< Tihtuh 1 >
1 Pamhnama mpya ja Jesuh Khritawa ngsä kei Pawluh üngkhyüh ni. Kei cun Pamhnama xüa khyangea jumeinak jah kpüi lü mi ningsaw üng mi ngtheia ngthungtak üng jah cehpüi khaia na xü lü a na tüih ni.
Ndine Paulo, mtumiki wa Mulungu, ndi mtumwi wa Yesu Khristu. Ndinatumidwa kuti nditsogolere amene Mulungu anawasankha ku chikhulupiriro ndi ku chidziwitso cha choonadi chimene chimawafikitsa ku moyo wolemekeza Mulungu
2 Acun hin anglät xünnak, äpeinak am tüneiki ni. Akcün am a tünei ham üng käh hleikia Pamhnam naw ahina xünnak khyütam jah pe lü, (aiōnios )
ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios )
3 akcün apha law üng ania mawng cun jah mdanki. Ahin cun kei üng na ap lü jah küikyanki Pamhnam naw na sangsaki.
Pa nthawi yake Mulungu, Mpulumutsi wathu anawulula poyera mawu ake ndipo analamula kuti ndipatsidwe udindo wolalikira uthengawu.
4 Atänga mi tak jumnak am ka ca kcang Tihtuha vei ca ka yuki ni. Pa Pamhnam ja mi küikyan Bawi Khritaw Jesuh naw bäkhäknak ja dim’yenak ning pe se.
Kwa Tito, mwana wanga weniweni mʼchikhulupiriro cha ife tonse: Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate ndi Khristu Yesu Mpulumutsi wathu.
5 Mlüh naküta sangcim ngvaie jah mcawnki lü hlükaw hamkie na jah bilo khaia Kareta ka ning tak hüt ni. Ka ning mcuhmthehe jah süm bä:
Ndinakusiya ku Krete kuti ulongosole zonse zimene ndinazisiya zisanathe ndiponso usankhe akulu ampingo mʼmizinda yonse, monga momwe ndinakulamulira.
6 ngvai vai cun mkhye am ve yah, a khyu mat däk la yah khai. A cae pi jumei u lü pyen kpet lü am längang yah u.
Mkulu wampingo akhale munthu wopanda cholakwa, akhale wa mkazi mmodzi yekha, munthu amene ana ake ndi okhulupirira, osati amakhalidwe oyipa ndi osamvera.
7 Sangcim ngvai cun Pamhnama khut bikia kya lü mkhye kpuk vai am ve yah. Ani cun khyang hnepeiki, a mlung cähki, mpyüihmahki, sosatki ja ngui jawngnakia am thawn yah.
Popeza mkulu wa mpingo amayendetsa ntchito za banja la Mulungu, ayenera kukhala wopanda cholakwa, asakhale womva zayekha, kapena wopsa mtima msanga, kapena womwa zoledzeretsa, kapena wandewu, kapena wopeza phindu mwachinyengo.
8 Ani cun khinnglei khina lü akdaw cun kphya na yah khai. Ani cun amät nängeiki, ngsungki, ngcimki ja sitihkia pi kya yah khai.
Koma akhale wosamala bwino alendo, wokonda zabwino, wodziretsa, wolungama, woyera mtima ndi wosunga mwambo.
9 Ningsaw naw a ä a jum phyakia mawng cän akceta kcüng yah khai. Acun ngtek püikie khyeki ti cun mdan lü mtheimthangnak akcang am khyang kcee pi ngjuktha jah pe thei yah khai.
Iye ayenera kugwiritsa mawu okhulupirika monga tinaphunzitsira, kuti athe kulimbikitsa ena ndi chiphunzitso choona ndiponso kugonjetsa amene atsutsana nacho.
10 Aktunga Judah ning üngkhyüh ngthunghlai law lü ia am ngtähngkhehki ami ksingnak am khyang jah mhlei u lü jah thühlawksaki khawhah vekie.
Paja pali anthu ambiri osaweruzika, makamaka mʼgulu la anthu a mdulidwe, oyankhula nkhani zopanda pake ndi kusocheretsa anzawo.
11 Ami pyensak jah him vai hlü ve, isetiakyaküng, ngkeeikse ngui yahnak vai mkhüh na u lü am ami jah mthei vai jah mthei lü imkyawnge jah uplatsakie ni.
Ayenera kuletsedwa kuyankhula chifukwa akusokoneza mabanja athunthu pophunzitsa zinthu zomwe sayenera kuwaphunzitsa. Iwo amachita izi kuti apeze ndalama mwachinyengo.
12 Karete üngka khyang mat amimäta sahmae naw, “Karet khyange cun hleihlakie, khyükseia kba se u lü dudam u lü eiawk kthanakie,” tia a pyen hin kcangki ni. Ahina phäh akdawa jumnak ami tak law vaia, angkhat kunga jah mcing lü
Mneneri wina, mmodzi wa iwo omwewo anati, “Akrete nthawi zonse ndi amabodza, akhalidwe loyipitsitsa ndiponso alesi adyera.”
Mawu amenewa ndi woona. Nʼchifukwa chake, uwadzudzule mwamphamvu, kuti akhale ndi chikhulupiriro choona,
14 ngthungtak mahki khyange üngkhyüh lawkia nghngicima ngthupete ja Judahea khuikame käh jah ngai ti khaie.
kuti asasamalenso nthano za Chiyuda, ndi malamulo a anthu amene akukana choonadi.
15 Amimät ngcimki hea phäh anaküt hin ngcim lü ami mlungkyawng ja amimät ksingeinak am ngcim lü am ami jumeia phäh avan hin am ngcim.
Kwa oyera mtima, zinthu zonse ndi zoyera, koma kwa amene ndi odetsedwa ndi osakhulupirira, palibe kanthu koyera. Kunena zoona, mitima yawo ndi chikumbumtima chawo, zonse nʼzodetsedwa.
16 Pamhnam ksingkiea pyen u lüpi ami vecawh naw kpetki. Amimi cun pyen am ngai lü jah cawkei phyakia kya lü akdaw pawh khaia am nglawi u.
Iwo amati amadziwa Mulungu, pamene ndi zochita zawo amamukana. Ndi anthu onyansa ndi osamvera, ndi osayenera kuchita kalikonse kabwino.