui lamloh yingyet uh.
Iwo onse anataya mtima; anatuluka mʼmalinga awo akunjenjemera.
47 BOEIPA kah hingnah dongah ka lungpang tah a yoethen pai tih, kai ham daemnah lungpang Pathen tah pomsang pai saeh.
“Yehova ndi wamoyo! Litamandidwe Thanthwe langa. Akuzike Mulungu, Thanthwe, Mpulumutsi wanga!
48 Pathen loh kai hamla tawnlohnah a paek tih, pilnam te kai kungdak la a suntlak sak.
Iye ndi Mulungu amene amabwezera chilango, amene amayika anthu a mitundu yonse pansi pa ulamuliro wanga,
49 Ka thunkha rhoek taeng lamkah kai nan poh, kai aka tlai thil rhoek kah a sola kai nan pomsang bal. Hlang kah kuthlahnah lamkah kai nan huul.
amene amandimasula mʼmanja mwa adani anga. Inu munandikuza kuposa adani anga; munandilanditsa mʼmanja mwa anthu ankhanza.
50 Te dongah BOEIPA nang te namtom taengah kan uem vetih na ming te ka tingtoeng ni.
Choncho ine ndidzakutamandani Inu Yehova, pakati pa anthu a mitundu ina; ndidzayimba nyimbo zotamanda dzina lanu.
51 A manghai kah khangnah imsang tah len pai. Te dongah ni sitlohnah he a koelh taengah khaw, David neh a tiingan taengah khaw kumhal duela a saii pah,” a ti.
“Iye amapereka chipambano chachikulu kwa mfumu yake, amaonetsa kukoma mtima kwa wodzozedwa wake, kwa Davide ndi zidzukulu zake kwamuyaya.”

< 2 Samuel 22 >