< Nyimbo ya Solomoni 7 >
1 Iwe namwali waufumu, mapazi ako ngokongola mu nsapato wavalazo! Ntchafu zako nʼzowumbika bwino ngati miyala yamtengowapatali, ntchito ya manja ya mmisiri waluso.
“Di da a: fini ida: iwanedafa. Dia emo, dia emo salasu ganodini da isisima: goi ba: sa. Dia masele dalegala: i da fedege liligi hahamosu dawa: dui dunu ea hamosu defele gala.
2 Mchombo wako uli ngati chikho chowumbika bwino chimene nthawi zonse ndi chodzaza ndi vinyo. Chiwuno chako ndi choningʼa ngati mtolo wa tirigu utazunguliridwa ndi maluwa okongola.
Dia semogofo da ononoi faigelei waini hanoga nabane, ebelemu da hamedei agoane ba: sa. Dia bulu ga: su da widi dabosu amo ‘lili’ mosoi amoga bului agoai ba: sa.
3 Mawere ako akuoneka ngati ana awiri a mbawala, ngati mphoyo zamapasa.
Dia dodo da ‘dia’ ohe aduna lalelegei amola ‘gasele dia’ aduna agoane ba: sa.
4 Khosi lako lili see! ngati nsanja ya mnyanga wa njovu. Maso ako ali ngati mayiwe a ku Hesiboni, amene ali pafupi ndi chipata cha Bati Rabimu. Mphuno yako ili ngati nsanja ya ku Lebanoni, yoyangʼana ku Damasiko.
Dia galogoa da ‘aifoli’ diasu sedade gagagula heda: i agoane ba: sa. Dia si elea da hano wayabo Hesiabone moilai bai bagade amo ea logo holei gadenene diala, agoai ba: sa. Dia mi da Lebanone diasu sedade gagagula heda: i amo da Dama: sagase moilai bai bagadega, sosodo aligisu dunu amo moilai ouligimusa: esaloma: ne gagui, agoaiwane noga: idafa ba: sa.
5 Mutu wako uli bwinobwino nengʼaa ngati phiri la Karimeli. Tsitsi lako lili ngati nsalu yakuda yaufumu; mfumu yakopeka ndi maonekedwe ake okongola.
Gamele Goumi da gadodafa agoai, di da dia dialuma gadoba: le gadole ahoa. Dia dialumasa da ‘sa: dini’ abula ea ela: mai agoai ba: sa. Ea isisima: goi da hina bagade gagulaligimu defele gala.
6 Ndiwe wokongola kwambiri ndiponso wosangalatsa, iwe wokondedwa, namwali wokondweretsawe!
Di da isisima: goidafa! Dia noga: idafa sasagesu hou amo da dunu gumima: ne agoane hamosa.
7 Msinkhu wako uli ngati mtengo wa mgwalangwa, ndipo mawere ako ali ngati phava la zipatso.
Di da gumudi ifa agoane, da: da: lole ahoa. Dia dodo da dadi fage sosogoi agoane ba: sa.
8 Ndinati, “Ndikwera mtengo wa mgwalangwa; ndidzathyola zipatso zake.” Mawere ako ali ngati maphava a mphesa, fungo la mpweya wako lili ngati ma apulosi,
Na da dadi ifaba: le heda: le, ea fage faimu. Na da dia dodo waini fage sosogoi agoai ba: sa, amola dia mifo amo ‘a: bele’ fage ea gabusiga: defele gala.
9 ndipo pakamwa pako pali ngati vinyo wokoma kwambiri. Mkazi Tsono vinyo ameneyu amuthirire wachikondi wanga, ayenderere bwino pa milomo yake ndi mano ake.
Amola dia lafi da baligili noga: i waini defele gala.” Uda da amane sia: sa, “Defea! Amo waini hano da moloiwane na sasagesu dunu masunu da defea. Waini hano da ea lafi amola ea bese amodili musa: le sa: imu da defea.
10 Wokondedwayo ine ndine wake, ndipo chilakolako chake chili pa ine.
Na da na sasagesu dunu ea: Amola e da na hanasa.
11 Bwera wachikondi wanga, tiye tipite ku madera a ku midzi, tikagone ku midzi.
Na dogolegei! Misa! Ani da hamega gadili amoga asili, diasu gilisisu fonobahadi amo ganodini gasi afae golamu.
12 Tiye tilawirire mmamawa kupita ku minda ya mpesa, tikaone ngati mitengo ya mpesa yayamba kuphukira, ngati maluwa ake ayamba kuoneka, komanso ngati makangadza ayamba kuonetsa maluwa. Kumeneko ndidzakuonetsa chikondi changa.
Ani da hahabedafa wa: legadole, waini efe sagai muni, heda: bayale amola sogea da falegabeyale, amola ‘bomegala: nidi’ ifa sogea heda: bayale abodemu. Amogawi na da dima sasagesu imunu.
13 Mitengo ya mankhwala a chisulo ikupereka fungo lake labwino, ndipo pa khomo pathu pali zipatso zonse zokoma, zatsopano ndi zakale zomwe, zimene ndakusungira wokondedwa wanga.
Di da ‘ma: nadala: ige’ ea gabusiga: noga: idafa nabimu. Amola fage noga: idafa ania logo ga: su gadenene ligi dialebe ba: mu. Na dogolegei! Na gaheabolo amola hea hahawane hamosu amo dima imunusa: modai diala.