< Zekariya 14 >
1 Taonani tsiku la Yehova likubwera pamene zinthu zimene adani ako anakulanda azidzagawana iwe ukuona.
BOEIPA kah khohnin lo li coeng ke. Te dongah na khui ah na kutbuem a tael pawn ni.
2 Ndidzasonkhanitsa anthu a mitundu yonse kuti adzathire nkhondo Yerusalemu; mzindawu udzalandidwa, nyumba zidzaphwasulidwa, ndipo akazi adzagwiriridwa. Theka la anthu a mu mzindamu lidzapita ku ukapolo, koma ena onse otsala mu mzindamu sadzachotsedwa.
Te dongah namtom boeih te caemtloek ham Jerusalem la ka coi ni. Khopuei te a loh vetih im a reth uh ni. Huta te a yalh rhoe a yalh puei uh vetih khopuei rhakthuem vangsawn la a khuen ni. Tedae pilnam kah a coih tah khopuei lamloh khoe mahpawh.
3 Pamenepo Yehova adzabwera kudzamenyana ndi mitundu ya anthu imeneyi, ngati mmene amachitira pa nthawi ya nkhondo.
Te phoeiah BOEIPA te cet vetih namtom te a tloek ni. Te tlam ni caemrhal hnin ah tah a vathoh hnin kah bangla om ni.
4 Tsiku limenelo adzayimirira pa Phiri la Olivi, kummawa kwa Yerusalemu, ndipo Phiri la Olivilo lidzagawikana pawiri kuyambira kummawa mpaka kumadzulo, kupanga chigwa chachikulu, kuchititsa kuti theka la phiri lisunthire kumpoto ndi linalo kummwera.
Te khohnin ah tah khothoeng neh Jerusalem dan kah olive tlang ah a kho neh pai ni. Olive tlang a rhakthuem ah khocuk lamloh khotlak duela rhek ni. Kolrhawk te bahoeng len ni. Tlang rhakthuem te tlangpuei la, a rhakthuem te tuithim la nong ni.
5 Inu mudzathawa podzera mʼchigwa chapakati pa phirilo, pakuti chidzafika mpaka ku Azeli. Mudzathawa monga munachitira pa tsiku la chivomerezi nthawi ya Uziya mfumu ya Yuda. Kenaka Yehova Mulungu wanga adzabwera, pamodzi ndi oyera ake onse.
Azel duela tlang kol a pha ham dongah ka tlang kol la na rhaelrham uh ni. Judah manghai Uzziah tue ah lingluei hmai lamloh na rhaelrham bangla na rhaelrham uh ni. Te vaengah ka Pathen BOEIPA tah hlangcim boeih neh nang taengla halo ni.
6 Tsiku limenelo sipadzakhala kuwala, kuzizira kapena chisanu.
Te khohnin a pha vaengah khosae neh tuikhal dingsuk khaw om sut mahpawh.
7 Lidzakhala tsiku lapaderadera, silidzakhala usana kapena usiku; tsiku limeneli akulidziwa ndi Yehova yekha. Ikadzafika nthawi ya madzulo, kudzakhala kukuwalabe.
Te vaengah khohnin pakhat ni a om eh. Te te BOEIPA loh a ming coeng. Khothaih moenih, khoyin bal moenih. Hlaem tue a pha vaengah khaw vangnah om ni.
8 Tsiku limenelo madzi amoyo adzatuluka mu Yerusalemu, theka lidzapita ku nyanja ya kummawa ndipo theka lina ku nyanja ya kumadzulo, nthawi yachilimwe ndi nthawi yozizira yomwe.
Te khohnin a pha vaengah Jerusalem lamloh tui hing long vetih a rhakthuem te khocuk tuitunli la, a rhakthuem te khobawt tuitun la, khohal ah khaw, sikca ah khaw om ni.
9 Ndipo Yehova adzakhala mfumu pa dziko lonse lapansi. Tsiku limenelo padzakhala Ambuye mmodzi yekha, ndipo dzina lidzakhala limodzi lomwelo.
Te vaengah Yahweh tah diklai pum kah manghai la om ni. Te khohnin ah tah Yahweh pakhat bueng ni a ming a om eh.
10 Dziko lonse, kuyambira ku Geba mpaka ku Rimoni, kummwera kwa Yerusalemu, lidzakhala ngati Araba. Koma Yerusalemu adzakwezedwa ndipo adzakhala pamalo pakepo, kuyambira ku Chipata cha Benjamini mpaka ku malo amene ali ku Chipata Choyamba, ku Chipata Chapangodya, ndipo kuyambira ku Nsanja ya Hananeli mpaka ku malo opsinyira mphesa za mfumu.
Geba lamloh Jerusalem tuithim Rimmon hil, khohmuen boeih he kolken la poeh ni. Tedae Benjamin vongka lamloh lamhma vongka hmuen hil, bangkil vongka neh Hananel rhaltoengim kah manghai va-am hil tah a tai vetih amah hmuen la kho a sak ni.
11 Mʼmenemo mudzakhala anthu; sadzawonongedwanso. Yerusalemu adzakhala pa mtendere.
A khuikah khosa rhoek khaw yaehtaboeih la om voel pawt vetih Jerusalem khaw ngaikhuek la kho a sak ni.
12 Mliri umene Yehova adzakanthire nawo mitundu yonse ya anthu imene inkamenyana ndi Yerusalemu ndi uwu: Matupi awo adzawola iwo eni akuyenda, maso awo adzawola ali mʼmalo mwake, ndipo malilime awo adzawola ali mʼkamwa mwawo.
Te vaengah lucik pai ni. Jerusalem aka muk pilnam boeih te BOEIPA loh a yawk sak ni. A kho dongah a pai pangthuem a saa rhong vetih a mik khaw a khui ah rhong ni. A ka dongah a lai khaw rhong ni.
13 Pa tsiku limenelo Yehova adzasokoneza anthu akuluakulu. Munthu aliyense adzagwira dzanja la mnzake, ndi kuyamba kumenyana okhaokha.
Te khohnin a pha vaengah BOEIPA kah soekloeknah te amih taengah muep pai ni. Hlang loh a hui kah kut a hlaengtang vetih a kut loh a hui kah kut te a cuk thil ni.
14 Yuda nayenso adzachita nkhondo ku Yerusalemu. Chuma chonse cha anthu a mitundu yozungulira adzachisonkhanitsa pamodzi; golide, siliva ndi zovala zochuluka kwambiri.
Judah khaw Jerusalem ah a tloek vetih kaepvai namtom cungkuem kah thadueng te a coi ni. Sui khaw, cak himbai khaw muep cungkuem ni.
15 Mliri womwewo udzapha akavalo ndi nyulu, ngamira ndi abulu, pamodzi ndi nyama zonse zokhala ku misasako.
Marhang, muli-marhang, kalauk neh laak kah lucik om ni. He lucik bang he rhaehhmuen ah aka om rhamsa boeih soah khaw om ni.
16 Kenaka opulumuka ochokera mwa mitundu yonse ya anthu amene anathira nkhondo Yerusalemu, azidzapita chaka ndi chaka kukapembedza Mfumu Yehova Wamphamvuzonse, ndiponso kukachita Chikondwerero cha Misasa.
Jerusalem la aka kun namtom cungkuem lamkah aka sueng boeih khaw om vetih kum khat kah kum a toep vaengah caempuei manghai Yahweh bawk ham neh pohlip khotue lam hamla cet uh ni.
17 Ngati mitundu ina ya anthu pa dziko lapansi sidzapita ku Yerusalemu kukapembedza Mfumu Yehova Wamphamvuzonse, idzakhala wopanda mvula.
Diklai koca lamlong tah caempuei manghai BOEIPA te bawk ham Jerusalem la cet pawt khaming. Te vaengah amih hamla khonal om mahpawh.
18 Ndipo ngati anthu a ku Igupto sadzapita ndi kukakhala nawo kumeneko, adzakhala wopanda mvula. Yehova adzabweretsa pa iwo mliri umene analangira mitundu ina ya anthu imene sinapite ku Chikondwerero cha Misasa.
Egypt koca tah cet pawt tih mop pawt mai ni. Te vaengah amih soah lucik om het mahpawt a? Te nen ni pohlip khotue lam hamla aka cet pawh namtom te BOEIPA loh a yawk sak.
19 Chimenechi chidzakhala chilango cha Igupto ndiponso mitundu ina yonse imene sidzapita ku Chikondwerero cha Misasa.
Pohlip khotue lam hamla aka cet pawh Egypt kah tholhnah phu neh namtom boeih kah tholhnah phu la om ni.
20 Pa tsiku limenelo pa maberu a akavalo padzalembedwa mawu oti wopatulikira Yehova, ndipo miphika ya mʼNyumba ya Yehova idzakhala yopatulika ngati mbale za ku guwa.
Te khohnin ah tah marhang rhaloeng dongah khaw, BOEIPA K AH C IMCAIHNAH om vetih BOEIPA im kah umam khaw hmueihtuk hmai kah baelcak bangla om ni.
21 Mʼphika uliwonse ku Yerusalemu ndi ku Yuda udzakhala wopatulikira Yehova Wamphamvuzonse, ndipo onse amene adzabwera kudzapereka nsembe adzatenga miphika ina ndi kuphikiramo. Ndipo nthawi imeneyo simudzakhalanso Akanaani mʼNyumba ya Yehova Wamphamvuzonse.
Jerusalem ah khaw, Judah ah khaw umam boeih dongah caempuei BOEIPA kah cimcaihnah om ni. Aka nawn boeih khaw kun uh vetih amamih lamkah a khuen uh te amah ah a thong uh ni. Te khohnin ah tah caempuei BOEIPA im ah Kanaan hnoyoi om voel mahpawh.