< 1 Manghai 16 >
1 BOEIPA ol tah Baasha hamla Hanani capa Jehu taengla ha pawk tih,
Ndipo Yehova anayankhula kudzera mwa Yehu mwana wa Hanani, mawu odzudzula Baasa kuti,
2 “Nang te laipi lamloh kan pomsang tih ka pilnam Israel soah rhaengsang la nang kang khueh. Tedae Jeroboam kah longpuei ah na pongpa tih ka pilnam Israel te na tholh sak dongah amih kah tholhnah neh kai nan veet.
“Ine ndinakukuza kuchokera pa fumbi ndipo ndinakupanga kuti ukhale mtsogoleri wa anthu anga Aisraeli, koma iwe wakhala ukuyenda mʼnjira za Yeroboamu ndi kuchimwitsa anthu anga Aisraeli naputa mkwiyo wanga chifukwa cha machimo awo.
3 Baasha hnuk neh a imkhui hnuk te ka hlawp pah coeng he. Te dongah na imkhui te Nebat capa Jeroboam imkhui bangla kang khueh ni.
Taonani, Ine ndatsala pangʼono kuwononga Baasa pamodzi ndi nyumba yake, ndipo ndidzachitira nyumba yake zimene ndinachita pa nyumba ya Yeroboamu mwana wa Nebati.
4 Khopuei ah Baasha kah a duek rhok te ui loh a caak vetih kohong kah a duek rhok te vaan kah vaa loh a caak ni,” a ti.
Agalu adzadya aliyense wa banja la Baasa amene adzafere mu mzinda, ndipo mbalame za mu mlengalenga zidzadya iwo amene adzafere kuthengo.”
5 Baasha kah ol noi neh a saii te khaw, a thayung thamal khaw, Israel manghai rhoek kah khokhuen olka cabu dongah a daek moenih a?
Tsono ntchito zina za Baasa ndi zamphamvu zake zimene anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a Israeli?
6 Baasha te a napa rhoek taengla a khoem uh vaengah tah Tirzah ah a up. Te phoeiah a capa Elah te anih yueng la manghai.
Baasa anamwalira nayikidwa mʼmanda amene anayikidwa makolo ake ku Tiriza. Ndipo Ela mwana wake anakhala mfumu mʼmalo mwake.
7 BOEIPA mikhmuh ah boethae cungkuem a saii tih a kut saii neh amah a veet dongah, Jeroboam imkhui bangla khueh hamla, Hanani capa tonghma Jehu kut ah khaw Baasha ham neh a imkhui hamla BOEIPA ol ha pawk. Te dongah ni anih te a ngawn.
Komatu Yehova anayankhula kwa Baasa pamodzi ndi banja lake lonse kudzera mwa mneneri Yehu mwana wa Hanani, chifukwa cha zoyipa zonse zimene iye anachita pamaso pa Yehova, kukwiyitsa Yehovayo nakhala ngati nyumba ya Yeroboamu ndiponso chifukwa anawonongeratu banja la Yeroboamu.
8 Judah manghai Asa kah a kum kul kum rhuk vaengah Baasha capa Elah he Tirzah kah Israel ah kum nit manghai.
Mʼchaka cha 26 cha ufumu wa Asa mfumu ya Yuda, Ela mwana wa Baasa anakhala mfumu ya Israeli, ndipo analamulira ku Tiriza zaka ziwiri.
9 Anih tah amah kah sal, leng caem rhakthuem mangpa Zimri loh a taeng. Te vaengah amh te Tirzah kah Tirzah im tawt Arza im ah a ok tih rhui.
Zimuri, mmodzi mwa akuluakulu ake, amene ankalamulira theka la magaleta ake, anamuchitira chiwembu. Nthawi imeneyi Ela anali ku Tiriza, akumwa koledzera nako mʼnyumba ya Ariza, munthu amene ankayangʼanira nyumba yaufumu ku Tiriza.
10 Zimri a pawk vaengah Elah te a ngawn tih a duek sak. Judah manghai Asa kah kum kul kum rhih vaengah Elah yueng la manghai.
Zimuri anadzalowa, namukantha ndi kumupha mʼchaka cha 27 cha Asa mfumu ya Yuda. Ndipo Zimuriyo anakhala mfumu mʼmalo mwake.
11 A manghai neh a ngolkhoel dongah a ngol vanbangla Baasha imkhui te boeih a ngawn tih pangbueng aka yun thil khaw, a tlan sa khaw, a hui khaw hlun pawh.
Zimuri atangoyamba kulamulira, anapha banja lonse la Baasa. Sanasiyepo munthu wamwamuna ndi mmodzi yemwe, wachibale kapena bwenzi lake.
12 BOEIPA ol bangla Zimri loh Baasha imkhui te boeih a mitmoeng sak. Te te Baasha hamla tonghma Jehu kut ah ana thui coeng.
Choncho Zimuri anawononga banja lonse la Baasa, molingana ndi mawu amene Yehova anayankhula motsutsa Baasa kudzera mwa mneneri Yehu,
13 Baasha kah tholhnah cungkuem neh a capa Elah kah tholhnah dongah tholh uh. Te dongah Israel te a tholh sak tih amih kah a honghi neh Israel Pathen BOEIPA te a veet.
chifukwa cha machimo onse amene Baasa ndi mwana wake Ela anachita nachimwitsa Israeli, anakwiyitsa Yehova, Mulungu wa Israeli ndi mafano awo osapindulitsa.
14 Elah kah ol noi neh a saii boeih te Israel manghai rhoek kah khokhuen olka cabu dongah a daek uh moenih a?
Tsono ntchito zina za Ela ndi zina zonse zimene anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a Israeli?
15 Judah manghai Asa kah kum kul kum rhih, Tirzah ah Zimri hnin rhih a manghai vaengah pilnam loh Philisti kah Gibbethon a rhaeh rhil.
Mʼchaka cha 27 cha Asa mfumu ya Yuda, Zimuri analamulira ku Tiriza masiku asanu ndi awiri. Gulu la ankhondo linali litamanga misasa pafupi ndi Gibetoni, mzinda wa Afilisti.
16 Pilnam aka rhaeh loh a yaak vaengah, “Zimri loh a taeng tih manghai te khaw a ngawn,” a ti uh. Te dongah Israel pum loh Israel sokah caempuei mangpa Omri te rhaehhmuen khuiah hnin at neh a manghai sakuh.
Ankhondo amene anali ku misasa atamva kuti Zimuri wachita chiwembu ndi kupha mfumu, tsiku lomwelo ku misasako anasankha Omuri, mkulu wa ankhondo kukhala mfumu ya Israeli.
17 Te dongah Omri neh a taengkah Israel pum tah Gibbethon lamloh thoeih uh tih Tirzah te a dum uh.
Tsono Omuri ndi Aisraeli onse amene anali naye anachoka ku Gibetoni ndi kukazinga Mzinda wa Tiriza.
18 Khopuei a buem pah te Zimri loh a hmuh van neh manghai im kah impuei la kun. Te phoeiah manghai im te a kaep ah hmai neh a hoeh tih amah khaw duek.
Zimuri ataona kuti mzinda walandidwa, anathawira ku nsanja ya nyumba ya mfumu ndipo anatentha nyumbayo iye ali momwemo. Kotero iyeyo anafa,
19 A tholhnah dongah a tholhnah bangla BOEIPA mik ah boethae a saii te tholh coeng. Israel te tholh sak ham aka saii Jeroboam kah longpuei neh a tholhnah dongah ni a. pongpa.
chifukwa cha machimo amene iye anachita, kuchita zoyipa pamaso pa Yehova ndi kuyenda mʼnjira za Yeroboamu, nachimwitsa nazo Aisraeli.
20 Zimri kah ol noi, a lairhui neh a ven khaw, Israel manghai rhoek kah khokhuen olka cabu dongah a daek uh moenih a?
Tsono ntchito zina za Zimuri ndi chiwembu chake chimene anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a Israeli?
21 Te vaengah Israel pilnam he rhakthuem la vik a paek. Pilnam rhakthuem te Ginath capa Tibni taengah om tih amah te a manghai sak. A rhakthuem te Omri hnuk a vai.
Pambuyo pake Aisraeli anagawikana pakati: theka linatsatira Tibini mwana wa Ginati kuti limulonge ufumu, ndipo theka lina linatsatira Omuri.
22 Tedae Omri hnukkah pilnam loh Ginath capa Tibni hnukah pilnam te a khuk vaengah Tibni te duek tih Omri te manghai.
Koma anthu otsatira Omuri anali amphamvu kupambana amene ankatsatira Tibini mwana wa Ginati. Choncho Tibini anafa ndipo Omuri anakhala mfumu.
23 Judah manghai Asa kah kum sawmthum kum khat vaengah, Omri loh Israel kum hlai nit a manghai thil tih Tirzah ah kum rhuk manghai.
Mʼchaka cha 31 cha Asa mfumu ya Yuda, Omuri anakhala mfumu ya Israeli, ndipo analamulira zaka 12 ndi miyezi isanu ndi umodzi ku Tiriza.
24 Shemer taengkah Samaria tlang te cak talent panit neh a lai. Tlang soah kho a thoong tih a thoong khopuei ming te tlang kah boei Shemer ming neh Samaria la a khue.
Iye anagula phiri la Samariya kwa Semeri pa mtengo wa ndalama 6,000 za siliva ndipo pa phiripo anamangapo mzinda, nawutcha Samariya, potsata dzina la Semeri, dzina la mwini wakale wa phirilo.
25 Omri loh BOEIPA mik ah boethae a saii tih amah hmai kah boeih lakah thae a huet.
Koma Omuri anachita zoyipa pamaso pa Yehova ndipo anachimwa kuposa mafumu ena onse amene analipo iye asanakhale mfumu.
26 Nebat capa Jeroboam kah longpuei neh anih kah tholhnah cungkuem dongah ni a. pongpa. Anih kah tholhnah loh Israel te a tholh sak tih amih kah a honghi neh Israel Pathen BOEIPA te a veet.
Pakuti iye anayenda mʼnjira zonse za Yeroboamu mwana wa Nebati, ndipo tchimo lake anachimwitsa nalo Aisraeli, nakwiyitsa Yehova Mulungu wa Israeli ndi mafano awo opandapake.
27 Omri kah ol noi a khueh te khaw, a thayung thamal neh a tueng sak te khaw, Israel manghai rhoek kah khokhuen olka cabu dongah a daek uh moenih a?
Tsono ntchito zina za Omuri ndi zamphamvu zimene anachita, kodi sizinalembedwe mʼbuku la mbiri ya mafumu a Israeli?
28 Omri te a napa rhoek taengla a khoem uh vaengah Samaria ah a up. Te phoeiah a capa Ahab te anih yueng la manghai.
Choncho Omuri anamwalira nayikidwa mʼmanda amene anayikidwa makolo ake ku Samariya. Ndipo Ahabu mwana wake analowa ufumu mʼmalo mwake.
29 Judah manghai Asa kah kum sawmthum kum rhet kum vaengah Omri capa Ahab te Israel soah manghai. Omri capa Ahab loh Samaria kah Israel soah kum kul kum nit a manghai thil.
Mʼchaka cha 38 cha ufumu wa Asa, mfumu ya Yuda, Ahabu mwana wa Omuri anakhala mfumu ya Israeli nalamulira Israeli ku Samariya zaka 22.
30 Omri capa Ahab loh anih hmai kah boeih lakah khaw BOEIPA mikhmuh ah boethae a saii.
Ahabu mwana wa Omuri anachita zoyipa zambiri pamaso pa Yehova kupambana mafumu onse akale.
31 Nebat capa Jeroboam kah tholhnah dongah a pongpa te phoeng a? A yuu te Sidoni manghai Ethbaal canu Jezebel te a loh. Cet bal tih Baal taengah tho a thueng tih a taengah bakop.
Iye sanachiyese ngati chinthu chochepa chabe kuchita machimo a Yeroboamu mwana wa Nebati, koma anakwatiranso Yezebeli, mwana wa Etibaala mfumu ya Asidoni, nayamba kutumikira Baala ndi kumupembedza.
32 Baal hamla hmueihtuk a suem pah tih Samaria ah Baal im a sak.
Iye anapangira Baala guwa lansembe mʼnyumba ya Baala imene anamanga ku Samariya.
33 Ahab loh Asherah a saii. A saii te khaw amah hmai kah aka om Israel manghai boeih lakah khaw Israel Pathen BOEIPA a veet te Ahab loh a koei.
Ahabu anapanganso fano la Asera ndi kukwiyitsa kwambiri Yehova Mulungu wa Israeli, kupambana mafumu onse a Israeli amene analipo iye asanakhale mfumu.
34 Anih tue vaengah Betheli Hiel loh Jerikho te a thoh. Nun capa Joshua kut ah a thui BOEIPA ol bangla a caming Abiram neh a toong tih a canoi Segub neh thohkhaih a pai sak.
Pa nthawi ya Ahabu, Hiyeli wa ku Beteli anamanganso mzinda wa Yeriko. Pa nthawi yomanga maziko ake, mwana wake woyamba wa mwamuna, Abiramu anamwalira, ndipo pa nthawi yomanga zipata zake, mwana wa mngʼono wa mwamuna Segubu, anamwaliranso. Izi zinachitika monga momwe Yehova ananenera kudzera mwa Yoswa mwana wa Nuni.