< Tito 1 >

1 Ndine Paulo, mtumiki wa Mulungu, ndi mtumwi wa Yesu Khristu. Ndinatumidwa kuti nditsogolere amene Mulungu anawasankha ku chikhulupiriro ndi ku chidziwitso cha choonadi chimene chimawafikitsa ku moyo wolemekeza Mulungu
li tiline tie Pɔl n tena, wani tie U tienu Tuosɔnlo yen Jesu ŋɔtielo, yaab k U tienu lukdbi. O den lukd minn k n coanbi U tienu dandaanl ni yen k go waanbi mumuni kul tunda yal tie ti dandanlepo.
2 ndi kuwapatsa chiyembekezo cha moyo wosatha, umene Mulungu amene sanama, analonjeza nthawi isanayambe. (aiōnios g166)
Yen lan fidi bin yaa pia ya mial kaan gbeni. Ya Tienu k puɔ faag den puon ti yal mieli kaan gbel haali yoknu. (aiōnios g166)
3 Pa nthawi yake Mulungu, Mpulumutsi wathu anawulula poyera mawu ake ndipo analamula kuti ndipatsidwe udindo wolalikira uthengawu.
O yogn den pudi, Pɔl den waano omaam yen olabaal moni yaal ke o den teni, yeni U tienu yaa palopo yuaan ti Fietua.
4 Kwa Tito, mwana wanga weniweni mʼchikhulupiriro cha ife tonse: Chisomo ndi mtendere zochokera kwa Mulungu Atate ndi Khristu Yesu Mpulumutsi wathu.
N fuoda, Tidi n big buaadi kiti ya dendalin: N Jaandi k U tienu t baa yen Yesu Kristu ti Fietua n tena o ŋalebalk yen n yanduam.
5 Ndinakusiya ku Krete kuti ulongosole zonse zimene ndinazisiya zisanathe ndiponso usankhe akulu ampingo mʼmizinda yonse, monga momwe ndinakulamulira.
N den ŋaaŋaan Kreti dogoon yen lan fidi naan jodi letuol ki guani k bobni dogu kuli jandierin liga jabaa yen min den waan maanma. b
6 Mkulu wampingo akhale munthu wopanda cholakwa, akhale wa mkazi mmodzi yekha, munthu amene ana ake ndi okhulupirira, osati amakhalidwe oyipa ndi osamvera.
L buɔl k ligi yaaba kul lin yaa pia ya yeyienu ŋaan yen waan da tie ncocom. li boal k be yaan firi daan o bilaa po, o bilaa yeyenu lin yaa ŋaan cien k go yaa ŋaam jini bibaa.
7 Popeza mkulu wa mpingo amayendetsa ntchito za banja la Mulungu, ayenera kukhala wopanda cholakwa, asakhale womva zayekha, kapena wopsa mtima msanga, kapena womwa zoledzeretsa, kapena wandewu, kapena wopeza phindu mwachinyengo.
L yaapo, li buɔl ki jandiogu ligi yua da pia nangma, kelima o tie U tien deni liga yua. li ya po cedi ko ka tie yoa pia bidi onini ba pibinli, okan ya tie dañulo, likonkonl dano. Ki da pia ya bona k coyeni efe.
8 Koma akhale wosamala bwino alendo, wokonda zabwino, wodziretsa, wolungama, woyera mtima ndi wosunga mwambo.
wan ya tie o cangalo, o ŋanmu yadonl, o baa tie yoa ŋaam maali, k tuoli ŋani, o yeyinnu kaan pia jɔgnd ki go ya tie yoa cɔln oba.
9 Iye ayenera kugwiritsa mawu okhulupirika monga tinaphunzitsira, kuti athe kulimbikitsa ena ndi chiphunzitso choona ndiponso kugonjetsa amene atsutsana nacho.
wan ŋami k ya kubi labal ŋamo ya nanani ban den tundo yalaa. Li ya po obaa fidi k ya pagdii olieba nani atud ŋamaa ki yie yala k tie lani.
10 Paja pali anthu ambiri osaweruzika, makamaka mʼgulu la anthu a mdulidwe, oyankhula nkhani zopanda pake ndi kusocheretsa anzawo.
Kelima bocienli yie ke bi kaan coɔl U tienu mumuni. Bi ŋmand bi nuba yula k baan yaa ŋoa yala tie b ma faagu. Ti la binubanii bocienl ñaani Jufi yaaba ni.
11 Ayenera kuletsedwa kuyankhula chifukwa akusokoneza mabanja athunthu pophunzitsa zinthu zomwe sayenera kuwaphunzitsa. Iwo amachita izi kuti apeze ndalama mwachinyengo.
L buɔli ki nan munni bi ñanaa, kelima bi gulg ti diedi kul k moandi yalan kii bual, kelima bi kpaan ne ligi.
12 Mneneri wina, mmodzi wa iwo omwewo anati, “Akrete nthawi zonse ndi amabodza, akhalidwe loyipitsitsa ndiponso alesi adyera.”
Kreti yaaba den pia yoa k bi den yio sawal pual, O madi; k bi yaa nubaa tie faodanba, Bi tie ya yandi bia, yen ajidiciama yen bi kpaljidaanba.
13 Mawu amenewa ndi woona. Nʼchifukwa chake, uwadzudzule mwamphamvu, kuti akhale ndi chikhulupiriro choona,
Didi mani ya bubud ŋan: L buɔl k yin yaa ŋaanm jalgbi yen ban fid i ki ya pia li dandanl ŋanli.
14 kuti asasamalenso nthano za Chiyuda, ndi malamulo a anthu amene akukana choonadi.
ki baan da ŋoan Juifbaa maam yeni ya yikodi ki bi nub biliki fidi ki ŋmagdi binubi yaal tie mumuni.
15 Kwa oyera mtima, zinthu zonse ndi zoyera, koma kwa amene ndi odetsedwa ndi osakhulupirira, palibe kanthu koyera. Kunena zoona, mitima yawo ndi chikumbumtima chawo, zonse nʼzodetsedwa.
“yen yaa ba ŋam ŋani O tienu, lekul ŋani” ama ya nuba pia ti jɔkn yen n kan daama. Ba pu k ŋani bi nugani. Bi malma yen bi yan jagli kul jognoo.
16 Iwo amati amadziwa Mulungu, pamene ndi zochita zawo amamukana. Ndi anthu onyansa ndi osamvera, ndi osayenera kuchita kalikonse kabwino.
L ya po b mɔdo made k bi ban O tienu, ama bi yeyienu k ta yen O tien maam. Kelima nul ki buabi yen bi kan fedi suan tuol ŋanl ba kul.

< Tito 1 >