< Nyimbo ya Solomoni 5 >
1 Ndalowa mʼmunda mwanga, iwe mlongo wanga, iwe mkwatibwi wanga; ndasonkhanitsa mure wanga ndi zokometsera zakudya zanga. Ndadya uchi wanga pamodzi ndi zisa zake zomwe; ndamwa vinyo wanga ndi mkaka wanga. Abwenzi Idyani abwenzi anga, imwani; Inu okondana, imwani kwambiri.
Ka ngannu vasanu aw, kamah dum la ka lo coeng. Ka murrah neh ka botui te ka bit. Ka duup neh ka khoitui ka caak. Ka misurtui neh ka suktui khaw ka ok coeng. Rhoihui Ka hui long khaw ca saeh. O saeh lamtah ka hlo rhoek khaw rhuihmil pai saeh.
2 Ndinagona tulo koma mtima wanga unali maso. Tamverani, bwenzi langa akugogoda: “Nditsekulire, mlongo wanga, bwenzi langa, nkhunda yanga, wangwiro wanga. Mutu wanga wanyowa ndi mame, tsitsi langa lanyowa chifukwa cha nkhungu ya usiku.”
Ka ih muelh vaengah ka hlo kah a khoek ol loh ka lungbuei a haeng. Ka ngannu, ka cangyaeh, ka vahui neh ka cuemhmuet aw kai hamla ong pai. Ka lu dongkah ka sampin khaw khoyin tuicip, buemtui hah coeng.
3 Ndavula kale zovala zanga, kodi ndizivalenso? Ndasamba kale mapazi anga kodi ndiwadetsenso?
Ka angkidung te ka pit coeng tih metlam ka bai eh? Ka kho te ka silh dae metlam ka ti sak eh?
4 Bwenzi langa anapisa dzanja lake pa chibowo cha pa chitseko; mtima wanga unagunda chifukwa cha iye.
Ka hlo loh a kut te a put longah a thawt tih anih ham ka ko umya.
5 Ndinanyamuka kukamutsekulira wachikondi wangayo, ndipo manja anga anali noninoni ndi mure, zala zanga zinali mure chuchuchu, pa zogwirira za chotsekera.
Kamah hlo te ong pah ham kamah ka thoh vaengah ka kut dongah murrah cip. Ka kutdawn dongkah murrah te thohhna kut dongla long.
6 Ndinamutsekulira wachikondi wanga, koma nʼkuti wachikondi wangayo atachoka; iye anali atapita. Mtima wanga unafumuka chifukwa cha kuchoka kwake. Ndinamuyangʼanayangʼana koma sindinamupeze. Ndinamuyitana koma sanandiyankhe.
Ka hlo hamla ka ong pah vaengah ka hlo tah dongpam tih khum. Ka hinglu tah anih voek hamla cet coeng. Anih te ka toem dae amah ka hmuh moenih. Amah ka khue dae kai n'doo moenih.
7 Alonda anandipeza pamene ankayendera mzindawo. Anandimenya ndipo anandipweteka; iwo anandilanda mwinjiro wanga, alonda a pa khoma aja!
Khopuei ah aka hil tih aka tawt rhoek loh kai m'hmuh tih kai te n'ngawn uh. Vongtung aka tawt rhoek loh kai te n'hi sak uh tih ka pum dong lamkah ka lumuek hni te a phueih uh.
8 Inu akazi a ku Yerusalemu ndithu ndikukupemphani, mukapeza wokondedwa wangayo, kodi mudzamuwuza chiyani? Muwuzeni kuti ine ndadwala nacho chikondi.
Jerusalem nu nang te ka caeng coeng. Kai hlo te na hmu koinih ka lungnah a tloh te a taengah metlam na thui eh?
9 Iwe wokongola kuposa akazi onsewa, kodi wokondedwa wakoyo ndi wopambana wina aliyense bwanji? Kodi wokondedwa wakoyo ndi wopambana ena onse chotani kuti uzichita kutipempha motere?
Huta khuikah sakthen aw, kai hlo lakah nang hlo te metlam a om? Kaimih nan caeng van bangla a hlo lakah nang hlo tah tloe a?
10 Wokondedwa wangayo ndi wowala kwambiri ndi wathanzi pakati pa anthu 1,000.
Kamah hlo tah ngo tih thim, a thawngsang soah hnitai la pai.
11 Mutu wake ndi golide woyengeka bwino; tsitsi lake ndi lopotanapotana, ndiponso lakuda bwino ngati khwangwala.
A lu tah sui kah suicilh la om, a sampin bu tih vangak bangla muem.
12 Maso ake ali ngati nkhunda mʼmbali mwa mitsinje ya madzi, ngati nkhunda zitasamba mu mkaka, zitayima ngati miyala yamtengowapatali.
A mik rhoi tah sokca tui taengkah vahui bangla, suktui neh a yuh tih a hol hnothen bangla om.
13 Masaya ake ali ngati timinda ta mbewu zokometsera zakudya zopatsa fungo lokoma. Milomo yake ili ngati maluwa okongola amene akuchucha mure.
A kam rhoi tah canglak botui, rhaltoeng bo-ul bangla, a hmuilai tah tuilipai neh murrah tuicip la long.
14 Manja ake ali ngati ndodo zagolide zokongoletsedwa ndi miyala yamtengowapatali. Thupi lake ndi losalala ngati mnyanga wanjovu woyikamo miyala ya safiro.
A kut tah timsuih neh a moep sui hnaai van pawn ni. A bung khaw vueino saphi, minhum mueithuh van pawn ni.
15 Miyendo yake ili ngati mizati yamwala, yokhazikika pa maziko a golide. Maonekedwe ake ali ngati Lebanoni, abwino kwambiri ngati mkungudza.
A phai rhoi tah suicilh buenhol dongkah a sut lungbok tung van pawn ni. A mueimae neh Lebanon kah lamphai thing coelh van pawn ni.
16 Milomo yake ndi yosangalatsa kwambiri; munthuyo ndi wokongola kwambiri! Uyu ndiye wachikondi wanga ndi bwenzi langa, inu akazi a ku Yerusalemu.
Kamah hlo he a ka didip tih a pum la ngailaemnah la om. He tah ka hui Jerusalem nu.