< Zekariya 1 >
1 Mwezi wachisanu ndi chitatu, mʼchaka chachiwiri cha ulamuliro wa Dariyo, Yehova anayankhula ndi mneneri Zekariya mwana wa Berekiya, mwana wa Ido, kuti:
Oubi godo amola ode ageyadu amo Da: liase ea Besia sogega ouligisu hou amoga, Hina Gode da amo sia: ne iasu amo Segalaia (Belegaia egefe amola Idou ea aowa) ema i.
2 “Yehova anakwiya kwambiri ndi makolo anu.
Hina Gode Bagadedafa da Segalaiama amo sia: Ea fi dunu ilima alofele olelema: ne sia: i, “Na, Hina Gode, da dilia aowalali ilima bagadewane ougi galu.
3 Choncho awuze anthuwa kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Bwererani kwa Ine,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse. ‘Ndipo Ine ndidzabwerera kwa inu,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Be wali Na da dilima sia: sa, ‘Nama buhagima! Amasea, Na da dilima bu misunu!
4 Musakhale ngati makolo anu, amene aneneri akale anawalalikira kuti: Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Tsopano lekani njira zanu zoyipa ndi machitidwe anu oyipawo.’ Koma iwo sanamvere kapena kulabadira za Ine, akutero Yehova.
Dilia aowalali ilia hou agoane mae hamoma. Hemonega, balofede dunu da Na sia: ne iasu ilima i. Ilia da wadela: i hou fisimusa: ilima sia: i. Be ilia da Na sia: hamedafa nabi amola Na hamoma: ne sia: be nabawane hame hamosu.
5 Kodi makolo anuwo ali kuti tsopano? Nanga aneneri, kodi amakhalapo mpaka muyaya?
Dia aowalali amola amo balofede huluane ilia da bogoi dagoi.
6 Kodi mawu anga ndi malangizo anga, amene ndinawawuza atumiki anga aneneri, suja anawachitira makolo anu? “Tsono iwo analapa ndi kunena kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse watichitira zomwe zikuyenera njira zathu ndi machitidwe athu, monga anatsimikiza kuti adzachita.’”
Na hawa: hamosu balofede dunu amo ilimadi, Na da dilia aowalali ilima hamoma: ne sia: i amola sisasu dawa: digima: ne sia: ne i. Be ilia amo sia: mae nabane, se dabe lai dagoi. Amalalu, ilia da bu sinidigili, amo Na, Hina Gode Bagadedafa, da ilia hamoi defele amola Na ilegei defele, se dabe ilima i, amo da dafawane ilia da sia: i dagoi.”
7 Tsiku la 24 la mwezi wa 11, mwezi wa Sebati, chaka chachiwiri cha ulamuliro wa Dariyo, Yehova anayankhula ndi Zekariya mwana wa Berekiya, mwana wa Ido.
Eso 24 amola oubi gidayale (oubi Siba: de) amola ode ageyadu Da: liase ea Besia soge ouligisu amoga, Hina Gode da gasi afaega nama esala ba: su iasi.
8 Nthawi ya usiku ndinaona masomphenya. Ndinaona munthu atakwera pa kavalo wofiira. Iye anayima pakati pa mitengo ya mchisu mʼchigwa. Kumbuyo kwake kunali akavalo ofiira, akhofi ndi oyera.
Na da ba: loba, Hina Gode Ea a: igele dunu yoi hosi da: iya fila heda: le ahoanebe ba: i. E da ‘medele’ ifa labala fago, amo ganodini aliligibi ba: i. Ea baligia hosi eno, mogili yoi, mogili hoholei, mogili ahea: iai, lelebe ba: i.
9 Ine ndinafunsa kuti, “Mbuye wanga, kodi zimenezi ndi chiyani?” Mngelo amene amayankhula nane anayankha kuti, “Ndidzakuonetsa kuti zimenezi ndi chiyani.”
Na da ema adole ba: i, “Hina! Amo hosi ilia bai da adi olelesala: ?” E bu adole i, “Na da dima amo ea bai olelemu!
10 Pamenepo munthu amene anayima pakati pa mitengo ya mchisu anafotokoza kuti, “Amenewa ndiwo amene Yehova wawatuma kuti ayendere dziko lonse lapansi.”
Hina Gode da ili osobo bagade hou abodelalu masa: ne asunasi.”
11 Ndipo okwera pa akavalo enawo anafotokoza kwa mngelo wa Yehova, amene anayima pakati pa mitengo ya mchisu kuti, “Ife tayendera dziko lonse lapansi ndipo tapeza kuti dziko lonselo lili pa bata ndi mtendere.”
Hosi ilia da a: igele dunuma amane sia: ne i, “Ninia da osobo bagade huluane hohogola lalu. Ninia da ba: loba, osobo bagade fifi asi gala dunu huluane da gasa hamedene amola banenesi dagoi ba: i.”
12 Tsono mngelo wa Yehova anati, “Yehova Wamphamvuzonse, kodi mpaka liti mudzakhala osaonetsa chifundo chanu kwa Yerusalemu ndi mizinda ya Yuda, amene mwawakwiyira kwa zaka izi 70?”
Amalalu, a:igele dunu da amane sia: i, “Hina Gode Bagadedafa! Di da waha ode 70 agoane, Yelusaleme fi amola Yuda moilai bai bagade hamone gagai fi ilima ougi galu. Di da habogala ilima asigi hou bu olelema: bela: ?”
13 Choncho Yehova anayankhula mawu abwino ndi achitonthozo kwa mngelo amene ankayankhula nane.
Hina Gode da a: igele dunu ea dogo denesima: ne, ema dabe adole i.
14 Pamenepo mngelo amene ankayankhula nane anati, “Lengeza mawu awa: Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Ine ndikuchitira nsanje Yerusalemu ndi Ziyoni,
Amola a: igele da nama Hina Gode Bagadedafa Ea sia: i amo sisia: i lama: ne amane sia: i, “Na da Yelusaleme, Na Hadigi Moilai bai bagade, amoma bagade fofagisa.
15 koma ndakwiya kwambiri ndi anthu a mitundu ina amene akuganiza kuti ali pa mtendere. Ndinakwiyira anthu anga pangʼono pokha, koma iwo anawonjeza kuzunza anthu angawo.’
Amola, Na da ilima ha lai fifi asi gala amo da hahawane amola olofole esala, ilima bagadewane ougi. Na da Na fi dunuma fonobahadi ougiba: le, ilima se dabe i. Na da eno fifi asi gala dunuma amo hamoma: ne sia: beba: le, ilia da Na fi dunuma gegebeba: le, ilima se bagade i. Be ilia da Na hamoma: ne sia: i baligili, Na fi dunuma se baligili i.
16 “Choncho, Yehova akuti, ‘Ndidzabwerera ku Yerusalemu ndi mtima wachifundo, nyumba yanga adzayimanganso kumeneko. Ndipo adzatenganso chingwe choyezera kuti amange Yerusalemu,’ akutero Yehova Wamphamvuzonse.
Amaiba: le, Na da Yelusaleme fi ilima asigi hou olelema: ne, Yelusalemega buhagi. Na Debolo da bu hahamoi amola Yelusaleme moilai bai bagade da bu buga: le gagui dagoi ba: mu.”
17 “Lengezanso kuti, Yehova Wamphamvuzonse akuti, ‘Mizinda yanga idzakhalanso ndi zokoma zosefukira ndipo Yehova adzatonthoza Ziyoni ndi kusankhanso Yerusalemu.’”
Amola a: igele da nama na da eno sisia: i lama: ne amane sia: i, “Hina Gode Bagadedafa da amane sia: sa, ‘Na moilai bai bagade ilia da bu bagade gagui ba: mu. Amola Na da Yelusaleme fi bu fidimu amola Yelusaleme da Na moilai bai bagadedafa Na da bu sia: mu.’”
18 Kenaka ndinayangʼananso, ndipo patsogolo panga panali nyanga zinayi.
Esala ba: su eno ganodini, na da bulamagau hono biyaduyale ba: i.
19 Ndinamufunsa mngelo amene amayankhula nane kuti, “Kodi zimenezi ndi chiyani?” Iye anandiyankha kuti, “Izi ndi nyanga zimene zinabalalitsa Yuda, Israeli ndi Yerusalemu.”
Na da a: igele dunu (amo da nama sia: dasu) ema amane adole ba: i, “Amo hono ilia bai da adila: ?” E da nama bu adole i, “Ilia bai da gasa bagade fifi asi gala amo da Yuda, Isala: ili amola Yelusaleme amo fi dunu afagogolesi dagoi.”
20 Kenaka Yehova anandionetsa amisiri azitsulo anayi.
Amalalu, Hina Gode da ha: ma gagui hawa: hamosu dunu biyaduyale nama olei.
21 Ndinafunsa kuti, “Amisiri a zitsulowa akudzachita chiyani?” Iye anayankha kuti, “Izi ndi nyanga zimene zinabalalitsa Yuda kotero kuti panalibe wina amene akanalimbana nazo, koma amisiri a zitsulowa abwera kudzaziopseza ndi kugwetsa nyanga zimenezi za mitundu ya anthu amene analimbana ndi dziko la Yuda ndi kubalalitsa anthu ake.”
Na da amane adole ba: i, “Amo dunu ilia adi hamomusa: misibala: ? E da dabe adole i,” Fifi asi gala ha lai dunu ilia da Yuda fi dunu hasalasili, afagogolesi. Ha: ma gagui dunu da amo ha lai fifi asi gala amo beda: ma: ne hamone, hasalasimusa: misi dagoi.”