< Zekariya 12 >

1 Uthenga wa Yehova kwa Israeli. Yehova, amene amayala mlengalenga, amene amayika maziko a dziko lapansi, ndiponso amene amalenga mzimu wokhala mwa munthu, akunena kuti,
Umthwalo welizwi leNkosi ngoIsrayeli, itsho INkosi, eyelula amazulu, yabeka isisekelo somhlaba, yadala umoya womuntu ngaphakathi kwakhe:
2 “Taonani, ndidzasandutsa Yerusalemu kukhala chakumwa choledzeretsa chimene chidzasokoneza mitundu yonse ya anthu yomuzungulira. Yuda adzazingidwa pamodzinso ndi Yerusalemu.
Khangela, ngizakwenza iJerusalema ibe yinkezo yokudengezelisa kubo bonke abantu abazingelezeleyo; yebo, izakuba laphezu kukaJuda ekuvinjezelweni kumelene leJerusalema.
3 Pa tsiku limenelo, pamene mitundu yonse ya anthu a dziko lapansi idzasonkhana kulimbana naye, ndidzasandutsa Yerusalemu thanthwe losatheka kusunthidwa ndi mitundu yonse ya anthu. Onse oyesa kumusuntha adzadzipweteka.
Kuzakuthi-ke ngalolosuku ngenze iJerusalema ibe yilitshe elingumthwalo kubo bonke abantu; bonke abazithwalisa ngalo bazaqunywa lokuqunywa; labo bonke abantu bomhlaba bazabuthana bemelene layo.
4 Pa tsiku limenelo kavalo aliyense ndidzamuchititsa mantha kuti asokonezeke, ndipo wokwerapo wake ndidzamuchititsa misala,” akutero Yehova. “Ndidzayangʼanira nyumba ya Yuda koma ndidzachititsa khungu akavalo onse a anthu a mitundu ina.
Ngalolosuku, itsho iNkosi, ngizatshaya lonke ibhiza ngokudideka, lomgadi walo ngobuhlanya, ngivule amehlo ami phezu kwendlu kaJuda, ngitshaye lonke ibhiza lezizwe ngobuphofu.
5 Pamenepo atsogoleri a Yuda adzayankhula mʼmitima mwawo kuti, ‘Anthu a ku Yerusalemu ndi amphamvu, chifukwa Yehova Wamphamvuzonse ndiye Mulungu wawo.’
Khona ababusi bakoJuda bazakutsho enhliziyweni yabo: Abahlali beJerusalema bangamandla ami eNkosini yamabandla uNkulunkulu wabo.
6 “Pa tsiku limenelo ndidzasandutsa atsogoleri a Yuda kukhala ngati mbawula yotentha pakati pa nkhuni, ngati sakali yoyaka pa mitolo ya tirigu. Adzatentha mitundu yonse ya anthu yowazungulira, kumanja ndi kumanzere, koma Yerusalemu sadzasuntha pa malo ake.
Ngalolosuku ngizakwenza ababusi bakoJuda babe njengembawula yomlilo phakathi kwezigodo, lanjengesihlanti somlilo esithungweni; njalo bazaqeda ngakwesokunene langakwesokhohlo bonke abantu inhlangothi zonke; iJerusalema-ke izahlalwa futhi endaweni yayo eJerusalema.
7 “Yehova adzapulumutsa malo okhala Yuda poyamba, kuti ulemu wa nyumba ya Davide ndi wa anthu okhala mu Yerusalemu usapambane ulemu wa Yuda.
Futhi iNkosi izasindisa amathente akoJuda kuqala, ukuze udumo lwendlu kaDavida lodumo lwabakhileyo beJerusalema lungazikhulisi lumelene loJuda.
8 Pa tsiku limenelo Yehova adzatchinjiriza onse okhala mu Yerusalemu, kotero kuti anthu ofowoka kwambiri pakati pawo adzakhala ngati Davide, ndipo nyumba ya Davide idzakhala ngati Mulungu, ngati mngelo wa Yehova wowatsogolera.
Ngalolosuku iNkosi izavikela abakhileyo beJerusalema; lalowo obuthakathaka phakathi kwabo ngalolosuku abe njengoDavida; lendlu kaDavida ibe njengoNkulunkulu, njengengilosi yeNkosi phambi kwabo.
9 Pa tsiku limenelo ndidzawononga mitundu yonse yofuna kuthira nkhondo Yerusalemu.
Kuzakuthi-ke ngalolosuku ngidinge ukuchitha zonke izizwe eziza ukumelana leJerusalema.
10 “Ndipo pa nyumba ya Davide ndi pa anthu okhala mu Yerusalemu ndidzakhuthulirapo mzimu wachisomo ndi wopemphera. Iwo adzandiyangʼana Ine, amene anamubaya, ndipo adzamulirira kwambiri monga momwe munthu amalirira mwana wake mmodzi yekhayo, ndiponso adzamva chisoni kwambiri monga momwe amachitira ndi mwana woyamba kubadwa.
Njalo ngizathululela phezu kwendlu kaDavida laphezu kwabahlali beJerusalema umoya womusa lowokuncenga, njalo bazangikhangela mina abamgwazayo, bamlilele, njengokulilela indodana eyodwa, abe lobuhlungu ngayo, njengobuhlungu ngezibulo.
11 Pa tsiku limenelo mudzakhala kulira kwakukulu mu Yerusalemu, monga kulira kwa ku Hadadi-Rimoni ku chigwa cha Megido.
Ngalolosuku kuzakuba kukhulu ukulila eJerusalema, njengokulila kukaHadadirimoni esigodini seMegidoni.
12 Dziko lidzalira kwambiri, fuko lililonse pa lokha, akazi awo pa okhanso: fuko la Davide pamodzi ndi akazi awo, fuko la Natani pamodzi ndi akazi awo,
Futhi ilizwe lizalila, usapho ngosapho lulodwa, usapho lwendlu kaDavida lulodwa, labafazi babo bebodwa; usapho lwendlu kaNathani lulodwa, labafazi babo bebodwa;
13 nyumba ya Levi pamodzi ndi akazi awo, fuko la Simei pamodzi ndi akazi awo,
usapho lwendlu kaLevi lulodwa, labafazi babo bebodwa; usapho lukaShimeyi lulodwa, labafazi babo bebodwa;
14 ndiponso mafuko onse pamodzi ndi akazi awo.
zonke izinsapho eziseleyo, usapho ngosapho lulodwa, labafazi babo bebodwa.

< Zekariya 12 >